Isaya 30 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Isaya 30:1-33

Ole Wa Taifa Kaidi

130:1 Isa 29:15; 8:12; Kum 29:19; 21:18; 2Fal 17:4Bwana asema,

“Ole kwa watoto wakaidi,

kwa wale wanaotimiza mipango ambayo si yangu,

wakifanya makubaliano, lakini si kwa Roho wangu,

wakilundika dhambi juu ya dhambi,

230:2 Mwa 25:22; Hes 27:21; 2Fal 25:26; Isa 36:6; Yer 2:18, 36; 42:14; Eze 17:15; 29:16wale washukao kwenda Misri

bila kutaka shauri langu,

wanaotafuta msaada wa ulinzi wa Farao,

watafutao kivuli cha Misri kwa ajili ya kimbilio.

330:3 Yer 37:5-7; Isa 20:4-5; Amu 9:8-15; Za 44:13Lakini ulinzi wa Farao utakuwa kwa aibu yenu,

kivuli cha Misri kitawaletea fedheha.

430:4 Hes 13:22; Isa 19:11Ingawa wana maafisa katika Soani

na wajumbe wamewasili katika Hanesi,

530:5 Isa 20:5; 36:6; 2Fal 18:21; Za 108:12; Yer 37:3-5; Eze 17:15kila mmoja ataaibishwa

kwa sababu ya taifa lisilowafaa kitu,

ambalo haliwaletei msaada wala faida,

bali aibu tu na fedheha.”

630:6 Kut 1:3; Yer 11:4; Kum 8:15; Hos 8:9; Kut 5:10; Isa 13:1; 5:30; 5:29; Mwa 42:26Neno kuhusu wanyama wa Negebu:

Katika nchi ya taabu na shida,

ya simba za dume na jike,

ya nyoka mwenye sumu kali na nyoka warukao,

wajumbe huchukua utajiri wao juu ya migongo ya punda,

hazina zao juu ya nundu za ngamia,

kwa lile taifa lisilokuwa na faida,

730:7 Yer 2:36; Ay 9:13; 2Fal 18:2kuvipeleka Misri,

ambaye msaada wake haufai kabisa.

Kwa hiyo nimemwita “Rahabu Asiyefanya Chochote.”

830:8 Kut 17:14; Hab 2:2; Kum 27:8; Yer 25:13; Yos 24:26-27; Isa 8:1; Yer 30:2Nenda sasa, liandike neno hili juu ya kibao kwa ajili yao,

liandike kwenye kitabu,

ili liweze kuwa shahidi milele

kwa ajili ya siku zijazo.

930:9 Isa 28:15; Kum 32:20; Isa 59:3-4; Za 78:8; Eze 2:6Hawa ni watu waasi, watoto wadanganyifu,

watoto ambao hawataki kusikiliza mafundisho ya Bwana.

1030:10 Amo 7:13; Yer 11:21; 32:3; 1Sam 9:9; 1Fal 22:8; Yer 4:10; Eze 13:7; Rum 16:18; 2Tim 4:4Wanawaambia waonaji,

“Msione maono tena!”

Nako kwa manabii wanasema,

“Msiendelee kutupatia maono

ambayo ni ya kweli!

Tuambieni mambo ya kupendeza,

tabirini mambo ya uongo.

1130:11 Mdo 13:8; Ay 21:14; Isa 35:8-9; Mit 3:6; Isa 29:19; 48:17Acheni njia hii,

ondokeni katika mapito haya,

nanyi acheni kutukabili pamoja

na yeye Aliye Mtakatifu wa Israeli!”

1230:12 Isa 5:19; 5:24; Za 10:7; 12:5; Isa 5:7, 24Kwa hiyo, hili ndilo asemalo yeye Aliye Mtakatifu wa Israeli:

“Kwa sababu mmekataa ujumbe huu,

mkategemea uonevu na kutumainia udanganyifu,

1330:13 Neh 2:17; Za 80:12; 1Fal 20:30; Isa 17:14; Za 62:3dhambi hii itakuwa kwenu

kama ukuta mrefu,

wenye ufa na wenye kubetuka,

ambao unaanguka ghafula,

mara moja.

1430:14 Za 2:9; 2Pet 2:4-5Utavunjika vipande vipande kama chombo cha udongo

ukipasuka pasipo huruma

ambapo katika vipande vyake

hakuna kipande kitakachopatikana

kwa kuukulia makaa kutoka jikoni

au kuchotea maji kisimani.”

