Masalimo 127 – CCL & NVI

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 127:1-5

Salimo 127

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni.

1Yehova akapanda kumanga nyumba,

omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe.

Yehova akapanda kulondera mzinda,

mlonda akanangolondera pachabe.

2Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa

ndi kusagona msanga madzulo,

kuvutikira chakudya choti mudye,

pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.

3Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova,

ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.

4Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja

mwa munthu wankhondo.

5Wodala munthu

amene motengera mivi mwake mwadzaza.

Iwo sadzachititsidwa manyazi

pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.

Nueva Versión Internacional

Salmo 127:1-5

Salmo 127

Cántico de los peregrinos. De Salomón.

1Si el Señor no edifica la casa,

en vano se esfuerzan los albañiles.

Si el Señor no cuida la ciudad,

en vano hacen guardia los vigilantes.

2En vano madrugan ustedes

y se acuestan muy tarde

para comer un pan de fatigas,

porque Dios lo da a sus amados mientras duermen.

3Los hijos son una herencia del Señor,

el fruto del vientre es una recompensa.

4Como flechas en las manos del guerrero

son los hijos de la juventud.

5Dichoso aquel que llena su aljaba

con esta clase de flechas.127:5 con esta clase de flechas. Lit. con ellos.

No será avergonzado por sus enemigos

cuando litiguen contra él en los tribunales.