BUKU LACHINAYI
Masalimo 90–106
Salimo 90
Pemphero la Mose munthu wa Mulungu.
1Ambuye, mwakhala muli malo athu okhalamo
pa mibado yonse.
2Mapiri asanabadwe,
musanalenge nʼkomwe dziko lapansi ndi dziko lonse,
kuyambira muyaya mpaka muyaya Inu ndinu Mulungu.
3Inu mumabwezera anthu ku fumbi,
mumati, “Bwerera ku fumbi iwe mwana wa munthu.”
4Pakuti zaka 1,000 pamaso panu
zili ngati tsiku limene lapita
kapena ngati kamphindi ka usiku.
5Inu mumasesa anthu mʼtulo ta imfa,
iwo ali ngati udzu watsopano wa mmawa,
6ngakhale kuti mmawa umaphuka watsopano,
pofika madzulo wauma ndi kufota.
7Ife tathedwa ndi mkwiyo wanu;
ndipo taopsezedwa ndi kuyipidwa kwanu.
8Mwayika mphulupulu zathu pamaso panu,
machimo athu obisika poonekera pamaso panu.
9Masiku athu onse amatha ali pansi pa ukali wanu;
timatsiriza zaka zathu ndi kubuwula.
10Kuchuluka kwa masiku athu ndi 70,
kapena 80 ngati tili ndi mphamvu;
komabe zaka zonsezi ndi za mavuto ndi nkhawa,
zimatha mofulumira ndipo ife timawulukira kutali.
11Kodi ndani amadziwa mphamvu ya mkwiyo wanu?
Pakuti ukali wanu ndi waukulu ngati ulemu umene uyenera Inu.
12Tiphunzitseni kuwerenga masiku athu molondola,
kuti tikhale ndi mtima wanzeru.
13Lezani mtima Inu Yehova! Kodi mudzatikwiyira mpaka liti?
Achitireni chifundo atumiki anu.
14Mutikhutitse mmawa ndi chikondi chanu chosatha,
kuti tiyimbe ndi chimwemwe ndi kukhala okondwa masiku athu onse.
15Tisangalatseni masiku ambiri monga masiku amene mwatisautsa,
kwa zaka zambiri monga momwe tinaonera mavuto.
16Ntchito zanu zionetsedwe kwa atumiki anu,
kukongola kwanu kwa ana awo.
17Kukoma mtima kwa Ambuye Mulungu wathu kukhale pa ife;
tikhazikitsireni ntchito ya manja athu;
inde, khazikitsani ntchito ya manja athu.
Moses’ bøn
1En bøn af Guds tjener Moses.
Herre, du er vores tilflugt,
du har hjulpet os fra slægt til slægt.
2Du var til, før bjergene blev skabt,
du levede, før jorden blev dannet.
Din eksistens har ingen begyndelse
og kommer aldrig til en afslutning.
3Men menneskers liv får ende,
på din befaling bliver de til støv.
4Tusinde år er for dig som en enkelt dag er for os,
den varer nogle timer, og så er den forbi.
5Du gør ende på menneskers liv,
og de sover ind.
Om morgenen er græsset grønt og frisk,
6det glinser og er fuldt af liv.
Men om aftenen er det tørret ind
og vissent.
7Vi sygner hen under din fortærende vrede,
vi skælver under din voldsomme harme.
8Du ser vore skjulte synder,
vore fejl ligger udbredt for dine øjne.
9Vi mærker din vrede hver dag,
vi ender vores liv med et suk.
10Vi kan forvente at leve, til vi er halvfjerds,
måske nogle kan nå at blive firs.
Selv vore bedste år har nok af problemer,
men tiden flyver af sted, snart er alt forbi.
11Hvem kender styrken af din vrede?
Din harme fylder os med ærefrygt.
12Hjælp os til at huske, at livet er kort,
så vi kan vokse i visdom.
13Åh, Herre, se i nåde til os!
Hvor længe skal vi lide under din straf?
Vær barmhjertig imod dit eget folk.
14Mæt os hver morgen med din kærlighed,
så vi oplever glæde dag efter dag.
15Vi har været ulykkelige i umindelige tider.
Giv os nu lige så mange lykkelige år.
16Lad dit folk igen opleve dine undere,
lad vore børn få din herlighed at se.
17Vis os din nåde, Herre, vor Gud,
giv os gode tider og fremgang.