Masalimo 54 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 54:1-7

Salimo 54

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.”

1Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu;

onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu.

2Imvani pemphero langa, Inu Mulungu

mvetserani mawu a pakamwa panga.

3Alendo akundithira nkhondo;

anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga,

anthu amene salabadira za Mulungu.

4Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa;

Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.

5Lolani kuti choyipa chifike pa iwo amene amandichita chipongwe;

mwa kukhulupirika kwanu awonongeni.

6Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu;

ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova,

pakuti ndi labwino.

7Pakuti Iyeyo wandipulumutsa ku masautso anga onse,

ndipo maso anga apenya kupambana kwa pa adani anga.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 54:1-7

Zabbuli 54

Ya Mukulu wa Bayimbi. Eyimbibwa n’ebivuga eby’enkoba. Zabbuli ya Dawudi, Abazifu bwe bajja ne babuulira Sawulo nti, “Dawudi yeekwese mu ffe.”

154:1 a Zab 20:1 b 2By 20:6Olw’erinnya lyo ondokole, Ayi Katonda,

n’amaanyi go amangi onzigyeko omusango.

254:2 Zab 5:1; 55:1Wulira okusaba kwange, Ayi Katonda,

owulirize ebigambo by’omu kamwa kange.

354:3 a Zab 86:14 b Zab 40:14 c Zab 36:1Abantu be simanyi bannumba;

abantu abalina ettima abatatya Katonda;

bannoonya okunzita.

454:4 a Zab 118:7 b Zab 41:12Laba, Katonda ye mubeezi wange,

Mukama ye mukuumi wange.

554:5 a Zab 94:23 b Zab 89:49; 143:12Leka ebintu ebibi byonna bye bantegekera, bibeekyusize,

obazikirize olw’obwesigwa bwo.

654:6 a Zab 50:14 b Zab 52:9Nnaakuleeteranga ssaddaaka ey’ekyeyagalire;

ne ntendereza erinnya lyo, Ayi Mukama,

kubanga ddungi.

754:7 a Zab 34:6 b Zab 59:10Kubanga Katonda amponyezza ebizibu byange byonna;

era amaaso gange galabye ng’awangula abalabe bange.