Masalimo 110 – CCL & NRT

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 110:1-7

Salimo 110

Salimo la Davide.

1Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti,

“Khala ku dzanja langa lamanja

mpaka nditasandutsa adani ako

kukhala chopondapo mapazi ako.”

2Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni;

udzalamulira pakati pa adani ako.

3Ankhondo ako adzakhala odzipereka

pa tsiku lako la nkhondo.

Atavala chiyero chaulemerero,

kuchokera mʼmimba ya mʼbandakucha,

udzalandira mame a unyamata wako.

4Yehova walumbira

ndipo sadzasintha maganizo ake:

“Ndiwe wansembe mpaka muyaya

monga mwa unsembe wa Melikizedeki.”

5Ambuye ali kudzanja lako lamanja;

Iye adzaponda mafumu pa tsiku la ukali wake.

6Adzaweruza anthu a mitundu ina,

adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo ndipo adzaphwanya olamulira a pa dziko lonse lapansi.

7Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira;

choncho adzaweramutsa mutu wake.

New Russian Translation

Псалтирь 110:1-10

Псалом 110110 Псалом 110 В оригинале этот псалом написан в форме акростиха, т. е. каждая строка начинается с очередной буквы еврейского алфавита.

1Аллилуйя!

Славлю Господа всем своим сердцем

в совете праведных и в собрании.

2Велики дела Господа,

желанны всеми, кто любит их.

3Славны и великолепны деяния Его;

праведность Его пребудет вечно.

4Памятными сделал Он Свои дела;

милостив и милосерден Господь.

5Он дает пищу боящимся Его,

вечно помнит Свой завет.

6Народу Своему Он явил силу Своих дел,

отдав им землю чужих народов.

7Дела Его рук истинны и справедливы,

Его наставления верны.

8Вечно тверды они

и основаны на истине и правоте.

9Своему народу послал Он избавление,

установил навечно Свой завет.

Его имя свято и грозно!

10Начало мудрости – страх перед Господом.

Разумны те, кто исполняет Его наставления.

Вечная хвала Ему.