Zaburi 125 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 125:1-5

Zaburi 125

Usalama Wa Watu Wa Mungu

Wimbo wa kwenda juu.

1125:1 Za 46:5; 48:2-5; 48:12; Isa 33:20Wale wamtumainio Bwana ni kama mlima Sayuni,

ambao hauwezi kutikisika, bali wadumu milele.

2125:2 1Nya 21:15; Za 32:10; Zek 2:4-5Kama milima inavyozunguka Yerusalemu,

ndivyo Bwana anavyowazunguka watu wake

sasa na hata milele.

3125:3 Es 4:11; Za 89:22; Mit 22:8; Isa 13:11; 14:5; 24:10Fimbo ya waovu haitadumu juu ya nchi

waliopewa wenye haki,

ili wenye haki wasije wakatumia

mikono yao kutenda ubaya.

4125:4 Za 119:65; 36:10Ee Bwana, watendee mema walio wema,

wale walio wanyofu wa moyo.

5125:5 Ay 23:11; Isa 59:8; Za 92:7; 128:6; Mit 2:15; 17:6; Gal 6:16Bali wale wanaogeukia njia zilizopotoka,

Bwana atawafukuza pamoja na watenda mabaya.

Amani iwe juu ya Israeli.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 125:1-5

Salimo 125

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,

limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.

2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,

momwemonso Yehova azungulira anthu ake

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala

pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama,

kuti anthu olungamawo

angachite nawonso zoyipa.

4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,

amene ndi olungama mtima

5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,

Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa.

Mtendere ukhale pa Israeli.