1530:15 Isa 32:17; 2Nya 20:12; Mt 23:37Hili ndilo Bwana Mwenyezi, yeye Aliye Mtakatifu wa Israeli, asemalo:

“Katika kutubu na kupumzika ndio wokovu wenu,

katika kutulia na kutumaini ndizo nguvu zenu,

lakini hamkutaka.

1630:16 Yer 46:6; Kum 17:16; 1Fal 10:28-29Mlisema, ‘Hapana, tutakimbia kwa farasi.’

Kwa hiyo mtakimbia!

Mlisema, ‘Tutakimbia kwa farasi waendao kasi.’

Kwa hiyo wanaowafukuza watakwenda kasi!

1730:17 Kum 28:25; 2Fal 7:7; Law 26:8; Yos 23:10Watu 1,000 watakimbia

kwa ajili ya kitisho cha mtu mmoja,

kwa vitishio vya watu watano

wote mtakimbia,

hadi mtakapoachwa kama mlingoti wa bendera

juu ya kilele cha mlima,

kama bendera juu ya kilima.”

1830:18 Mwa 43:31; 2Pet 3:9, 15; Za 27:14; Mao 3:25; Isa 5:16; 42:14; 48:9; Yon 3:10Hata hivyo Bwana anatamani kutupatia neema,

anainuka ili kuwaonyesha huruma.

Kwa kuwa Bwana ni Mungu wa haki.

Wamebarikiwa wote wanaomngojea yeye!

1930:19 Isa 61:3; Ay 22:27; Mt 7:7-11; Isa 25:8; Ay 24:12; Zek 13:9; Za 86:7; Isa 41:17Enyi watu wa Sayuni, mnaoishi Yerusalemu, hamtalia tena. Tazameni jinsi atakavyokuwa na huruma mtakapolia kwa kumwomba msaada! Mara asikiapo, atawajibu. 2030:20 1Fal 22:27; Za 74:9; Isa 28:9; Amo 8:11Ingawa Bwana huwapa chakula cha shida na maji ya taabu, walimu wenu hawatafichwa tena, kwa macho yenu wenyewe mtawaona. 2130:21 Kum 5:32; Mit 4:27; Isa 29:24; Ay 33:11Mkigeuka kuume au kushoto, masikio yenu yatasikia sauti nyuma yenu ikisema, “Hii ndiyo njia, ifuateni.” 2230:22 Kut 32:4; Isa 2:20; Law 15:19-23; Eze 7:19-20Kisha mtanajisi sanamu zenu zilizofunikwa kwa fedha, na vinyago vyenu vilivyofunikwa kwa dhahabu. Mtazitupilia mbali kama vitambaa vya wakati wa hedhi na kuziambia, “Haya, tokeni hapa!”

2330:23 1Tim 4:8; Za 65:13; Kum 28:12; Isa 65:21-22; Yer 31:14; Ay 36:31Pia atawapa mvua kwa ajili ya mbegu mnazootesha ardhini, chakula kinachotoka ardhini kitakuwa kizuri sana, tena tele. Katika siku ile, ngʼombe wenu watalisha katika shamba pana la majani. 2430:24 Mt 3:12; Lk 3:17; Isa 32:14; Ay 6:5Maksai na punda walimao watakula majani makavu na vyakula vilivyotengenezwa, vinavyotandazwa kwa uma na sepeto. 2530:25 Isa 13:5; Kut 17:6; Isa 32:2; Yoe 3:18Katika siku ile ya mauaji makuu, wakati minara itakapoanguka, vijito vya maji vitatiririka juu ya kila mlima mrefu na kila kilima kilichoinuka sana. 2630:26 Zek 14:7-8; Ufu 21:23; 2Nya 7:14; Hos 14:4; Isa 60:19-20; Yer 3:22; 17:14Mwezi utaangaza kama jua, nao mwanga wa jua utangʼaa mara saba zaidi, kama nuru ya siku saba, wakati Bwana atakapoyafunga majeraha ya watu wake na kuwaponya vidonda alivyowatia.

2730:27 1Fal 18:24; Isa 26:20; 60:14; Eze 22:31; Ay 41:21Tazama, Jina la Bwana linakuja kutoka mbali,

likiwa na hasira kali inayowaka

pamoja na wingu zito la moshi,

midomo yake imejaa ghadhabu

na ulimi wake ni moto ulao.

2830:28 2The 2:8; Amo 9:9; 2Fal 19:28; Isa 37:29; 11:4; 28:15; Za 50:3Pumzi yake ni kama mkondo wa maji yaendayo kasi,

yakipanda hadi shingoni.

Hutikisa mataifa katika chekecheke ya uharibifu,

huweka lijamu katika mataya ya mataifa

ambayo huwaongoza upotevuni.

