Hosea 2 – ASCB & CCL

Asante Twi Contemporary Bible

Hosea 2:1-23

1“Frɛ wo nuammarimanom ‘Me nkurɔfoɔ’ na frɛ wo nuammaanom ‘Mʼadɔfoɔ.’ ”

Wɔtwe Israel Aso, Gye No To Mu Bio

2“Ka wo maame anim, ka nʼanim,

na ɔnnyɛ me yere

na mennyɛ ne kunu.

Ma ɔnsesa nʼanim a ayɛ adwaman anim no

na ɔnnyae awaresɛeɛ a ɔde ne nufu yɛ no.

3Anyɛ saa a mɛpa ne ho ntoma

na wada adagya te sɛ ɛda a wɔwoo no;

mɛma wayɛ sɛ anweatam,

mɛdane no asase a awo wesee

na mama osukɔm akum no.

4Merennɔ ne mma,

ɛfiri sɛ wɔyɛ adwaman mma.

5Wɔn maame anyɛ ɔnokwafoɔ

na ɔnyinsɛnee wɔn wɔ animguaseɛ mu.

Ɔkaa sɛ, ‘Mɛdi mʼadɔfoɔ akyi,

wɔn a wɔma me aduane ne nsuo,

ne kuntu ne nwera, ngo ne nsã.’

6Yei enti, mede nkasɛɛ bɛsi no ɛkwan;

mɛto ɔfasuo afa no ho, sɛdeɛ ɛbɛyɛ a ɔnhunu ɛkwan.

7Ɔbɛti nʼadɔfoɔ nanso ɔrento wɔn;

ɔbɛhwehwɛ wɔn, nanso ɔrenhunu wɔn.

Afei, ɔbɛka sɛ,

‘Mɛsane akɔ me kunu nkyɛn, te sɛ kane no,

ɛfiri sɛ, saa ɛberɛ no na ɛyɛ ma me sene seesei.’

8Ɔnnkae sɛ me na

memaa no aduane, nsã foforɔ ne ngo,

deɛ ɔmaa sikakɔkɔɔ ne dwetɛ buu no so

ma wɔde kɔsom Baal no.

9“Enti, sɛ mʼaduane no duru twaberɛ a mɛfa mʼadeɛ,

ne me nsã foforɔ no nso saa ara.

Mɛgye me kuntu ne me nwera,

a anka mepɛ sɛ ɔde kata nʼadagya so no.

10Enti afei mɛbɔ no adagya

wɔ nʼadɔfoɔ anim;

obiara rentumi nnye no mfiri me nsam.

11Mɛtwa nʼafahyɛ nyinaa so:

nʼafenhyia afahyɛ, Ɔbosome Foforɔ afahyɛ

Home Ɛda afahyɛ ne nʼafahyɛ ahodoɔ nyinaa.

12Mɛsɛe ne bobe ne borɔdɔma nnua,

deɛ ɔka sɛ nʼadɔfoɔ de tuaa no ka no;

mɛyɛ ne nyinaa nkyɛkyerɛ,

ama wiram mmoa awe.

13Mɛtwe nʼaso wɔ nna a

ɔhyee aduhwam maa Baal no ho;

ɔde nkawa ne agudeɛ hyehyɛɛ ne ho,

tu dii nʼadɔfoɔ akyi,

medeɛ ne werɛ firii me,”

deɛ Awurade seɛ nie.

14“Enti merekɔdaadaa no;

mede no bɛkɔ anweatam so

na makasa bɔkɔɔ akyerɛ no wɔ hɔ.

15Mɛsane de ne bobe mfuo ama no.

Mɛyɛ Akɔr bɔnhwa no,

anidasoɔ ɛkwan.

Ɛhɔ na ɔbɛto dwom sɛdeɛ na ɔyɛ ne mmabunu berɛ mu no

ne ɛberɛ a ɔfirii Misraim no.

16“Saa ɛda no,” sei na Awurade seɛ,

“Wobɛfrɛ me ‘me kunu’;

na woremfrɛ me ‘me wura’ bio.

17Mɛyi Baal ahodoɔ din no afiri nʼano;

na ɔrenkankye wɔ wɔn din mu bio.

18Saa ɛda no, mɛyɛ apam ama wɔn,

wɔne wiram mmoa ne ewiem nnomaa

ne mmoa a wɔwea wɔ asase so.

Tadua, mpea ne ɔko,

mɛbra wɔ asase no so

sɛdeɛ wɔn nyinaa bɛtena ase asomdwoeɛ mu.

19Mɛware wo afebɔɔ;

mɛyi tenenee ne atɛntenenee,

ahummɔborɔ ne ayamhyehyeɛ akyerɛ wo.

20Mɛware wo nokorɛ mu,

ama woahunu Awurade.

21“Saa ɛda no, mɛgye wo so,”

deɛ Awurade seɛ nie.

“Mɛgye ɔsoro so,

na ɔsoro de osuo bɛgye asase so,

22na asase nso bɛgye mfudeɛ so:

bobe foforɔ ne ngo dua,

na wɔn nso agye so sɛ ‘Yesreel’, ‘Onyankopɔn na wadua’.

23Mede Israel bɛdua asase no so ama me ho;

mɛda me dɔ adi akyerɛ deɛ mekaa sɛ ‘wonnyɛ me dɔfo’ no.

