Masalimo 91 – CCL & BPH

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 91:1-16

Salimo 91

1Iye amene amakhala mu mthunzi wa Wammwambamwamba

adzapuma mu mthunzi wa Wamphamvuzonse.

2Ndidzanena za Yehova, “Iye ndiye pothawira panga ndi linga langa,

Mulungu wanga amene ndimadalira.”

3Ndithu, Iye adzakupulumutsa ku msampha wa mlenje

ndi ku mliri woopsa;

4Adzakuphimba ndi nthenga zake,

ndipo udzapeza malo othawira mʼmapikomo;

kukhulupirika kwake kudzakhala chishango chako ndi lihawo.

5Sudzachita mantha ndi zoopsa za usiku,

kapena muvi wowuluka masana,

6kapena mliri umene umayenda mu mdima,

kapena zowononga za pa nthawi ya masana.

7Anthu 1,000 atha kufa pambali pako,

anthu 10,000 kudzanja lako lamanja,

koma zoopsazo sizidzafika pafupi ndi iwe.

8Udzapenya ndi maso ako

ndipo udzaona mmene anthu oyipa amalangidwira.

9Pakuti wasankha Wammwambamwamba kukhala malo ako okhalamo;

wavomera Yehova kukhala kothawira kwako.

10Choncho palibe choyipa chimene chidzakugwera,

zoopsa sizidzafika pafupi ndi tenti yako.

11Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe,

kuti akutchinjirize mosamala pa njira zako zonse;

12ndipo adzakunyamula ndi manja awo,

kuti phazi lako lisagunde pa mwala.

13Udzapondaponda mkango ndi njoka,

udzapondereza mkango wamphamvu ndiponso chinjoka.

14“Chifukwa iye amandikonda,” akutero Yehova, “Ndidzamulanditsa;

ndidzamuteteza pakuti wavomereza dzina langa.

15Adzandiyitana, ndipo ndidzamuyankha;

ndidzakhala naye pa mavuto,

ndidzamupulumutsa ndi kumulemekeza.

16Ndidzamupatsa moyo wautali

ndi kumupulumutsa.”

Bibelen på hverdagsdansk

Salmernes Bog 91:1-16

I Herrens varetægt

1De, der søger hjælp hos den Højeste,

bliver beskyttet af den almægtige Gud.

2Jeg siger til Herren: „Du er min tilflugt,

jeg stoler trygt på dig, min Gud.”

3Han bevarer dig fra at gå i fælden,

redder dig fra dødelige sygdomme.

4Han dækker dig med sine fjer,

du er tryg under hans vinger.

Du kan fuldt ud stole på hans hjælp.

5Du skal ikke ligge vågen om natten af frygt,

eller være bange for de pile, der flyver om dagen.

6Du skal ikke ængstes for at blive syg om natten,

eller for at ulykker skal ramme dig ved højlys dag.

7Om så tusinde falder ved siden af dig,

eller ti tusinde bukker under omkring dig,

skal ulykken ikke ramme dig.

8Med dine egne øjne får du at se,

hvordan gudløse mennesker bliver straffet.

9Når du søger tilflugt hos Herren,

og beder den Almægtige beskytte dig,

10skal du ikke rammes af noget ondt,

ingen ulykke skal ødelægge dit hjem.

11For han befaler sine engle at passe på dig,

de skal vogte dig, hvor du end går.

12De skal bære dig på hænder,

så du ikke støder din fod på nogen sten.

13Du kan overvinde både løver og slanger

og sætte din fod på dem som sejrherre.

14Herren siger: „Jeg redder dem, der elsker mig,

beskytter dem, der har tillid til mig.

15Når de kalder, vil jeg svare.

Jeg hjælper dem, når de har problemer,

redder dem og giver dem oprejsning.

16Jeg velsigner dem med et langt liv,

de skal opleve, at jeg frelser dem.”