Salmos 43 – NVI-PT & CCL

Nova Versão Internacional

Salmos 43:1-5

Salmo 43

1Faze-me justiça, ó Deus,

e defende a minha causa contra um povo infiel;

livra-me dos homens traidores e perversos.

2Pois tu, ó Deus, és a minha fortaleza.

Por que me rejeitaste?

Por que devo sair vagueando e pranteando,

oprimido pelo inimigo?

3Envia a tua luz e a tua verdade;

elas me guiarão

e me levarão ao teu santo monte,

ao lugar onde habitas.

4Então irei ao altar de Deus,

a Deus, a fonte da minha plena alegria.

Com a harpa te louvarei,

ó Deus, meu Deus!

5Por que você está assim tão triste, ó minha alma?

Por que está assim tão perturbada dentro de mim?

Ponha a sua esperança em Deus!

Pois ainda o louvarei;

ele é o meu Salvador e o meu Deus.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 43:1-5

Salimo 43

1Onetsani kusalakwa kwanga Inu Mulungu;

ndipo mundinenere mlandu wanga kutsutsana ndi mtundu wosapembedza;

mundilanditse mʼmanja mwa achinyengo ndi anthu oyipa.

2Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga.

Nʼchifukwa chiyani mwandikana ine?

Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira,

woponderezedwa ndi mdani?

3Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu

kuti zinditsogolere;

mulole kuti zindifikitse ku phiri lanu loyera,

kumalo kumene inu mumakhala.

4Ndipo ndidzapita ku guwa lansembe la Mulungu,

kwa Mulungu, chimwemwe changa ndi chikondwerero changa.

Ndidzakutamandani ndi zeze,

Inu Mulungu wanga.

5Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni iwe moyo wanga?

Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga?

Khulupirira Mulungu,

pakuti ndidzamutamandabe Iye,

Mpulumutsi wanga ndi Mulungu wanga.