Masalimo 121 – CCL & NRT

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 121:1-8

Salimo 121

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Ndikweza maso anga ku mapiri;

kodi thandizo langa limachokera kuti?

2Thandizo langa limachokera kwa Yehova,

wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.

3Sadzalola kuti phazi lako literereke;

Iye amene amakusunga sadzawodzera.

4Taonani, Iye amene amasunga Israeli

sadzawodzera kapena kugona.

5Yehova ndiye amene amakusunga;

Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.

6Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,

kapena mwezi nthawi ya usiku.

7Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;

adzasunga moyo wako.

8Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

New Russian Translation

Псалтирь 121:1-9

Псалом 121

1Песнь восхождения Давида.

Обрадовался я, когда мне сказали:

«Пойдем в дом Господень».

2Ноги наши стоят

у твоих ворот, Иерусалим.

3Иерусалим – плотно застроенный город.

4Туда поднимаются роды, роды Господни,

по предписанию121:4 Букв.: «по свидетельству»., данному Израилю,

воздать хвалу имени Господа.

5Там стоят престолы суда,

престолы дома Давидова.

6Молитесь о мире для Иерусалима:

«Пусть будут благополучны любящие тебя.

7Пусть будет мир в твоих стенах

и благополучие в твоих дворцах».

8Ради братьев и моих друзей

скажу: «Мир тебе!»

9Ради дома Господа, нашего Бога,

желаю блага тебе, Иерусалим.