Књига пророка Исаије 20 – NSP & CCL

New Serbian Translation

Књига пророка Исаије 20:1-6

Асирци освајају Азот

1Оне године кад је у Азот дошао Тартан, кога је послао Саргон, цар асирски, и заратио на Азот и заузео га, 2негде у то време рече Господ преко Исаије, сина Амоцова. Рече му: „Иди и скини кострет с бедара и изуј обућу с ногу својих.“ Он је то учинио, те је ходао неодевен и бос.

3Тад је Господ рекао: „Како је слуга мој Исаија три године ходао неодевен и бос, као знак и знамење Египћанима и Кушанима, 4тако ће цар асирски одвести робље из Египта и изгнанике из Куша, младе и старе, неодевене и босе, откривених задњица на срамоту Египту. 5Тада ће се збунити и застидети због Куша, своје узданице, и Египта, поноса својега. 6И говориће у дан онај становници овог приморја: ’Ето, то је узданица наша, камо смо бежали да нам помогне, да нас избави од цара асирског. А како ми да утекнемо?’“

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesaya 20:1-6

Za Chilango cha Igupto ndi Kusi

1Mʼchaka chimene mkulu wankhondo wotumidwa ndi mfumu ya ku Asiriya, anabwera ku Asidodi ndi kuwuthira nkhondo ndi kuwulanda, 2nthawi imeneyo Yehova anawuza Yesaya mwana wa Amozi kuti, “Pita kavule chiguduli ndi nsapato zako.” Ndipo iye anaterodi, ankangoyenda wamaliseche ndiponso wopanda nsapato.

3Kenaka Yehova anati, “Monga momwe mtumiki wanga Yesaya wakhala akuyendera wamaliseche ndiponso wopanda nsapato kwa zaka zitatu ngati chizindikiro ndi chenjezo kwa dziko la Igupto ndi Kusi, 4momwemonso mfumu ya ku Asiriya idzatenga ukapolo anthu a ku Igupto ndi a ku Kusi, anyamata ndi okalamba. Iwo adzakhala amaliseche ndi opanda nsapato, matako ali pa mtunda. Zimenezi zidzachititsa manyazi Igupto. 5Amene ankadalira Kusi, ndiponso amene ankadzitukumula chifukwa cha Igupto adzakhumudwa ndi kuchita manyazi. 6Tsiku limenelo anthu amene amakhala mʼmbali mwa nyanja adzati, ‘Taonani zomwe zawachitikira amene ife tinkawadalira, amene ife tinkathawirako kuti atithandize ndi kutipulumutsa kwa mfumu ya ku Asiriya! Nanga ife tidzapulumuka bwanji?’ ”