Yeremia 2 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Yeremia 2:1-37

Israeli Amwacha Mungu

12:1 Isa 38:4; Eze 1:3Neno la Bwana lilinijia kusema, 22:2 Za 71:17; Eze 16:8; Kut 13:21; Hos 2:15; Ufu 2:4; Isa 54:4; Yer 3:4; Kum 1:29“Nenda ukahubiri masikioni mwa watu wa Yerusalemu:

“ ‘Nakumbuka moyo wako wa uchaji katika ujana wako,

jinsi ulivyonipenda kama bibi arusi

na kunifuata katika jangwa lile lote,

katika nchi isiyopandwa mbegu.

32:3 Kut 19:6; Yak 1:18; Kum 7:6; Law 23:9-14; Yer 10:25; Ufu 14:4; Yer 30:16; 50:7Israeli alikuwa mtakatifu kwa Bwana,

kama malimbuko ya kwanza ya mavuno yake;

wote waliowaangamiza walihesabiwa kuwa na hatia,

nayo maafa yaliwakumba,’ ”

asema Bwana.

4Sikia neno la Bwana, ee nyumba ya Yakobo,

nanyi nyote jamaa za nyumba ya Israeli.

52:5 2Fal 17:15; Rum 1:21; Isa 44:9; Kum 32:21; 1Sam 12:21; Za 31:9Hivi ndivyo asemavyo Bwana:

“Je, baba zenu waliona kosa gani kwangu,

hata wakatangatanga mbali nami hivyo?

Walifuata sanamu zisizofaa,

nao wenyewe wakawa hawafai.

62:6 Hos 13:4; Kum 18:5; 32:10; Kut 6:6; Yer 51:43Hawakuuliza, ‘Yuko wapi Bwana,

aliyetupandisha kutoka Misri

na kutuongoza kupitia nyika kame,

kupitia nchi ya majangwa na mabonde,

nchi ya ukame na giza,

nchi ambayo hakuna mtu asafiriye ndani yake

wala hakuna mtu aishiye humo?’

72:7 Hes 13:27; Kum 11:10-12; Za 106:34-39; Kum 8:7-9; Yer 7:30; 16:18; Eze 36:17Niliwaleta katika nchi yenye wingi wa vitu

ili mpate kula matunda yake

na utajiri wa mazao yake.

Lakini mkaja na kuinajisi nchi yangu,

na kuufanya urithi wangu chukizo.

82:8 2Sam 2:12; Rum 2:20; 1Fal 18:22; Yer 23:13; Isa 40:19; Yer 4:22; 3:15; 9:14Makuhani hawakuuliza,

‘Yuko wapi Bwana?’

Wale wanaoshughulikia sheria hawakunijua mimi;

viongozi waliasi dhidi yangu.

Manabii walitabiri kwa jina la Baali,

wakifuata sanamu zisizofaa.

92:9 Isa 3:13; Mik 6:2; Eze 20:35-36; Yer 25:31“Kwa hiyo naleta tena mashtaka dhidi yako,”

asema Bwana.

“Nami nitaleta mashtaka dhidi ya watoto wa watoto wako.

102:10 Mwa 10:4; 25:13Vuka, nenda ngʼambo mpaka pwani ya Kitimu2:10 Kitimu hapa ni Kipro, kisiwa katika Bahari ya Mediterania. nawe uangalie,

tuma watu waende Kedari, wachunguze kwa makini,

uone kama kumekuwepo kitu kama hiki.

112:11 Gal 4:8; Isa 37:19; Za 106:20; Rum 1:23; Kum 4:5-9; 1Sam 4:21; Yer 16:20Je, taifa limebadili miungu yake wakati wowote?

(Hata ingawa hao si miungu kamwe.)

Lakini watu wangu wamebadili Utukufu wao

kwa sanamu zisizofaa kitu.

12Shangaeni katika hili, ee mbingu,

nanyi tetemekeni kwa hofu kuu,”

asema Bwana.

