詩篇 53 – JCB & CCL

Japanese Contemporary Bible

詩篇 53:1-6

53

1「神などいない」と言うのは愚か者です。

心がひねくれていて、

うしろ暗い生活を送っている証拠です。

その人のいのちは罪にむしばまれています。

2神は天から全人類を見下ろして、

だれか一人でも、正しいことを行い、

心から神を求める者がいないかと、

探しておられます。

3しかし、神に背いていない人間などいません。

人々は罪にまみれ、芯まで腐りきっています。

正しい者は一人もいません。

4どうしてこんなことになったのでしょう。

彼らはわからないのでしょうか。

彼らはパンのように、わたしの民を食いちぎり、

神に立ち返ろうとしないからです。

5しかし、そのうち、

かつてないほどの恐怖に取りつかれます。

神は、このような敵どもを見捨て、

その骨をばらまかれます。

6ああ、今、神がシオンからおいでになって、

イスラエルを救ってくださいますように。

主ご自身が人々を元どおりにされるとき、

人々は再び幸せになれるのです。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 53:1-6

Salimo 53

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a Mahalati. Ndakatulo ya Davide.

1Chitsiru chimati mu mtima mwake,

“Kulibe Mulungu.”

Iwo ndi oyipa ndipo njira zawo ndi zonyansa;

palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino.

2Mulungu kumwamba amayangʼana pansi pano

pa ana a anthu

kuti aone ngati alipo wina wanzeru,

wofunafuna Mulungu.

3Aliyense wabwerera,

iwo onse pamodzi akhala oyipa;

palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino,

ngakhale mmodzi.

4Kodi anthu ochita zoyipawa adzaphunziradi;

anthu amene amadya anthu anga monga mmene anthu amadyera buledi,

ndipo sapemphera kwa Mulungu?

5Iwo anali pamenepo atathedwa nzeru ndi mantha aakulu

pamene panalibe kanthu kochititsa mantha.

Mulungu anamwazamwaza mafupa a anthu amene anakuthirani nkhondo;

inuyo munawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawanyoza.

6Ndithu, chipulumutso cha Israeli nʼchochokera ku Ziyoni!

Pamene Mulungu adzabwezeretsanso ulemerero wa anthu ake,

lolani Yakobo akondwere ndi Israeli asangalale!