Salimo 23
Salimo la Davide.
1Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
2Amandigoneka pa msipu wobiriwira,
amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
3amatsitsimutsa moyo wanga.
Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo
chifukwa cha dzina lake.
4Ngakhale ndiyende
mʼchigwa cha mdima wakuda bii,
sindidzaopa choyipa,
pakuti Inu muli ndi ine;
chibonga chanu ndi ndodo yanu
zimanditonthoza.
5Mumandikonzera chakudya
adani anga akuona.
Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta;
chikho changa chimasefukira.
6Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata
masiku onse a moyo wanga,
ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova
kwamuyaya.
Zaburi 23
Bwana Mchungaji Wetu
Zaburi ya Daudi.
123:1 Mwa 48:15; Yn 10:11; Flp 4:19; Za 28:9; 34:9, 10; 84:11; 107:9; 1Pet 2:25Bwana ndiye mchungaji wangu,
sitapungukiwa na kitu.
223:2 Eze 34:14; Ufu 7:17; Za 36:8; 46:4Hunilaza katika malisho
ya majani mabichi,
kando ya maji matulivu huniongoza,
323:3 Isa 42:16; Za 5:8; 106:8; 19:7; 79:9; 25:9, 11; 73:24; 31:3; 109:21; 143:11hunihuisha nafsi yangu.
Huniongoza katika njia za haki
kwa ajili ya jina lake.
423:4 Ay 3:5; Za 107:14; Isa 43:2; Za 3:6; 27:1; 16:8; 46:11; Isa 8:10; Zek 8:23; Mt 1:23; Mdo 18:9, 10Hata kama nikipita katikati
ya bonde la uvuli wa mauti,
sitaogopa mabaya,
kwa maana wewe upo pamoja nami;
fimbo yako na mkongojo wako
vyanifariji.
523:5 Ay 36:16; Za 16:5; 45:7; 92:10; Lk 7:46Waandaa meza mbele yangu
machoni pa adui zangu.
Umenipaka mafuta kichwani pangu,
kikombe changu kinafurika.
623:6 Neh 9:25; 2Kor 5:1Hakika wema na upendo vitanifuata
siku zote za maisha yangu,
nami nitakaa nyumbani mwa Bwana
milele.