132:13 Za 36:9; Yn 4:14; Yer 17:13; Kum 31:16; Isa 65:11; 12:3“Watu wangu wametenda dhambi mbili:

Wameniacha mimi,

niliye chemchemi ya maji yaliyo hai,

nao wamejichimbia visima vyao wenyewe,

visima vilivyobomoka, visivyoweza kuhifadhi maji.

142:14 Kut 4:22; Yer 31:9Je, Israeli ni mtumishi, yaani mtumwa kwa kuzaliwa?

Kwa nini basi amekuwa mateka?

152:15 Yer 4:7; 50:17; 2Fal 25:9; Law 26:43Simba wamenguruma;

wamemngurumia.

Wameifanya nchi yake kuwa ukiwa;

miji yake imeteketezwa, nayo imeachwa haina watu.

162:16 Isa 19:13; Yer 43:7-9Pia watu wa Memfisi2:16 Memfisi kwa Kiebrania ni Nofu. na Tahpanhesi2:16 Tahpanhesi ni mji katika nchi ya Misri.

wamevunja taji ya kichwa chako.

172:17 Yer 4:18; Isa 1:28; Yer 17:13; 19:4Je, hukujiletea hili wewe mwenyewe

kwa kumwacha Bwana, Mungu wako

alipowaongoza njiani?

182:18 Isa 30:2; Hos 13:3; Eze 17:15; 2Fal 16:7; Hos 5:13; 7:11; Isa 7:20Sasa kwa nini uende Misri

kunywa maji ya Shihori?2:18 Kijito kinachoelekeza maji katika Mto Naili.

Nawe kwa nini kwenda Ashuru

kunywa maji ya Mto Frati?

192:19 Hos 14:4; Isa 59:12; Yer 14:7; Kut 19:5; Ay 20:14; Amo 8:10; Yer 3:11; 19:4Uovu wako utakuadhibu;

kurudi nyuma kwako kutakukemea.

Basi kumbuka, utambue

jinsi lilivyo ovu na chungu kwako

unapomwacha Bwana Mungu wako

na kutokuwa na hofu yangu,”

asema Bwana, Bwana Mwenye Nguvu Zote.

202:20 Law 26:13; Yer 3:23; Kum 12:2; Yer 5:5; Ay 21:14; Isa 57:7; Eze 16:15; Isa 1:12“Zamani nilivunja nira yako

na kukatilia mbali vifungo vyako;

ukasema, ‘Sitakutumikia!’

Naam kweli, kwenye kila kilima kirefu

na chini ya kila mti uliotanda matawi yake

ulijilaza kama kahaba.

212:21 Kut 15:17; Za 80:8; Mk 12:1; Isa 5:4Nilikupanda ukiwa mzabibu ulio bora sana,

mkamilifu na wa mbegu nzuri.

Ilikuwaje basi ukawa kinyume nami,

ukaharibika na kuwa mzabibu mwitu?

222:22 Za 51:2; Ay 9:30; Mao 1:8, 17; Yer 17:1Hata ujisafishe kwa magadi

na kutumia sabuni nyingi,

bado doa la hatia yako liko mbele zangu,”

asema Bwana Mwenyezi.

232:23 Yer 23:27; Mwa 3:12-13; Rum 3:19; 2Fal 23:10; Yer 31:22; Mit 30:12; Yer 9:14“Wawezaje kusema, ‘Mimi si najisi,

sijawafuata Mabaali’?

Kumbuka jinsi ulivyotenda kule bondeni;

fikiri uliyoyafanya.

Wewe ni ngamia jike mwenye mbio

ukikimbia hapa na pale,

242:24 Mwa 16:12; Yer 14:6; Ay 39:6punda-mwitu aliyezoea jangwa,

anayenusa upepo katika tamaa yake kubwa:

katika wakati wake wa kuhitaji mbegu

ni nani awezaye kumzuia?

Madume yoyote yanayomfuatilia

hayana haja ya kujichosha;

wakati wa kupandwa kwake watampata tu.

252:25 Isa 57:10; Kum 32:16; Yer 3:13; 14:10Usikimbie hadi miguu yako iwe haina viatu,

na koo lako liwe limekauka.

