Zaburi 117 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 117:1-2

Zaburi 117

Sifa Za Bwana

1117:1 Za 22:23; 103:2; Rum 15:11Msifuni Bwana, enyi mataifa yote;

mtukuzeni yeye, enyi watu wote.

2117:2 Za 17:7; 103:11; 119:90; 146:6Kwa kuwa upendo wake kwetu ni mkuu,

uaminifu wa Bwana unadumu milele.

Msifuni Bwana.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 117:1-2

Salimo 117

1Tamandani Yehova, inu anthu a mitundu yonse;

mulemekezeni Iye, inu mitundu ya anthu.

2Pakuti chikondi chake pa ife ndi chachikulu,

ndipo kukhulupirika kwa Yehova nʼkosatha.

Tamandani Yehova.