Mithali 27 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Mithali 27:1-27

127:1 Lk 12:19-20; Yak 4:13; Mt 6:34; 1Fal 20:11Usijisifu kwa ajili ya kesho,

kwa kuwa hujui ni nini kitakachozaliwa kwa siku moja.

227:2 Mit 25:27Mwache mwingine akusifu,

wala si kinywa chako mwenyewe;

mtu mwingine afanye hivyo

na si midomo yako mwenyewe.

327:3 Ay 6:3; Es 1:12Jiwe ni zito na mchanga ni mzigo,

lakini kukasirishwa na mpumbavu ni kuzito kuliko vyote viwili.

427:4 1Yn 3:12Hasira ni ukatili na ghadhabu kali ni gharika,

lakini ni nani awezaye kusimama mbele ya wivu?

527:5 Gal 2:14Afadhali karipio la wazi

kuliko upendo uliofichika.

627:6 Za 141:5; Mit 28:23Majeraha kutoka kwa rafiki yaonyesha uaminifu,

bali kubusu kwa adui ni kwingi sana.

727:7 Ay 6:7Yeye aliyeshiba huchukia kabisa asali,

bali kwa mwenye njaa

hata kile kilicho kichungu

kwake ni kitamu.

827:8 Isa 16:2; Ay 39:14Kama ndege atangatangavyo mbali na kiota chake,

ndivyo alivyo mtu atangatangaye

mbali na nyumbani mwake.

927:9 Es 2:12; Za 45:8Manukato na uvumba huleta furaha moyoni,

nao uzuri wa rafiki huchipuka

kutoka kwenye ushauri wake wa uaminifu.

1027:10 Mit 17:17Usimwache rafiki yako wala rafiki wa baba yako,

tena usiende nyumbani mwa ndugu yako

wakati umepatwa na maafa.

Bora jirani wa karibu

kuliko ndugu aliye mbali.

1127:11 Mit 10:1; 23:15-16; Mwa 24:60Mwanangu, uwe na hekima,

nawe ulete furaha moyoni mwangu,

ndipo nitakapoweza kumjibu yeyote

anitendaye kwa dharau.

1227:12 Mit 22:3Mtu mwenye busara huona hatari na kujificha,

bali mjinga huendelea mbele nayo ikamtesa.

1327:13 Mit 20:16Chukua vazi la yule awekaye dhamana

kwa ajili ya mgeni;

lishikilie iwe dhamana kama anafanya hivyo

kwa ajili ya mwanamke mpotovu.

1427:14 Za 12:2Kama mtu akimbariki jirani yake kwa sauti kuu

asubuhi na mapema,

itahesabiwa kama ni laana.

1527:15 Es 1:18; Mit 19:13Mke mgomvi ni kama

matone yasiyokoma ya siku ya mvua.

16Kumzuia yeye ni kama kuuzuia upepo

au kukamata mafuta kwa kiganja cha mkono.

17Kama vile chuma kinoavyo chuma,

ndivyo mtu amnoavyo mwenzake.

1827:18 1Kor 9:7; Lk 19:12-27; Kum 20:6Yeye autunzaye mtini atakula tunda lake,

naye amtunzaye bwana wake ataheshimiwa.

19Kama uso uonekanavyo kwenye maji,

ndivyo hivyo moyo wa mtu humwonyesha alivyo.

2027:20 Mit 30:15-16; Hab 2:5; Mhu 6:7Kuzimu na Uharibifu havishibi

kadhalika macho ya mwanadamu.

2127:21 Mit 17:3Kalibu ni kwa ajili ya fedha

na tanuru kwa ajili ya dhahabu,

bali mtu hupimwa kwa sifa azipokeazo.

2227:22 Isa 1:5; Yer 5:3; Mit 23:35Hata ukimtwanga mpumbavu kwenye kinu,

ukimtwanga kama nafaka kwa mchi,

hutauondoa upumbavu wake.

2327:23 Mit 12:10; Yer 5:3Hakikisha kuwa unajua hali ya makundi yako

ya kondoo na mbuzi,

angalia kwa bidii ngʼombe zako.

