Miyambo 21 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Miyambo 21:1-31

1Mtima wa mfumu uli ngati mtsinje wamadzi mʼdzanja la Yehova;

Iye amautsongolera pa chilichonse chimene akufuna.

2Makhalidwe a munthu amaoneka olungama kwa mwini wakeyo,

koma Yehova ndiye amayesa mtima wake.

3Za chilungamo ndi zolondola

ndi zomwe zimakondweretsa Yehova kuposa kupereka nsembe.

4Maso odzikuza ndi mtima wonyada,

zimatsogolera anthu oyipa ngati nyale nʼchifukwa chake amachimwa.

5Zolinga za munthu wakhama zimachulukitsa zinthu zake;

koma aliyense wochita zinthu mofulumira amadzakhala wosauka.

6Chuma chochipeza ndi mawu onyenga ndi chosakhalitsa

ndipo chimakola anthu mu msampha wa imfa.

7Chiwawa cha anthu oyipa chidzawawononga,

pakuti iwo amakana kuchita zolungama.

8Njira ya munthu wolakwa ndi yokhotakhota,

koma makhalidwe a munthu wosalakwa ndi olungama.

9Nʼkwabwino kukhala wekha pa ngodya ya denga la nyumba,

kuposa kukhala mʼnyumba pamodzi ndi mkazi wolongolola.

10Munthu woyipa amalakalaka zoyipa;

sachitira chifundo mnansi wake wovutika.

11Munthu wonyoza akalangidwa, anthu opusa amapeza nzeru;

koma munthu wanzeru akalangizidwa, amapeza chidziwitso.

12Zolingalira za munthu woyipa nʼzosabisika pamaso pa Yehova,

ndipo Iye adzawononga woyipayo.

13Amene atsekera mʼkhutu mwake wosauka akamalira,

nayenso adzalira koma palibe adzamuyankhe.

14Mphatso yoperekedwa mseri imathetsa mkwiyo,

ndipo chiphuphu choperekedwa mobisa chimathetsa mphamvu ya ukali woopsa.

15Chilungamo chikachitika anthu olungama amasangalala,

koma anthu oyipa amaopsedwa nazo.

16Munthu amene amachoka pa njira ya anthu anzeru

adzapezeka mʼgulu la anthu akufa.

17Aliyense wokonda zisangalalo adzasanduka mʼmphawi,

ndipo wokonda vinyo ndi mafuta sadzalemera.

18Anthu oyipa adzakhala chowombolera cha anthu olungama

ndipo osakhulupirika chowombolera anthu olungama mtima.

19Nʼkwabwino kukhala mʼchipululu

kuposa kukhala ndi mkazi wolongolola ndi wopsa mtima msanga.

20Munthu wanzeru samwaza chuma chake,

koma wopusa amachiwononga.

21Amene amatsata chilungamo ndi kukhulupirika,

amapeza moyo ndi ulemerero.

22Munthu wanzeru amagonjetsa mzinda wa anthu amphamvu

ndi kugwetsa linga limene iwo amalidalira.

23Amene amagwira pakamwa pake ndi lilime lake

sapeza mavuto.

24Munthu wonyada ndi wodzikuza amamutcha, “Mnyodoli,”

iye amachita zinthu modzitama kwambiri.

25Chilakolako cha munthu waulesi chidzamupha yekha

chifukwa manja ake amangokhala goba osagwira ntchito.

26Tsiku lonse anthu oyipa amasirira zambiri,

koma anthu olungama amapereka mowolowamanja.

27Nsembe ya anthu oyipa imamunyansa Yehova,

nanji akayipereka ndi cholinga choyipa!

28Mboni yonama idzawonongeka,

koma mawu a munthu wakumva adzakhala nthawi zonse.

29Munthu woyipa amafuna kudzionetsa ngati wolimba mtima,

koma munthu wowongoka amaganizira njira zake.

30Palibe nzeru, palibe kumvetsa bwino, palibenso uphungu,

zimene zingapambane Yehova.

31Kavalo amamukonzera tsiku la nkhondo,

koma ndi Yehova amene amapambanitsa.

Luganda Contemporary Bible

Engero 21:1-31

1Omutima gwa kabaka guli ng’amazzi agakulukutira mu mukono gwa Mukama,

era agukyusiza gy’ayagala yonna.

221:2 Nge 16:2; 24:12; Luk 16:15Buli kkubo lya muntu liba ng’ettuufu mu maaso ge,

naye Mukama apima omutima.

321:3 1Sa 15:22; Nge 15:8; Is 1:11; Kos 6:6; Mi 6:6-8Okukola ebituufu n’eby’amazima

kisanyusa Mukama okusinga ssaddaaka.