Lakini ulisema, ‘Haina maana!

Ninaipenda miungu ya kigeni,

nami lazima niifuatie.’

26“Kama vile mwizi aaibikavyo wakati amekamatwa,

hivyo ndivyo nyumba ya Israeli inavyoaibishwa:

wao wenyewe, wafalme wao na maafisa wao,

makuhani wao na manabii wao.

272:27 Yer 32:33; Eze 7:22; Isa 26:16; Yer 10:8; 9:3; 1Fal 14:9; 2Nya 29:9Wanaiambia miti, ‘Wewe ndiwe baba yangu,’

nalo jiwe, ‘Wewe ndiwe uliyenizaa.’

Wamenipa visogo vyao

wala hawakunigeuzia nyuso zao;

lakini wakiwa katika taabu, wanasema,

‘Njoo utuokoe!’

282:28 Isa 45:20; Kum 32:37; 2Fal 17:29; Isa 40:19Iko wapi basi ile miungu mliyojitengenezea?

Yenyewe na ije kama inaweza kuwaokoa

wakati mko katika taabu!

Kwa maana mna miungu mingi

kama mlivyo na miji, ee Yuda.

292:29 Dan 9:11; Mik 3:11; Yer 6:13; Mik 7:2“Kwa nini mnaleta mashtaka dhidi yangu?

Ninyi nyote mmeniasi,”

asema Bwana.

302:30 Neh 9:26; 2Nya 36:16; Mdo 7:52; 1The 2:15; Yer 11:21; Law 26:23“Nimeadhibu watu wako bure tu,

hawakujirekebisha.

Upanga wako umewala manabii wako

kama simba mwenye njaa.

312:31 Isa 45:19; Ay 21:14“Enyi wa kizazi hiki, tafakarini neno la Bwana:

“Je, nimekuwa jangwa kwa Israeli

au nchi ya giza kuu?

Kwa nini watu wangu wanasema, ‘Sisi tuko huru kuzurura,

hatutarudi kwako tena’?

32Je, mwanamwali husahau vito vyake,

au bibi arusi mapambo yake ya arusi?

Lakini watu wangu wamenisahau mimi,

tena kwa siku zisizo na hesabu.

33Je, wewe una ustadi kiasi gani katika kufuatia mapenzi!

Hata wale wanawake wabaya kuliko wote

wanaweza kujifunza kutokana na njia zako.

342:34 Yer 19:4; Mit 6:17; Kut 22:2; 2Fal 21:16Katika nguo zako watu huona

damu ya uhai ya maskini wasio na hatia,

ingawa hukuwakamata wakivunja nyumba.

Lakini katika haya yote

352:35 Mit 28:13; Eze 17:20; 2Sam 12:13; 1Yn 1:8-10; Mit 30:12; Isa 66:16; Yer 25:31unasema, ‘Sina hatia;

Mungu hajanikasirikia.’

Lakini nitakuhukumu kwa sababu unasema,

‘Mimi sijatenda dhambi.’

362:36 Yer 31:22; Hos 5:13; Za 108:12; Isa 30:2-7; Yer 37:7Kwa nini unatangatanga sana,

kubadili njia zako?

Utakatishwa tamaa na Misri

kama ulivyokatishwa na Ashuru.

372:37 2Sam 13:19; Yer 37:7Pia utaondoka mahali hapo

ukiwa umeweka mikono kichwani,

kwa kuwa Bwana amewakataa wale unaowatumainia;

hutasaidiwa nao.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yeremiya 2:1-37

Aisraeli Asiya Mulungu

1Yehova anandiwuza kuti, 2“Pita ukalengeze kwa anthu a ku Yerusalemu kuti Yehova akuti,

“ ‘Ine ndikukumbukira mmene umakhulupirikira pa unyamata wako,

mmene unkandikondera ngati momwe amachitira mkwatibwi,

mmene unkanditsata mʼchipululu muja;

mʼdziko losadzalamo kanthu.

