Zaburi 4 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 4:1-8

Zaburi 4

Sala Ya Jioni Ya Kuomba Msaada

Kwa mwimbishaji. Kwa ala za nyuzi za muziki. Zaburi ya Daudi.

14:1 Za 13:3; 27:7; 69:16; 30:10; 54:2; 84:8; 88:2; 6:7; 102:2; Mwa 32:7; Amu 2:15Nijibu nikuitapo,

Ee Mungu wangu mwenye haki!

Nipumzishe katika shida zangu;

nirehemu, usikie ombi langu.

24:2 Kut 16:7; Amo 2:4; 2Fal 19:26; Ay 8:22; Yer 13:25; 16:19; Za 12:1; 40:4; 1Sam 4:21Enyi watu, mtabadilisha utukufu wangu

kuwa aibu mpaka lini?

Mtapenda udanganyifu

na kufuata miungu ya uongo mpaka lini?

34:3 Za 6:8; 12:1; 30:4; 31:23; 79:2; Mik 7:2, 7; Kut 33:16; 1Tim 4:7; 2Pet 3:11Fahamuni hakika kwamba Bwana amewatenga

wale wamchao kwa ajili yake;

Bwana atanisikia nimwitapo.

44:4 Efe 4:26; Za 63:6; Dan 2:28; Mit 3:74:4 Za 11:1; 25:20; 31:2; 32:11Katika hasira yako, usitende dhambi.

Mkiwa vitandani mwenu, mtulie kimya

mkiichunguza mioyo yenu.

54:5 Za 31:6; 37:3; 115:9; Mit 3:5; 28:26; Kum 33:19; Yn 14:1; Isa 26:44:5 Hes 14:18; Isa 65:6-7; Yer 32:17Toeni dhabihu zilizo haki;

mtegemeeni Bwana.

64:6 Hes 6:25; Za 80:3Wengi wanauliza, “Ni nani awezaye

kutuonyesha jema lolote?”

Ee Bwana, tuangazie nuru ya uso wako.

74:7 Mdo 14:17; Isa 9:3; 35:10; 65:14, 18; Mwa 27:28; Kum 28:51Wewe umejaza moyo wangu kwa furaha kubwa

kuliko watu waliopata nafaka na divai kwa wingi.

84:8 Law 26:6; Hes 6:26; Yer 32:37; Ay 11:18; Flp 4:7; Kum 12:10; 33:28; Yn 14:274:8 Law 11:44Nitajilaza chini na kulala kwa amani,

kwa kuwa wewe peke yako, Ee Bwana,

waniwezesha kukaa kwa salama.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 4:1-8

Salimo 4

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide.

1Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu,

Inu Mulungu wa chilungamo changa.

Pumulitseni ku zowawa zanga;

chitireni chifundo ndi kumva pemphero langa.

2Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi?

Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza?

Sela.

3Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika;

Yehova adzamva pamene ndidzamuyitana.

4Kwiyani koma musachimwe;

pamene muli pa mabedi anu,

santhulani mitima yanu ndi kukhala chete.

Sela

5Perekani nsembe zolungama

ndipo dalirani Yehova.

6Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?”

Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova.

7Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu

kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano.

8Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere,

pakuti Inu nokha, Inu Yehova,

mumandisamalira bwino.