2930:29 Mt 26:30; Za 42:4; Isa 25:9; 1Sam 10:5; Mwa 49:24Nanyi mtaimba kama usiku ule mnaadhimisha

sikukuu takatifu.

Mioyo yenu itashangilia

kama vile watu wanapokwea na filimbi

kwenye mlima wa Bwana,

kwa Mwamba wa Israeli.

3030:30 Kut 19:18; Za 29:3; Kut 20:18; Isa 47:14; 9:12Bwana atawasababisha watu waisikie sauti yake ya utukufu,

naye atawafanya wauone mkono wake ukishuka

pamoja na hasira yake kali na moto ulao,

kukiwa na tufani ya mvua,

ngurumo za radi na mvua ya mawe.

3130:31 Isa 10:5, 12; 11:4Sauti ya Bwana itaivunjavunja Ashuru,

kwa fimbo yake ya utawala atawapiga.

3230:32 Isa 11:15; 10:26; Eze 32:10; Kut 15:20Kila pigo Bwana atakaloliweka juu yao

kwa fimbo yake ya kuadhibu,

litakuwa kwa wimbo wa matari na vinubi,

anapopigana nao katika vita

kwa mapigo ya mkono wake.

3330:33 2Fal 23:10; Yer 7:31; Mwa 19:24; Ufu 9:17; 2Sam 22:16Tofethi imeandaliwa toka zamani,

imewekwa tayari kwa ajili ya mfalme.

Shimo lake la moto limetengenezwa kwa kina kirefu

na kwa upana mkubwa,

likiwa na moto na kuni tele;

pumzi ya Bwana,

kama kijito cha kiberiti,

huuwasha moto.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesaya 30:1-33

Tsoka kwa Mtundu Wopanduka

1Yehova akuti, “Tsoka kwa ana ondipandukira

amene amachita zowakomera iwo okha osati Ine,

nachita mgwirizano wawowawo

koma osati motsogozedwa ndi Ine.

Choncho amanka nachimwirachimwira.

2Amapita ku Igupto kukapempha thandizo

koma osandifunsa;

amathawira kwa Farao kuti awateteze,

ku Igupto amafuna malo opulumulira.

3Koma chitetezo cha Farao chidzakhala manyazi anu,

malo a mthunzi a ku Igupto mudzachita nawo manyazi.

4Ngakhale kuti nduna zawo zili ku Zowani,

ndipo akazembe awo afika kale ku Hanesi,

5aliyense wa ku Yuda adzachita manyazi

chifukwa cha anthu opanda nawo phindu,

amene sabweretsa thandizo kapena phindu,

koma manyazi ndi mnyozo.”

6Uthenga wonena za nyama za ku Negevi:

Akazembe akuyenda mʼdziko lovuta ndi losautsa,

mʼmene muli mikango yayimuna ndi yayikazi,

mphiri ndi njoka zaululu.

Iwo amasenzetsa abulu ndi ngamira chuma chawo,

kupita nazo kwa mtundu wa anthu

umene sungawathandize.

7Amapita ku Igupto amene thandizo lake ndi lachabechabe.

Nʼchifukwa chake dzikolo ndalitcha

Rahabe chirombo cholobodoka.

8Yehova anandiwuza kuti, “Tsopano pita,

ukalembe zimenezi mʼbuku iwo akuona

ndipo lidzakhala ngati umboni wosatha

masiku a mʼtsogolo.

9Amenewa ndi anthu owukira, onama ndi

osafuna kumvera malangizo a Yehova.

10Iwo amawuza alosi kuti,

‘Musationerenso masomphenya!’

Ndipo amanena kwa mneneri kuti,

‘Musatinenerenso zoona,’

mutiwuze zotikomera,

munenere za mʼmutu mwanu.

11Patukani pa njira ya Yehova,

lekani kutsata njira ya Yehova;

ndipo tisamvenso mawu

a Woyerayo uja wa Israeli!”

12Nʼchifukwa chake Woyerayo wa Israeli akunena kuti,

“Popeza inu mwakana uthenga uwu,

mumakhulupirira zopondereza anzanu

ndipo mumadalira kuchita zoyipa,

13choncho tchimo linalo lidzakhala ngati mingʼalu

pa khoma lalitali ndi lopendama

limene linagwa mwadzidzidzi ndi mwamsangamsanga.

14Lidzaphwanyika ngati mbiya

imene yanyenyekeratu,

mwakuti pakati pake sipadzapezeka phale ngakhale

lopalira moto mʼngʼanjo

kapena lotungira madzi mʼchitsime.”

