詩篇 110 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

詩篇 110:1-7

第 110 篇

上帝和祂揀選的王

大衛的詩歌。

1耶和華對我主說:

「你坐在我的右邊,

等我使你的仇敵成為你的腳凳。」

2耶和華必從錫安擴展你的王權,

你必統管你的仇敵。

3你跟仇敵作戰的時候,

你的百姓必甘心跟從,

他們衣著聖潔,

如清晨的甘露。

4耶和華起了誓,永不反悔,

祂說:「你照麥基洗德的模式永遠做祭司。」

5主在你身旁保護你,

祂發怒的時候,必毀滅列王。

6祂要審判列國,

使列國屍橫遍野。

祂要毀滅世上的首領。

7祂要喝路旁的溪水,

祂必精神抖擻。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 110:1-7

Salimo 110

Salimo la Davide.

1Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti,

“Khala ku dzanja langa lamanja

mpaka nditasandutsa adani ako

kukhala chopondapo mapazi ako.”

2Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni;

udzalamulira pakati pa adani ako.

3Ankhondo ako adzakhala odzipereka

pa tsiku lako la nkhondo.

Atavala chiyero chaulemerero,

kuchokera mʼmimba ya mʼbandakucha,

udzalandira mame a unyamata wako.

4Yehova walumbira

ndipo sadzasintha maganizo ake:

“Ndiwe wansembe mpaka muyaya

monga mwa unsembe wa Melikizedeki.”

5Ambuye ali kudzanja lako lamanja;

Iye adzaponda mafumu pa tsiku la ukali wake.

6Adzaweruza anthu a mitundu ina,

adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo ndipo adzaphwanya olamulira a pa dziko lonse lapansi.

7Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira;

choncho adzaweramutsa mutu wake.