3Israeli anali wopatulika wa Yehova,

anali ngati zipatso zake zoyamba kucha pa nthawi yokolola;

onse amene anamuzunza anapezeka kuti ndi olakwa

ndipo mavuto anawagwera,’ ”

akutero Yehova.

4Imvani mawu a Yehova, inu zidzukulu za Yakobo,

inu mafuko onse a Israeli.

5Yehova akuti,

“Kodi makolo anu anandipeza nʼcholakwa chanji,

kuti andithawe?

Iwo anatsata milungu yachabechabe,

nawonso nʼkusanduka achabechabe.

6Iwo sanafunse nʼkomwe kuti, ‘Kodi Yehova ali kuti,

amene anatitulutsa mʼdziko la Igupto

natitsogolera mʼchipululu mʼdziko lowuma

ndi lokumbikakumbika,

mʼdziko lopanda mvula ndi la mdima,

dziko limene munthu sadutsamo ndipo simukhala munthu aliyense?’

7Ndinakufikitsani ku dziko lachonde

kuti mudye zipatso zake ndi zabwino zake zina.

Koma inu mutafika munaliyipitsa dziko langa

ndi kusandutsa cholowa changa kukhala chonyansa.

8Ansembe nawonso sanafunse kuti,

‘Yehova ali kuti?’

Iwo amene amaphunzitsa malamulo sanandidziwe;

atsogoleri anandiwukira.

Aneneri ankanenera mʼdzina la Baala,

ndi kutsatira mafano achabechabe.

9“Chifukwa chake Ine ndidzakuyimbaninso mlandu,”

akutero Yehova.

“Ndipo ndidzayimbanso mlandu zidzukulu zanu.

10Pitani kumadzulo ku chilumba cha Kitimu, ndipo mukaone,

tumizani anthu ku Kedara kuti akafufuze bwino;

ndipo muona kuti zinthu zoterezi sizinachitikepo nʼkale lomwe:

11Kodi ulipo mtundu wa anthu uliwonse umene unasinthapo milungu yake?

(Ngakhale kuti si milungu nʼkomwe).

Koma anthu anga asinthitsa Mulungu wawo waulemerero

ndi mafano achabechabe.

12Inu mayiko akumwamba, dabwani ndi zimenezi,

ndipo njenjemerani ndi mantha aakulu,”

akutero Yehova.

13“Popeza anthu anga achita machimo awiri:

Andisiya Ine

kasupe wa madzi a moyo,

ndi kukadzikumbira zitsime zawo,

zitsime zongʼaluka, zomwe sizingathe kusunga madzi.

14Israeli si wantchito kapena kapolo wobadwira mʼnyumba, ayi.

Nanga nʼchifukwa chiyani amuwononga chotere?

15Adani ake abangulira

ndi kumuopseza ngati mikango.

Dziko lake analisandutsa bwinja;

mizinda yake anayitentha popanda wokhalamo.

16Ndiponso Aigupto a ku Mefisi ndi a ku Tapanesi

akuphwanyani mitu.

17Zimenezitu zakuchitikirani

chifukwa munasiya Yehova Mulungu wanu

pamene Iye ankakutsogolerani pa njira yanu?

18Tsopano mudzapindula chiyani mukapita ku Igupto,

kukamwa madzi a mu Sihori?

Ndipo mudzapindulanji mukapita ku Asiriya,

kukamwa madzi a mu mtsinje wa Yufurate?

19Kuyipa kwanuko kudzakulangani;

kubwerera mʼmbuyo kwanuko kudzakutsutsani.

Tsono ganizirani bwino,

popeza ndi chinthu choyipa

kundisiya Ine Yehova Mulungu wanu;

ndi chinthu chowawa ndithu kusandiopa Ine Mulungu wanu.

Akutero Ambuye Yehova Wamphamvuzonse.

20“Kuyambira kalekale inu munathyola goli lanu

ndi kudula msinga zanu;

munanena kuti, ‘Sitidzakutumikirani!’

Ndithudi, inu mwakhala ngati mkazi wachiwerewere.

Mukupembedza milungu ina pa phiri lililonse lalitali

ndiponso pansi pa mtengo uliwonse wa masamba ambiri.