15Zimene Ambuye Yehova, Woyerayo wa Israeli ananena ndi izi:

“Ngati mubwerera ndi kupuma mudzapulumuka,

ngati mukhala chete ndi kukhulupirira mudzakhala amphamvu,

koma inu munakana zimenezi.

16Inu mukuti, ‘Ayi ife tidzathawa,

tidzakwera pa akavalo aliwiro.’

Zoonadi kuti mudzakwera pa akavalo aliwiro,

koma okuthamangitsani adzakhalanso aliwiro.

17Anthu 1,000 mwa inu adzathawa

poona mdani mmodzi;

poona adani asanu okha

nonsenu mudzathawa.

Otsala anu

adzakhala ngati mbendera pa phiri,

ndi ngati chizindikiro cha pa chulu.”

18Komatu Yehova akufunitsitsa kuti akukomereni mtima,

iye ali wokonzeka kuti akuchitireni chifundo.

Pakuti Yehova ndi Mulungu wachilungamo.

Ndi odala onse amene amakhulupirira Iye!

19Inu anthu a ku Ziyoni, amene mukhala mu Yerusalemu simudzaliranso. Mulungu adzakukomerani mtima pamene adzamva kulira kwanu kopempha thandizo! Ndipo akadzamva, adzakuyankhani. 20Ngakhale Ambuye adzakulowetseni mʼmasautso, aphunzitsi anu sadzakhala kakasi; inu mudzawaona ndi maso anuwo. 21Ngati mudzapatukira kumanja kapena kumanzere, mudzamva mawu kumbuyo kwanu woti, “Njira ndi iyi; yendani mʼmenemo.” 22Pamenepo mudzawononga mafano anu okutidwa ndi siliva ndiponso zifanizo zanu zokutidwa ndi golide; mudzawataya ngati zinthu zonyansa ndipo mudzati, “Zichoke zonsezi!”

23Yehova adzakugwetseraninso mvula pa mbewu zanu zimene mukadzale mʼnthaka, ndipo chakudya chimene mudzakolole chidzakhala chabwino ndi chochuluka. Tsiku limenelo ngʼombe zanu zidzadya msipu wochuluka. 24Ngʼombe ndi abulu amene amalima mʼmunda adzadya chakudya chamchere, chopetedwa ndi foloko ndi fosholo. 25Pa tsiku limene adani anu adzaphedwa ndi nsanja zawo kugwa, mitsinje ya madzi idzayenda pa phiri lililonse lalikulu ndi pa phiri lililonse lalingʼono. 26Mwezi udzawala ngati dzuwa, ndipo kuwala kwa dzuwa kudzawonjezereka kasanu nʼkawiri, ngati kuwala kwa tsiku limodzi. Yehova adzamanga mabala a anthu ake ndi kupoletsa zilonda zimene Iye anachititsa polanga anthu ake.

27Taonani, Yehova akubwera kuchokera kutali,

ndipo mkwiyo wake ndiwonyeka ndi chiweruzo chake chidzakhala chopweteka.

Iye wayankhula mwaukali kwambiri,

ndipo mawu ake ali ngati moto wonyeka.

28Mpweya wake uli ngati mtsinje wosefukira,

wa madzi ofika mʼkhosi.

Iye adzasefa anthu a mitundu ina ndi sefa wosakaza;

Iye akuyika zitsulo mʼkamwa mwa anthu a mitundu ina ngati akavalo,

kuti ziwasocheretse.

29Ndipo inu mudzayimba

mokondwa monga mumachitira usiku pa chikondwerero chopatulika.

Mudzasangalala

ngati anthu oyimba zitoliro

popita ku phiri la Yehova,

thanthwe la Israeli.

30Anthu adzamva liwu la ulemerero la Yehova

ndipo adzaona dzanja lake likutsika pa iwo

ndi mkwiyo woopsa, pamodzi ndi moto wonyeketsa,

mphenzi, namondwe ndi matalala.

31Asiriya adzaopa liwu la Yehova,

ndipo Iye adzawakantha ndi ndodo.

32Yehova akamadzalanga adani ake ndi ndodo,

anthu ake adzakhala akuvina nyimbo

zoyimbira matambolini ndi azeze,

Yehova ndiye ati adzamenyane ndi Asiriyawo.

33Malo otenthera zinthu akonzedwa kale;

anakonzera mfumu ya ku Asiriya.

Dzenje la motolo ndi lozama ndi lalikulu,

ndipo muli nkhuni zambiri;

mpweya wa Yehova,

wangati mtsinje wa sulufule,

udzayatsa motowo pa nkhunizo.