詩篇 26 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

詩篇 26:1-12

第 26 篇

義人的祈求

大衛的詩。

1耶和華啊,求你為我伸冤,

因為我行為純全,

毫不動搖地信靠你。

2耶和華啊,求你察驗我,

試煉我,鑒察我的心思意念。

3因為我銘記你的慈愛,

我行在你的真理中。

4我沒有與詭詐者為伍,

沒有跟虛偽之人同流。

5我憎恨奸惡之輩,

不願與惡人交往。

6耶和華啊,我洗手表明清白,

再走到你的壇前,

7高唱感恩之歌,

述說你的一切奇妙作為。

8耶和華啊,我愛你的殿,

你榮耀充滿的地方。

9別把我的靈魂和罪人同毀,

別把我的性命與嗜血之徒同滅。

10他們滿腹奸計,收受賄賂。

11但我行為純全,

求你施恩拯救我。

12我站在平安之地,

我要在眾人面前讚美耶和華。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 26:1-12

Salimo 26

Salimo la Davide.

1Weruzeni Inu Yehova

pakuti ndakhala moyo wosalakwa.

Ndadalira Yehova

popanda kugwedezeka.

2Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni,

santhulani mtima wanga ndi maganizo anga;

3pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse,

ndipo ndimayenda mʼchoonadi chanu nthawi zonse.

4Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo,

kapena kufunsa nzeru kwa achiphamaso.

5Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa

ndipo ndimakana kukhala pansi pamodzi ndi oyipa.

6Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga

ndi kupita kukatumikira pa guwa lanu la nsembe, Inu Yehova,

7kulengeza mofuwula za matamando anu

ndi kuwuza onse za ntchito zanu zodabwitsa.

8Ndimakonda Nyumba imene Inu Yehova mumakhalamo,

malo amene ulemerero wanu umapezekako.

9Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa,

moyo wanga pamodzi ndi anthu akupha anzawo,

10amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa,

dzanja lawo lamanja ladzaza ndi ziphuphu.

11Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa;

mu msonkhano wa anthu anu ndidzatamanda Yehova.

12Ndayima pa malo wopanda zovuta

ndipo ndidzatamanda Yehova mu msonkhano waukulu.