Salimo 111
1Tamandani Yehova.
Ndidzathokoza Yehova ndi mtima wanga wonse
mʼbwalo la anthu olungama mtima ndi pa msonkhano.
2Ntchito za Yehova nʼzazikulu;
onse amene amakondwera nazo amazilingalira.
3Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu,
ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike;
Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo.
5Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye;
amakumbukira pangano lake kwamuyaya.
6Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake,
kuwapatsa mayiko a anthu a mitundu ina.
7Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama;
malangizo ake onse ndi odalirika.
8Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi,
ochitidwa mokhulupirika ndi molungama.
9Iyeyo amawombola anthu ake;
anakhazikitsa pangano lake kwamuyaya
dzina lake ndi loyera ndi loopsa.
10Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru;
onse amene amatsatira malangizo ake amamvetsa bwino zinthu.
Iye ndi wotamandika mpaka muyaya.
Псалом 111111 Псалом 111 В оригинале этот псалом написан в форме акростиха, т. е. каждая строка начинается с очередной буквы еврейского алфавита.
1Аллилуйя!
Блажен человек, боящийся Господа,
получающий большое наслаждение от Его повелений.
2Могущественным будет на земле его потомство;
поколение праведных благословится.
3Изобилие и богатство будут в его доме,
и его праведность будет пребывать вечно.
4Для честных восходит свет во тьме,
он милостив, милосерден и праведен111:4 Или: « … во тьме, потому что Бог … ».
5Благо человеку, который великодушен и щедро дает взаймы,
тому, кто ведет свои дела справедливо.
6Он никогда не поколеблется;
праведник будет в вечной памяти.
7Не побоится плохих известий;
сердце его твердо, уповая на Господа.
8Сердце его крепко – он не испугается;
он увидит падение своих врагов.
9Он щедро раздал свое имущество бедным,
и его праведность пребывает вовек,
рог111:9 Рог был символом могущества, власти и силы. его вознесется в славе.
10Нечестивый увидит и разозлится,
заскрипит зубами и исчезнет.
Желание нечестивых не сбудется.