Salimo 24
Salimo la Davide.
1Dziko lapansi ndi la Yehova ndi zonse zimene zili mʼmenemo,
dziko ndi onse amene amakhala mʼmenemo;
2pakuti Iye ndiye anayika maziko ake pa nyanja
ndi kulikhazika pamwamba pa madzi.
3Ndani angakwere phiri la Yehova?
Ndani angathe kuyima pa malo ake opatulika?
4Iye amene ali ndi mʼmanja moyera ndi mtima woyera,
amene sapereka moyo wake kwa fano
kapena kulumbira mwachinyengo.
5Iyeyo adzalandira madalitso kwa Yehova
ndipo Mulungu mpulumutsi wake adzagamula kuti alibe mlandu.
6Umenewo ndiwo mʼbado wa amene amafunafuna Yehova;
amene amafunafuna nkhope yanu, Inu Mulungu wa Yakobo.
Sela
7Tukulani mitu yanu inu zipata;
tsekukani, inu zitseko zakalekalenu,
kuti Mfumu yaulemerero ilowe.
8Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?
Yehova Wamphamvuzonse,
Yehova ndiye wamphamvu pa nkhondo.
9Tukulani mitu yanu, inu zipata;
tsekukani, inu zitseko zakalekalenu,
kuti Mfumu yaulemerero ilowe.
10Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?
Yehova Wamphamvuzonse,
Iye ndiye Mfumu yaulemerero.
Sela
Zaburi 24
Mfalme Mkuu
Zaburi ya Daudi.
124:1 Kut 9:29; Ay 41:11; 1Kor 10:26Dunia ni mali ya Bwana, na vyote vilivyomo ndani yake,
ulimwengu, na wote waishio ndani yake,
224:2 Za 104:3; Mwa 1:6; 2Pet 3:5maana aliiwekea misingi yake baharini
na kuifanya imara juu ya maji.
324:3 Za 2:6; 15:1; 65:4Nani awezaye kuupanda mlima wa Bwana?
Ni nani awezaye kusimama patakatifu pake?
424:4 2Sam 22:21; Za 51:10; 73:1; Mt 5:8; Eze 18:15Ni yule mwenye mikono safi na moyo mweupe,
yule ambaye hakuinulia sanamu nafsi yake
au kuapa kwa kitu cha uongo.
524:5 Kum 11:26; Za 17:2Huyo atapokea baraka kutoka kwa Bwana,
na hukumu ya haki kutoka kwa Mungu Mwokozi wake.
624:6 Za 27:8; 105:4; 119:58; Hos 5:15Hiki ndicho kizazi cha wale wamtafutao,
wale wautafutao uso wako, Ee Mungu wa Yakobo.
724:7 Isa 26:2; 60:11, 18; 62:10; Za 74:12; 29:3; 118:19, 20; 44:4; Mdo 7:2; 1Kor 2:8; Zek 9:9; Mt 21:5; Hag 2:7; Mal 3:1Inueni vichwa vyenu, enyi malango,
inukeni enyi milango ya kale,
ili mfalme wa utukufu apate kuingia.
824:8 1Nya 29:11; Za 89:13; Kum 4:34; Yer 50:34; Efe 6:10; Kut 15:3, 6Ni nani huyu Mfalme wa utukufu?
Ni Bwana aliye na nguvu na uweza,
ni Bwana aliye hodari katika vita.
9Inueni vichwa vyenu, enyi malango,
viinueni juu enyi milango ya kale,
ili Mfalme wa utukufu apate kuingia.
1024:10 1Sam 1:11Ni nani yeye, huyu Mfalme wa utukufu?
Ni Bwana Mwenye Nguvu Zote;
yeye ndiye Mfalme wa utukufu.