Salimo 121
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Ndikweza maso anga ku mapiri;
kodi thandizo langa limachokera kuti?
2Thandizo langa limachokera kwa Yehova,
wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3Sadzalola kuti phazi lako literereke;
Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4Taonani, Iye amene amasunga Israeli
sadzawodzera kapena kugona.
5Yehova ndiye amene amakusunga;
Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,
kapena mwezi nthawi ya usiku.
7Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;
adzasunga moyo wako.
8Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;
kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Salmo 121
Cántico de los peregrinos.
1A las montañas levanto mis ojos;
¿de dónde ha de venir mi ayuda?
2Mi ayuda proviene del Señor,
que hizo el cielo y la tierra.
3No permitirá que tu pie resbale;
jamás duerme el que te cuida.
4Jamás duerme ni se adormece
el que cuida de Israel.
5El Señor es quien te cuida;
el Señor es tu sombra a tu mano derecha.
6De día el sol no te hará daño
ni la luna de noche.
7El Señor te cuidará;
de todo mal guardará tu vida.
8El Señor cuidará tu salida y tu entrada,
desde ahora y para siempre.