Salimo 125
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,
limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,
momwemonso Yehova azungulira anthu ake
kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala
pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama,
kuti anthu olungamawo
angachite nawonso zoyipa.
4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,
amene ndi olungama mtima
5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,
Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa.
Mtendere ukhale pa Israeli.
Tryghed hos Herren
1En valfartssang.
De, der stoler på Herren,
står fast som Zions bjerg.
I evighed rokkes de ikke.
2Som bjergene omslutter Jerusalem,
vil Herren altid omslutte sit folk.
3Onde konger skal ikke herske for evigt
over det land, Gud gav de gudfrygtige,
for ellers ville de glemme deres gudsfrygt.
4Herre, vis godhed mod de gode,
de, som har et oprigtigt hjerte.
5Men de, som slår ind på ondskabens vej,
vil Herren jage bort sammen med de onde.
Fred være med Israel!