ヨブ 記 17 – JCB & CCL

Japanese Contemporary Bible

ヨブ 記 17:1-16

17

1私の病は重く、死の一歩手前です。

墓は口を開いて私を迎えます。

2あざける者が私を取り巻き、

右を見ても左を見ても、彼らの姿が目につきます。

3-4私の潔白を証明してくれる者は、

どこにもいないのでしょうか。

ああ神よ、だれも私を理解しないよう仕向けたのは、

あなたです。

だから、お願いします。

彼らが勝ち誇らないようにしてください。

5わいろをもらって友人を告発するような者の

子どもたちは、目が衰えて見えなくなる。

6神は私を物笑いの種にした。

人々は私の顔につばを吐く。

7あまりの情けなさに、目は涙にかすむ。

今の私は昔の影にすぎない。

8公正な人がいたら、私を見て驚くだろう。

しかし最後には、潔白な人は不信心な者の先頭に立つ。

9正しい人は躍進を続け、

心のきよい人はいっそう力を増し加える。

10みんな、頼むから帰ってくれないか。

だれも、理解できていないのだ。

11私の古き良き時代は終わった。

希望は失せ、夢は破れた。

12夜を昼、昼を夜だと人は言う。

とんでもない錯覚だ。

13-14死ねば、暗闇の中に入り、

墓をわが父と言い、うじ虫をわが母、わが姉妹と呼ぶ。

15そうなったら、私の望みはどうなるのだ。

だれが、望みを見つけてくれるのか。

16それは、私とともに墓に下る。

ちりの中で共に憩うようになるのだ。」

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 17:1-16

1“Mtima wanga wasweka,

masiku anga atha,

manda akundidikira.

2Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira;

maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.

3“Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna.

Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?

4Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu;

choncho simudzawalola kuti apambane.

5Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma,

ana ake sadzaona mwayi.

6“Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense,

munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.

7Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni;

ndawonda ndi mutu womwe.

8Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi;

anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.

9Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo,

ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.

10“Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo,

sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.

11Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka,

pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.

12Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana,

nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’

13Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda,

ngati ndiyala bedi langa mu mdima,

14ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’

ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’

15tsono chiyembekezo changa chili kuti?

Ndani angaone populumukira panga?

16Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse,

polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.”