Masalimo 23 – CCL & NEN

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 23:1-6

Salimo 23

Salimo la Davide.

1Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.

2Amandigoneka pa msipu wobiriwira,

amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,

3amatsitsimutsa moyo wanga.

Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo

chifukwa cha dzina lake.

4Ngakhale ndiyende

mʼchigwa cha mdima wakuda bii,

sindidzaopa choyipa,

pakuti Inu muli ndi ine;

chibonga chanu ndi ndodo yanu

zimanditonthoza.

5Mumandikonzera chakudya

adani anga akuona.

Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta;

chikho changa chimasefukira.

6Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata

masiku onse a moyo wanga,

ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova

kwamuyaya.

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 23:1-6

Zaburi 23

Bwana Mchungaji Wetu

Zaburi ya Daudi.

123:1 Mwa 48:15; Yn 10:11; Flp 4:19; Za 28:9; 34:9, 10; 84:11; 107:9; 1Pet 2:25Bwana ndiye mchungaji wangu,

sitapungukiwa na kitu.

223:2 Eze 34:14; Ufu 7:17; Za 36:8; 46:4Hunilaza katika malisho

ya majani mabichi,

kando ya maji matulivu huniongoza,

323:3 Isa 42:16; Za 5:8; 106:8; 19:7; 79:9; 25:9, 11; 73:24; 31:3; 109:21; 143:11hunihuisha nafsi yangu.

Huniongoza katika njia za haki

kwa ajili ya jina lake.

423:4 Ay 3:5; Za 107:14; Isa 43:2; Za 3:6; 27:1; 16:8; 46:11; Isa 8:10; Zek 8:23; Mt 1:23; Mdo 18:9, 10Hata kama nikipita katikati

ya bonde la uvuli wa mauti,

sitaogopa mabaya,

kwa maana wewe upo pamoja nami;

fimbo yako na mkongojo wako

vyanifariji.

523:5 Ay 36:16; Za 16:5; 45:7; 92:10; Lk 7:46Waandaa meza mbele yangu

machoni pa adui zangu.

Umenipaka mafuta kichwani pangu,

kikombe changu kinafurika.

623:6 Neh 9:25; 2Kor 5:1Hakika wema na upendo vitanifuata

siku zote za maisha yangu,

nami nitakaa nyumbani mwa Bwana

milele.