Zaburi 125
Usalama Wa Watu Wa Mungu
Wimbo wa kwenda juu.
1125:1 Za 46:5; 48:2-5; 48:12; Isa 33:20Wale wamtumainio Bwana ni kama mlima Sayuni,
ambao hauwezi kutikisika, bali wadumu milele.
2125:2 1Nya 21:15; Za 32:10; Zek 2:4-5Kama milima inavyozunguka Yerusalemu,
ndivyo Bwana anavyowazunguka watu wake
sasa na hata milele.
3125:3 Es 4:11; Za 89:22; Mit 22:8; Isa 13:11; 14:5; 24:10Fimbo ya waovu haitadumu juu ya nchi
waliopewa wenye haki,
ili wenye haki wasije wakatumia
mikono yao kutenda ubaya.
4125:4 Za 119:65; 36:10Ee Bwana, watendee mema walio wema,
wale walio wanyofu wa moyo.
5125:5 Ay 23:11; Isa 59:8; Za 92:7; 128:6; Mit 2:15; 17:6; Gal 6:16Bali wale wanaogeukia njia zilizopotoka,
Bwana atawafukuza pamoja na watenda mabaya.
Amani iwe juu ya Israeli.
Salimo 125
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,
limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,
momwemonso Yehova azungulira anthu ake
kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala
pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama,
kuti anthu olungamawo
angachite nawonso zoyipa.
4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,
amene ndi olungama mtima
5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,
Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa.
Mtendere ukhale pa Israeli.