Masalimo 126 – CCL & BPH

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 126:1-6

Salimo 126

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni,

tinali ngati amene akulota.

2Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka;

malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe.

Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti,

“Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”

3Yehova watichitira zinthu zazikulu,

ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.

4Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova,

monga mitsinje ya ku Negevi.

5Iwo amene amafesa akulira,

adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.

6Iye amene amayendayenda nalira,

atanyamula mbewu yokafesa,

adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe,

atanyamula mitolo yake.

Bibelen på hverdagsdansk

Salmernes Bog 126:1-6

Guds hjemvendte folk

1En valfartssang.

Da Herren bragte os hjem til Zion,

var det, som om vi drømte.

2Vi lo og jublede, vi sang af glæde.

Folkeslagene udbrød: „Herren har gjort et under for sit folk!”

3Ja, Herren har gjort et under for os,

vi jubler af glæde.

4Herre, velsign os igen og giv os fremgang,

som regnen fylder de udtørrede floder.

5De, der såede med gråd,

skal høste med glæde.

6Grædende spredte de sæden ud,

syngende bringer de høsten i hus.