Masalimo 76 – CCL & BDS

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 76:1-12

Salimo 76

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo la Asafu.

1Mulungu amadziwika mu Yuda;

dzina lake ndi lotchuka mu Israeli.

2Tenti yake ili mu Salemu,

malo ake okhalamo mu Ziyoni.

3Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka,

zishango ndi malupanga, zida zankhondo.

Sela

4Wolemekezeka ndinu,

wamphamvu kuposa mapiri amene ali ndi nyama zambiri.

5Anthu owuma mtima amagona atalandidwa chuma,

Iwowo amagona tulo tawo totsiriza;

palibe mmodzi wamphamvu

amene angatukule manja ake.

6Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo,

kavalo pamodzi ndi galeta zimakhala chete zitagona pansi.

7Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa.

Angathe kuyima pamaso panu ndani mukakwiya?

8Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo,

ndipo dziko linaopa ndi kukhala chete,

9pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze,

kupulumutsa onse osautsidwa mʼdziko.

Sela

10Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando

ndipo opulumuka ku ukali wanu mumawasunga pafupi nanu.

11Chitani malumbiro kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse;

anthu onse omuzungulira abweretse mphatso

kwa Iye amene ayenera kuopedwa.

12Iye amaswa mzimu wa olamulira;

amaopedwa ndi mafumu a dziko lapansi.

La Bible du Semeur

Psaumes 76:1-13

Dieu est vainqueur

1Au chef de chœur. Un psaume d’Asaph76.1 Voir note 50.1. La version grecque ajoute : contre l’Assyrien.. A chanter avec accompagnement d’instruments à cordes.

2Dieu s’est fait connaître en Juda,

son nom est grand en Israël.

3Sa résidence est à Salem76.3 Ancien nom de Jérusalem (Gn 14.18) choisi ici peut-être à cause de son assonance avec shalom, « paix ».,

et sa demeure est en Sion.

4C’est là qu’il a brisé ╵les flèches fulgurantes,

les boucliers, les glaives, ╵toutes armes de guerre.

Pause

5Tu es resplendissant, ╵plus éclatant

que les monts éternels76.5 D’après l’ancienne version grecque. Texte hébreu traditionnel : les montagnes de butin..

6Tous les vaillants guerriers ╵ont été dépouillés,

ils se sont endormis ╵de leur dernier sommeil.

Tous ces valeureux hommes ╵n’ont pas su retrouver ╵la vigueur de leurs mains.

7Dieu de Jacob, à ta menace

les chars et les chevaux ╵se sont figés sur place.

8Que tu es redoutable !

Qui tiendrait devant toi ╵quand ta colère éclate ?

9Du ciel, tu fais entendre ton verdict,

et la terre, effrayée, ╵se tient dans le silence

10quand toi, ô Dieu, tu interviens ╵pour exercer le jugement

et pour apporter le salut ╵à tous les humbles de la terre.

Pause

11Car même la fureur des hommes ╵tournera à ta gloire

et tu t’attacheras ╵les rescapés de ta colère76.11 Hébreu de sens incertain. Autre traduction : et tu te pareras des restes de (leur ?) fureur..

12Vous tous qui entourez ╵l’Eternel votre Dieu,

faites des vœux ╵et accomplissez-les !

Apportez vos présents ╵à ce Dieu redoutable.

13Il brise l’esprit résolu des princes,

il se rend redoutable ╵pour les rois de la terre.