Zaburi 36
Uovu Wa Mwanadamu
Kwa mwimbishaji. Zaburi ya Daudi mtumishi wa Bwana.
136:1 Ay 21:16; 23:15; Yer 2:19; 36:16, 24; Rum 3:18; Mit 8:13; Mwa 20:11; Mhu 12:3Kuna neno moyoni mwangu
kuhusu hali ya dhambi ya mwovu.
Hakuna hofu ya Mungu
mbele ya macho yake.
236:2 Kum 29:19Kwa kuwa machoni pake mwenyewe hujisifu mno
hata hawezi kugundua au kuichukia dhambi yake.
336:3 Yer 4:22; 13:23; Za 10:7; 5:6, 9; 43:1; 144:8, 11; 94:8; Ay 5:13; Isa 44:20; Amo 3:10Maneno ya kinywa chake ni maovu na ya udanganyifu,
ameacha kuwa mwenye hekima na kutenda mema.
436:4 Mik 2:1; Rum 12:9; Isa 65:2; Za 52:3Hata kitandani mwake hupanga hila mbaya,
hujitia katika njia ya dhambi
na hakatai lililo baya.
536:5 Za 89:1; 119:90; 108:4; 57:10; 89:2; 71:19; 103:11Upendo wako, Ee Bwana, unafika hadi mbinguni,
uaminifu wako hadi kwenye anga.
636:6 Za 5:8; 68:15; Mwa 1:2; Za 104:14; 7:11; 145:9; Neh 9:6; Rum 11:33; Ay 7:20; 11:8Haki yako ni kama milima mikubwa,
hukumu zako ni kama kilindi kikuu.
Ee Bwana, wewe huwahifadhi
mwanadamu na mnyama.
736:7 Za 6:4; 17:8; 57:1; 91:4; Rut 2:12Upendo wako usiokoma
ni wa thamani mno!
Watu wakuu na wadogo
hujificha uvulini wa mbawa zako.
836:8 Za 65:4; 23:2; 63:5; Yer 31:12, 14; Ufu 22:1; Isa 25:6; Ay 20:17Wanajifurahisha katika wingi nyumbani mwako,
nawe utawanywesha katika mto wa furaha zako.
936:9 Isa 12:3; 2:5; 9:2; 60:1, 19; Yer 2:13; Zek 13:1; Yn 1:4; 4:10, 14; Ufu 21:6; Mdo 26:18; Efe 5:8; Kol 1:13; 1Pet 2:9; Mit 10:11; 16:22; Za 87:7; 4:6; 27:1; 76:4; 104:2Kuwa pamoja nawe ni kijito cha uzima,
katika nuru yako twaona nuru.
1036:10 Yer 31:3; 9:24; 22:16; Za 7:10; 11:2; 94:15; 125:4Dumisha upendo wako kwa wale wanaokujua wewe,
haki yako kwa wale walio wanyofu wa moyo.
1136:11 Za 71:4; 140:4Mguu wa mwenye kiburi usije dhidi yangu,
wala mkono wa mwovu usinifukuze.
1236:12 Za 18:38Angalia jinsi watenda mabaya walivyoanguka:
wametupwa chini, hawawezi kuinuka!
Salimo 36
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide, mtumiki wa Yehova.
1Uthenga uli mu mtima mwanga
wonena za kuchimwa kwa munthu woyipa:
Mu mtima mwake
mulibe kuopa Mulungu.
2Pakuti iye mʼkuona kwake amadzinyenga yekha kwambiri,
sazindikira kapena kudana ndi tchimo lake.
3Mawu a pakamwa pake ndi oyipa ndi achinyengo;
iyeyo waleka kukhala wanzeru ndi kuchita zabwino.
4Ngakhale ali pa bedi pake amakonzekera zoyipa;
iye amadzipereka yekha ku njira ya uchimo
ndipo sakana cholakwa chilichonse.
5Chikondi chanu Yehova, chimafika ku mayiko a kumwamba,
kukhulupirika kwanu mpaka ku mitambo.
6Chilungamo chanu Mulungu chili ngati mapiri aakulu,
chiweruzo chanu chili ngati kuzama kwakukulu.
Yehova mumasunga munthu pamodzi ndi chinyama.
7Chikondi chanu chosatha ndi chamtengowapatali!
Otchuka pamodzi ndi anthu wamba pakati pa anthu
amapeza pothawirapo mu mthunzi wa mapiko anu.
8Iwo amadyerera zinthu zambiri za mʼnyumba yanu;
Inu mumawapatsa chakumwa kuchokera mu mtsinje wanu wachikondwerero.
9Pakuti kwa Inu kuli kasupe wamoyo;
mʼkuwala kwanu ifenso timaona kuwala.
10Pitirizani chikondi chanu pa iwo amene amakudziwani,
chilungamo chanu kwa olungama mtima.
11Musalole kuti phazi la wodzikuza libwere kulimbana nane,
kapena dzanja la oyipa kundithamangitsa.
12Onani momwe ochita zoyipa agonera atagwa,
aponyeni pansi, kuti asathe kudzukanso!