Masalimo 120 – CCL & CCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 120:1-7

Salimo 120

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga,

ndipo Iye amandiyankha.

2Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza,

ndi kwa anthu achinyengo.

3Kodi adzakuchitani chiyani,

ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?

4Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo,

ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.

5Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki,

kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!

6Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati

pa iwo amene amadana ndi mtendere.

7Ine ndine munthu wamtendere;

koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

诗篇 120:1-7

第 120 篇

祈求上帝帮助

上圣殿朝圣之诗。

1我在患难中向耶和华祷告,

祂就应允了我。

2耶和华啊,

求你救我远离虚谎诡诈之徒。

3诡诈之徒啊!

你会受到怎样的惩罚呢?

你会有什么下场呢?

4等待你的是勇士的利箭和炙热的炭火。

5我寄居在米设基达的人当中有祸了!

6我住在憎恶和平的人当中太久了。

7我爱和平,

但我倡导和平的时候,

他们却要战争。