Salimo 112
1Tamandani Yehova.
Wodala munthu amene amaopa Yehova,
amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.
2Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko;
mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.
3Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake,
ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima;
wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.
5Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu,
amene amachita ntchito yake mwachilungamo.
6Ndithu sadzagwedezeka;
munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.
7Saopa akamva zoyipa zimene zachitika;
mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.
8Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha;
potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.
9Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka,
chilungamo chake chimanka mpaka muyaya;
nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.
10Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima;
adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka.
Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.
خوشبختی درستكاران
1خداوند را سپاس باد!
خوشا به حال كسی كه از خداوند میترسد و احكام او را با رغبت انجام میدهد. 2فرزندان شخص درستكار در دنيا نيرومند خواهند شد و نسل او بركت خواهند يافت. 3خانوادهاش صاحب مال و ثروت خواهد شد و خوبیهای او هرگز از ياد نخواهد رفت.
4برای كسی كه درستكار و بخشنده، مهربان و نيكوكار است، حتی در تاريكی شب نيز نور طلوع میكند. 5خوشبخت است كسی كه دلسوز و قرض دهنده باشد و در كسب و كارش با انصاف باشد. 6او در زندگی پيوسته ثابت قدم و پايدار خواهد بود و نام نيكش هميشه در يادها باقی خواهد ماند.
7او از شنيدن خبر بد نمیترسد، زيرا ايمان او قوی است و بر خداوند توكل دارد. 8او نگران نمیشود و نمیترسد زيرا مطمئن است كه شكست دشمنانش را خواهد ديد. 9با سخاوتمندی به فقيران میبخشد؛ اثرات نيكوكاری او تا ابد باقی میماند و هميشه نزد مردم سربلند و محترم میباشد. 10بدكاران اين را میبينند و خشمگين میشوند؛ دندانهای خود را به هم میفشارند و همراه آرزوهايشان از بين میروند.