Salmos 67 – OL & CCL

O Livro

Salmos 67:1-7

Salmo 67

Salmo de David. Sobre instrumentos de cordas. Para o diretor do coro.

1Que Deus tenha misericórdia de nós e nos abençoe.

Que a tua luz brilhe sobre nós. (Pausa)

2Que se venha a conhecer o teu caminho

e a tua salvação em toda a Terra.

3Que os povos te louvem!

Que todos os povos te louvem, ó Deus!

4As nações serão felizes e viverão alegres,

quando julgares com verdadeira justiça,

quando fores tu quem as governa. (Pausa)

5Que os povos te louvem!

Que todos os povos te louvem, ó Deus!

6A terra dará abundantes colheitas;

Deus, o nosso Deus, nos abençoará.

7Que Deus nos abençoe

e os povos das terras distantes temerão a Deus!

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 67:1-7

Salimo 67

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

achititse kuti nkhope yake itiwalire.

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo

ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

6Nthaka yabereka zokolola zake;

tidalitseni Mulungu wathu.

7Mulungu atidalitse

kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.