421:4 Nge 6:17Amaaso ageegulumiza, n’omutima ogw’amalala,

ye ttabaaza y’ababi, era ebyo kwonoona.

521:5 Nge 10:4; 28:22Enteekateeka z’omunyiikivu zivaamu magoba meereere,

naye okwanguyiriza okutalina nteekateeka kuvaamu bwavu.

621:6 2Pe 2:3Okufuna obugagga n’olulimi olulimba,

mpewo buwewo etwalibwa eruuyi n’eruuyi era mutego gwa kufa.

7Obukambwe bw’ababi bulibamalawo,

kubanga bagaana okukola eby’ensonga.

821:8 Nge 2:15Ekkubo ly’abazza emisango liba kyamu,

naye ery’abataliiko musango liba golokofu.

921:9 Nge 25:24Okusula ku kasolya k’ennyumba,

kisinga okubeera mu nnyumba n’omukazi omuyombi.

10Emmeeme y’omubi yeegomba okukola ebibi;

talaga muliraanwa we kisa n’akatono.

1121:11 Nge 19:25Omukudaazi bw’abonerezebwa, atalina magezi agafuna;

n’ow’amagezi bw’ayigirizibwa afuna okutegeera.

1221:12 Nge 14:11Katonda alaba ebifa mu nnyumba y’omubi,

era abakozi b’ebibi abazikkiririza ddala.

1321:13 Mat 18:30-34; Yak 2:13Oyo aziba amatu ge eri okulaajana kw’omwavu,

naye alikoowoola nga talina amwanukula.

1421:14 Nge 18:16; 19:6Ekirabo ekigabire mu kyama kikakkanya obusungu obungi,

n’enguzi ebikiddwa mu munagiro eggyawo ekiruyi ekingi.

1521:15 Nge 10:29Ensonga bwe zisalibwa mu bwenkanya, lye ssanyu eri abatuukirivu,

naye kiba kyekango eri abakozi b’ebibi.

1621:16 Zab 49:14Omuntu awaba okuva mu kkubo ly’okutegeera,

agukira mu bafu.

1721:17 Nge 23:20-21, 29-35Aganza eby’amasanyu anaabanga mwavu, n’oyo

ayagala omwenge n’amafuta taligaggawala.

1821:18 Nge 11:8; Is 43:3Abakozi b’ebibi batuukibwako emitawaana egyandigudde ku balungi,

n’ekyandituuse ku b’amazima kituuka ku batali beesigwa.

1921:19 nny 9Okubeera mu ddungu,

kisinga okubeera n’omukazi omuyombi anyiiganyiiga.

20Mu nnyumba y’omutuukirivu mubaamu eby’obugagga eby’omuwendo,

naye omusirusiru ebibye byonna abyonoona.

2121:21 Mat 5:6Agoberera obutuukirivu n’ekisa,

alibeera n’obulamu obukulaakulana n’ekitiibwa.

2221:22 Mub 9:15-16Omuntu ow’amagezi alumba ekibuga eky’abazira nnamige,

era n’asesebbula enfo yaabwe gye beesiga.

2321:23 a Yak 3:2 b Nge 12:13; 13:3Afuga akamwa ke n’olulimi lwe,

yeewoonya emitawaana.

2421:24 Zab 1:1; Nge 1:22; Is 16:6; Yer 48:29“Mukudaazi,” lye linnya ly’ab’amalala abeeraga,

abeetwalira mu kwemanya okw’ekitalo mwe batambulira.

2521:25 Nge 13:4Okwetaaga kw’omugayaavu lwe luliba olumbe lwe,

kubanga emikono gye tegyagala kukola.

2621:26 Zab 37:26; Mat 5:42; Bef 4:28Olunaku lwonna aba yeegomba kweyongezaako,

naye omutuukirivu agaba awatali kwebalira.

2721:27 a Is 66:3; Yer 6:20; Am 5:22 b Nge 15:8Ssaddaaka y’omubi ya muzizo,

na ddala bw’agireeta ng’alina ekigendererwa ekitali kirungi.

2821:28 Nge 19:5Omujulizi ow’obulimba alizikirira,

naye ekigambo ky’oyo ayogera eby’amazima kiribeerera emirembe gyonna.

29Omuntu omubi yeekazaakaza,

naye omuntu ow’amazima yeegendereza amakubo ge.

3021:30 a Yer 9:23 b Is 8:10; Bik 5:39Tewali magezi, newaakubadde okutegeera, wadde ebiteeso

ebiyinza okulemesa Mukama.

3121:31 Zab 3:8; 33:12-19; Is 31:1Embalaasi etegekerwa olunaku olw’olutalo,

naye obuwanguzi buva eri Mukama.