Zaburi 5 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 5:1-12

Zaburi 5

Sala Kwa Ajili Ya Ulinzi Wakati Wa Hatari

Kwa mwimbishaji. Kwa filimbi. Zaburi ya Daudi.

15:1 1Fal 8:29; Za 17:1; 38:9; 40:1; 116:2; Dan 9:18; Isa 35:10; 51:11Ee Bwana, tegea sikio maneno yangu,

uangalie kupiga kite kwangu.

25:2 Ay 19:7; 24:12; 36:5; Za 44:4; 68:24; 84:3Sikiliza kilio changu ili unisaidie,

Mfalme wangu na Mungu wangu,

kwa maana kwako ninaomba.

35:3 Isa 28:19; 50:4; Yer 21:12; Sef 3:5; Eze 46:13; Hab 2:1; Rum 8:19; Za 30:5; 62:1; 119:81; 130:5Asubuhi, unasikia sauti yangu, Ee Bwana;

asubuhi naleta haja zangu mbele zako,

na kusubiri kwa matumaini.

45:4 Za 1:5; 11:5; 104:35; Mit 2:22; Mal 2:17Wewe si Mungu unayefurahia uovu,

kwako mtu mwovu hataishi.

55:5 2Fal 19:32; Za 1:5; 45:10; 1:3; 119:104; 73:3; 75:4; 14:1; Isa 33:19; 37:33; Mit 8:13; Hab 1:13Wenye kiburi hawawezi kusimama mbele yako,

unawachukia wote watendao mabaya.

65:6 Mit 19:22; Yn 8:44; Mdo 5:3; Ufu 21:8Unawaangamiza wasemao uongo.

Bwana huwachukia

wamwagao damu na wadanganyifu.

75:7 Kum 13:4; Yer 44:10; Dan 6:26; 2Sam 12:16; Za 138:2; 1Fal 8:48Lakini mimi, kwa rehema zako kuu,

nitakuja katika nyumba yako,

kwa unyenyekevu, nitasujudu

kuelekea Hekalu lako takatifu.

85:8 Za 23:3; 31:1; 71:2; 85:13; 89:16; Mit 8:20; 1Fal 8:36; Yn 1:23Niongoze katika haki yako, Ee Bwana,

kwa sababu ya adui zangu,

nyoosha njia yako mbele yangu.

95:9 Yer 5:16; Lk 11:44; Za 12:2; 28:3; 36:3; Yer 9:8; Rum 3:135:9 Isa 13:8; Yer 46:5Hakuna neno kinywani mwao linaloweza kuaminika,

mioyo yao imejaa maangamizi.

Koo lao ni kaburi lililo wazi,

kwa ndimi zao, wao hunena udanganyifu.

105:10 Mao 1:5; 3:42; Za 78:40; 106:7; 107:11Uwatangaze kuwa wenye hatia, Ee Mungu!

Hila zao ziwe anguko lao wenyewe.

Wafukuzie mbali kwa sababu ya dhambi zao nyingi,

kwa kuwa wamekuasi wewe.

115:11 1Kor 2:9; Za 33:1; 81:1; 90:14; 92:4; 95:1; 145:7; 69:36; 119:132; Ay 22:19Lakini wote wakimbiliao kwako na wafurahi,

waimbe kwa shangwe daima.

Ueneze ulinzi wako juu yao,

ili wale wapendao jina lako

wapate kukushangilia.

125:12 Za 112:2; 32:7; Mwa 15:1Kwa hakika, Ee Bwana, unawabariki wenye haki,

unawazunguka kwa wema wako kama ngao.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 5:1-12

Salimo 5

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe zoyimbira za zitoliro. Salimo la Davide.

1Tcherani khutu ku mawu anga, Inu Yehova,

ganizirani za kusisima kwanga

2Mverani kulira kwanga kofuna thandizo,

Mfumu yanga ndi Mulungu wanga,

pakuti kwa Inu, ine ndikupemphera.

3Mmawa, Yehova mumamva mawu anga;

Mmawa ndimayala zopempha zanga pamaso panu

ndi kudikira mwachiyembekezo.

4Inu si Mulungu amene mumasangalala ndi zoyipa;

choyipa sichikhala pamaso panu.

5Onyada sangathe kuyima pamaso panu;

Inu mumadana ndi onse ochita zoyipa.

6Mumawononga iwo amene amanena mabodza;

anthu akupha ndi achinyengo,

Yehova amanyansidwa nawo.

7Koma Ine, mwa chifundo chanu chachikulu,

ndidzalowa mʼNyumba yanu;

mwa ulemu ndidzaweramira pansi

kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera.

8Tsogolereni Inu Yehova, mwa chilungamo chanu

chifukwa cha adani anga ndipo

wongolani njira yanu pamaso panga.

9Palibe mawu ochokera mʼkamwa mwawo amene angadalirike;

mtima wawo wadzaza ndi chiwonongeko.

Kummero kwawo kuli ngati manda apululu;

ndi lilime lawo amayankhula zachinyengo.

10Lengezani kuti ndi olakwa, Inu Mulungu!

Zochita zawo zoyipa zikhale kugwa kwawo.

Achotseni pamaso panu chifukwa cha machimo awo ambiri,

pakuti awukira Inu.

11Koma lolani kuti onse amene apeza chitetezo mwa Inu akondwere;

lolani kuti aziyimba nthawi zonse chifukwa cha chimwemwe.

Aphimbeni ndi chitetezo chanu,

iwo amene amakonda dzina lanu akondwere mwa Inu.

12Ndithu, Inu Yehova, mumadalitsa olungama;

mumawazungulira ndi kukoma mtima kwanu ngati chishango.