Salmernes Bog 120 – BPH & CCL

Bibelen på hverdagsdansk

Salmernes Bog 120:1-7

En landflygtigs bøn

1En valfartssang.

I min nød råbte jeg til Herren,

og han svarede mig.

2„Herre,” bad jeg, „red mig fra de løgnere,

som hele tiden snyder og bedrager!”

3Hvad skal Herren gøre ved bedragerne?

Hvordan skal han straffe dem?

4Jo, med krigerens spidse pile,

som blev skærpet ved de gloende trækul.

5Hvor længe skal jeg leve her i Meshek,

bo som fremmed blandt Kedars telte?

6Alt for længe har jeg været hos et folk, der hader fred.

7Jeg taler fredens sag, men de råber på krig.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 120:1-7

Salimo 120

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga,

ndipo Iye amandiyankha.

2Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza,

ndi kwa anthu achinyengo.

3Kodi adzakuchitani chiyani,

ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?

4Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo,

ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.

5Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki,

kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!

6Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati

pa iwo amene amadana ndi mtendere.

7Ine ndine munthu wamtendere;

koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.