21Ine ndinakudzala iwe ngati mtengo wampesa wosankhika;

unali mpesa wabwino kwambiri ndi wodalirika.

Nanga nʼchifukwa chiyani wasanduka mpesa

wachabechabe wonga wa kutchire?

22Ngakhale utasamba ndi soda

kapena kusambira sopo wambiri,

kuthimbirira kwa machimo ako kumaonekabe pamaso panga,”

akutero Ambuye Yehova.

23“Iwe ukunena bwanji kuti, ‘Ine sindinadziyipitse;

sindinatsatire Abaala’?

Takumbukira mmene unkandichimwira mʼchigwa muja;

zindikira bwino zomwe wachita.

Iwe uli ngati ngamira yayikazi yaliwiro

yomangothamanga uku ndi uku,

24wakhala ngati mbidzi yozolowera mʼchipululu,

yonka ninunkhiza pa nthawi yachisika.

Ndani angayiretse chilakolako chakecho?

Mphongo iliyonse yoyikhumba sidzavutika.

Pa nthawi yachisika chakecho mphongoyo idzayipeza.

25Iwe usathamange, nsapato zingakuthere kuphazi

ndi kukhosi kwako kuwuma ndi ludzu.

Koma unati, ‘Zamkutu!

Ine ndimakonda milungu yachilendo,

ndipo ndidzayitsatira.’

26“Monga momwe mbala imachitira manyazi pamene yagwidwa,

moteronso nyumba ya Israeli idzachita manyazi;

Aisraeliwo, mafumu ndi akuluakulu awo,

ansembe ndi aneneri awo.

27Iwo amawuza mtengo kuti, ‘Iwe ndiwe abambo athu,’

ndipo amawuza mwala kuti, ‘Iwe ndiye amene unatibala.’

Iwo andifulatira Ine,

ndipo safuna kundiyangʼana;

Koma akakhala pa mavuto amati,

‘Bwerani mudzatipulumutse!’

28Nanga ili kuti milungu yanu imene munadzipangira nokha?

Ibweretu ngati ingathe kukupulumutsani

pamene muli pamavuto!

Inu anthu a ku Yuda,

milungu yanu ndi yambiri kuchuluka kwake ngati mizinda yanu.

29“Kodi mukundizengeranji mlandu?

Nonse mwandiwukira,”

akutero Yehova.

30“Ine ndinalanga anthu ako popanda phindu;

iwo sanaphunzirepo kanthu.

Monga mkango wolusa,

lupanga lanu lapha aneneri anu.

31“Inu anthu a mʼbado uno, ganizirani bwino mawu a Yehova:

“Kodi Ine ndinakhalapo ngati chipululu kwa Israeli

kapena ngati dziko la mdima wandiweyani?

Chifukwa chiyani anthu anga akunena kuti, ‘Ife tili ndi ufulu omayendayenda;

sitidzabweranso kwa Inu’?

32Kodi namwali amayiwala zokongoletsera zake,

kapena kuyiwala zovala zake za ukwati?

Komatu anthu anga andiyiwala

masiku osawerengeka.

33Mumadziwa bwino njira zopezera zibwenzi!

Choncho ngakhale akazi oyipa omwe mumawaphunzitsa njira zanu.

34Ngakhale pa zovala zako anthu amapezapo

magazi a anthu osauka osalakwa.

Anthuwo simunawapeze akuthyola nyumba.

Komabe ngakhale zinthu zili chomwechi,

35inu mukunena kuti, ‘Ndife osalakwa,

sadzatikwiyira.’

Ndidzakuyimbani mlandu

chifukwa mukunena kuti, ‘Ife sitinachimwe.’

36Chifukwa chiyani

mukunkabe nimusinthasintha njira zanu?

Aigupto adzakukhumudwitsani

monga momwe Asiriya anakuchititsani manyazi.

37Mudzachokanso kumeneko

manja ali kunkhongo.

Popeza Ine Yehova ndawakana anthu amene munkawadalira,

choncho sadzakuthandizani konse.