2427:24 Mit 23:5Kwa kuwa utajiri haudumu milele,

nayo taji haidumu vizazi vyote.

2527:25 Za 104:14Wakati majani makavu yameondolewa

na mapya yamechipua,

nayo majani toka milimani yamekusanywa,

26wana-kondoo watakupatia mavazi

na mbuzi thamani ya shamba.

27Utakuwa na maziwa mengi ya mbuzi

kukulisha wewe na jamaa yako,

na kuwalisha watumishi wako wa kike.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Miyambo 27:1-27

1Usamanyadire za mawa,

pakuti sudziwa zimene zidzachitike pa tsikulo.

2Munthu wina akutamande, koma osati wekha;

mlendo akakutamanda, ndiponi koma osati ndi pakamwa pako.

3Mwala ndi wolemera ndipo mchenganso ndi wolemera kwambiri,

koma makani a chitsiru ndi oposa zonsezo kulemera kwake.

4Mkwiyo umadzetsa nkhanza ndipo kupsa mtima kumachititsa zoopsa.

Koma nsanje imachita zoopsa zopambana.

5Kudzudzula munthu poyera nʼkwabwino

kuposa chikondi chobisika.

6Munthu amene amakukonda ngakhale akupweteke zili bwino,

koma mdani wako amakupsompsona mwachinyengo.

7Iye amene wakhuta amayipidwa ndi chisa cha uchi,

koma kwa munthu wanjala ngakhale chimene chili chowawa chimamukomera.

8Munthu amene wasochera ku nyumba kwake,

ali monga mbalame imene yasochera pa chisa chake.

9Mafuta ndi zonunkhira zimasangalatsa mtima,

ndipo kukoma mtima kwa bwenzi kwagona pa malangizo ake.

10Usasiye bwenzi lako ndiponso bwenzi la abambo ako,

ndipo usapite ku nyumba ya mʼbale wako pamene wakumana ndi mavuto;

mnzako wokhala naye pafupi amaposa mʼbale wako wokhala kutali.

11Mwana wanga, khala wanzeru, ndipo ukondweretse mtima wanga;

pamenepo ine ndidzatha kuyankha aliyense amene amandinyoza.

12Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala,

koma munthu wopusa amangopitirira ndipo amakumana ndi mavuto.

13Utenge chovala cha munthu amene waperekera mlendo chikole;

ngati chigwiriro chifukwa waperekera chikole mlendo wosadziwika.

14Ngati munthu apatsa mnzake moni mofuwula mmamawa kwambiri,

anthu adzamuyesa kuti akutemberera.

15Mkazi wolongolola ali ngati

mvula yamvumbi.

16Kumuletsa mkazi wotereyu zimenezi zili ngati kuletsa mphepo

kapena kufumbata mafuta mʼdzanja.

17Chitsulo chimanoledwa ndi chitsulo chinzake,

chomwechonso munthu amanoledwa ndi munthu mnzake.

18Amene amasamalira mtengo wamkuyu adzadya zipatso zake,

ndipo iye amene amasamalira mbuye wake adzalandira ulemu.

19Monga momwe nkhope imaonekera mʼmadzi,

chomwechonso mtima wa munthu umadziwika ndi ntchito zake.

20Manda sakhuta,

nawonso maso a munthu sakhuta.

21Siliva amasungunulira mu uvuni ndipo golide mʼngʼanjo,

chomwechonso munthu amadziwika ndi zomwe akudzitamandira nazo.

22Ngakhale utakonola chitsiru mu mtondo

ndi musi ngati chimanga,

uchitsiru wakewo sudzachoka.

23Uzidziwe bwino nkhosa zako momwe zilili.

Kodi usamalire bwino ziweto zako?

24Paja chuma sichikhala mpaka muyaya,

ndipo ufumu sukhala mpaka mibado yonse.

25Pamene udzu watha, msipu nʼkumera;

ndipo atatuta udzu wa ku mapiri,

26ana ankhosa adzakupatsani chovala

ndipo pogulitsa mbuzi mudzapeza ndalama yogulira munda.

27Mudzakhala ndi mkaka wambuzi wambiri

kuti muzidya inuyo ndi banja lanu

ndi kudyetsa antchito anu aakazi.