Zaburi 92 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 92:1-15

Zaburi 92

Wimbo Wa Kumsifu Mungu

Zaburi. Wimbo wa siku ya Sabato.

192:1 Za 27:6; 147:1; 135:3Ni vyema kumshukuru Bwana

na kuliimbia jina lako, Ee Uliye Juu Sana,

292:2 Za 55:17kuutangaza upendo wako asubuhi,

na uaminifu wako wakati wa usiku,

392:3 Za 71:22; 1Sam 10:5; Neh 12:27; Za 33:2; 81:2kwa zeze yenye nyuzi kumi

na kwa sauti ya kinubi.

492:4 Za 5:11; 27:6; 8:6; 111:7; 143:5Ee Bwana, kwa kuwa matendo yako yamenifurahisha,

nitaziimba kwa shangwe kazi za mikono yako.

592:5 Ay 36:24; Ufu 15:3; Za 40:5; 139:17; Isa 28:29; 31:2; Rum 11:33Ee Bwana, tazama jinsi yalivyo makuu matendo yako,

tazama jinsi yalivyo ya kina mawazo yako!

692:6 Za 73:22Mjinga hafahamu,

mpumbavu haelewi,

792:7 Ay 21:7; Yer 12:1; Mal 3:15; Za 37:1ingawa waovu huchipua kama majani

na wote watendao mabaya wanastawi,

wataangamizwa milele.

8Bali wewe, Ee Bwana,

utatukuzwa milele.

992:9 Za 45:5; 68:1; 89:10Ee Bwana, hakika adui zako,

hakika adui zako wataangamia.

Wote watendao mabaya watatawanyika.

1092:10 Za 89:17; 29:6; 89:10Umeitukuza pembe92:10 Pembe inawakilisha nguvu. yangu kama ile ya nyati dume,

mafuta mazuri yamemiminwa juu yangu.

1192:11 Za 54:7; 91:8Macho yangu yamewaona adui zangu wakishindwa,

masikio yangu yamesikia maangamizi ya adui zangu waovu.

1292:12 Za 72:7; 1:3; 52:8; Yer 17:8; Hos 14:6; Wim 7:7Wenye haki watastawi kama mtende,

watakuwa kama mwerezi wa Lebanoni,

1392:13 Isa 60:21; Mt 15:13; Yn 15:2, 5; Za 135:2waliopandwa katika nyumba ya Bwana,

watastawi katika nyua za Mungu wetu.

1492:14 Za 1:3; Yn 15:2Wakati wa uzee watakuwa bado wanazaa matunda,

watakuwa wabichi tena wamejaa nguvu,

1592:15 Ay 34:10wakitangaza, “Bwana ni mkamilifu;

yeye ni Mwamba wangu,

na ndani yake hamna uovu.”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 92:1-15

Salimo 92

Salimo. Nyimbo ya pa tsiku la Sabata.

1Nʼkwabwino kutamanda Yehova

ndi kuyimbira nyimbo dzina lanu, Inu Wammwambamwamba,

2Kulengeza chikondi chanu mmawa,

ndi kukhulupirika kwanu nthawi ya usiku,

3kuyimbira nyimbo choyimbira cha zingwe khumi

ndi mayimbidwe abwino a zeze.

4Pakuti Inu mumandisangalatsa ndi ntchito zanu, Inu Yehova;

Ine ndikuyimba mwachimwemwe pa ntchito ya manja anu.

5Ndi yayikuludi ntchito yanu Yehova,

maganizo anu ndi ozamadi!

6Munthu wopanda nzeru sadziwa,

zitsiru sizizindikira,

7kuti ngakhale anthu oyipa aphuka ngati udzu

ndipo anthu onse ochita zoyipa apindula,

adzawonongedwa kwamuyaya.

8Koma Inu Yehova, ndinu wokwezedwa kwamuyaya.

9Zoonadi adani anu Yehova,

zoonadi adani anu adzawonongeka;

onse ochita zoyipa adzabalalitsidwa.

10Inu mwakweza nyanga yanga ngati nyanga ya njati;

mafuta abwino akhuthulidwa pamutu wanga.

11Maso anga aona kugonjetsedwa kwa olimbana nane,

makutu anga amva za kugwa kwa amaliwongo anga oyipa.

12Anthu olungama adzaphuka ngati mtengo wa mgwalangwa,

adzakula ngati mkungudza wa ku Lebanoni;

13odzalidwa mʼnyumba ya Yehova,

adzakula bwino mʼmabwalo a Mulungu wathu.

14Iwo adzaberekabe zipatso mu ukalamba wawo,

adzakhala anthete ndi obiriwira,

15kulengeza kuti, “Yehova ndi wolungama;

Iye ndiye Thanthwe langa, ndipo mwa Iye mulibe choyipa.”