Meka akyerɛ wɔn a mesee wɔn sɛ ‘monnyɛ me nkurɔfoɔ’ sɛ

‘moyɛ me nkurɔfoɔ’,

na wɔn nso aka sɛ, ‘Wone me Onyankopɔn.’ ”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Hoseya 2:1-23

1“Nena kwa abale ako kuti, ‘Ndinu anthu anga,’ kwa alongo ako kuti ‘Ndinu okondedwa anga.’ ”

Kulangidwa ndi Kubwezeretsedwa kwa Israeli

2“Dzudzulani amayi anu, adzudzuleni iwo,

pakuti si mkazi wanga,

ndipo ine sindine mwamuna wake.

Iyeyo achotse maonekedwe adama pa nkhope yake,

ndi kusakhulupirika pa mawere ake.

3Akapanda kutero ndidzamuvula,

ndipo adzakhala wamaliseche monga tsiku limene anabadwa;

ndidzamuwumitsa ngati chipululu,

adzakhala ngati dziko lopanda madzi,

ndi kumupha ndi ludzu.

4Sindidzaonetsa chikondi changa pa ana ake,

chifukwa ndi ana a mʼchiwerewere.

5Amayi awo akhala akuchita zachiwerewere

ndipo anawabereka anawo akuchita zinthu zochititsa manyazi.

Iwo anati, ‘Ine ndidzatsatira zibwenzi zanga,

zimene zimandipatsa chakudya ndi madzi,

ubweya ndi thonje, mafuta ndi chakumwa.’

6Choncho njira yake ndidzayitseka ndi minga;

ndidzamuzinga ndi khoma kotero kuti sadzapezanso njira yotulukira.

7Adzathamangira zibwenzi zake koma sadzazipeza;

adzazifunafuna koma sadzazipeza.

Pamenepo iye adzati,

‘Ndibwerera kwa mwamuna wanga woyamba uja,

pakuti ndinali pabwino ndi iyeyo kusiyanitsa ndi pano.’

8Iye sanazindikire kuti ndine amene

ndinkamupatsa tirigu, vinyo watsopano ndi mafuta.

Ndine amene ndinkamukhuthulira siliva ndi golide,

zimene ankapangira mafano a Baala.

9“Choncho Ine ndidzamulanda tirigu wanga pa nthawi yokolola,

ndi vinyo wanga watsopano pa nthawi yopsinya mphesa.

Ndidzamulanda ubweya ndi thonje langa,

zomwe akanaphimba nazo umaliseche wake.

10Motero tsopano ndidzaonetsa maliseche ake

pamaso pa zibwenzi zake;

palibe ndi mmodzi yemwe adzamupulumutse mʼmanja mwanga.

11Ndidzathetsa zikondwerero zake zonse:

zikondwerero zake za chaka ndi chaka, za mwezi watsopano,

za pa masiku a Sabata ndi maphwando ake onse a pa masiku okhazikitsidwa.

12Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa ndi mitengo yake yamkuyu,

imene iye ankanena kuti inali malipiro ake ochokera kwa zibwenzi zake.

Ndidzayisandutsa chithukuluzi,

ndipo zirombo zakuthengo zidzadya zipatsozo.

13Ndidzamulanga chifukwa cha masiku

amene anafukiza lubani kwa Abaala;

anadzikongoletsa povala mphete ndi mikanda yamtengowapatali

ndipo anathamangira zibwenzi zake,

koma Ine anandiyiwala,”

akutero Yehova.

14“Koma tsopano ndidzamukopa mkaziyo;

ndidzapita naye ku chipululu

ndipo ndidzamuyankhula mwachikondi.

15Kumeneko ndidzamubwezera minda yake ya mpesa,

ndipo ndidzasandutsa Chigwa cha Akori kukhala khomo la chiyembekezo.

Kumeneko iye adzayimba nyimbo monga mʼmasiku a ubwana wake,

monga tsiku limene anatuluka ku Igupto.

16“Tsiku limeneli,” Yehova akuti,

“udzandiyitana kuti, ‘Amuna anga;’

sudzandiyitananso kuti, ‘Mbuye wanga.’

17Ndidzachotsa mayina a Abaala pakamwa pake;

sadzatchulanso mayina awo popemphera.

18Tsiku limenelo ndidzachita pangano

ndi zirombo zakuthengo ndi mbalame zamumlengalenga

ndiponso zolengedwa zokwawa pansi kuti ziyanjane ndi anthu anga.

Ndidzachotsa mʼdzikomo uta,

lupanga ndi zida zonse zankhondo,

kuti onse apumule mwamtendere.

19Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya;

ndidzakutomera mwachilungamo, mwaungwiro,

mwachikondi ndi mwachifundo.

20Ndidzakutomera mokhulupirika

ndipo udzadziwa Yehova.

21“Tsiku limenelo Ine ndidzayankha,”

akutero Yehova.

“Ndidzayankha mlengalenga pempho lake lofuna mitambo

ndipo mvula idzagwa pa dziko lapansi;

22ndipo nthaka idzamvera kupempha kwa tirigu,

vinyo ndi mafuta,

ndipo zidzamvera Yezireeli.

23Ndidzadzala Israeli mʼdziko kuti akhale wanga:

ndidzaonetsa chikondi changa kwa anthu amene ndinkawatchula dzina loti, ‘Sakondedwa.’

Ndidzawawuza amene ndinkawatchula dzina loti, ‘Si anthu anga,’ kuti, ‘Ndinu anthu wanga;’

ndipo adzanena kuti, ‘ndinu Mulungu wathu,’ ”