Zaburi 110 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 110:1-7

Zaburi 110

Bwana Na Mfalme Wake Mteule

Zaburi ya Daudi.

1110:1 Mt 22:44; Lk 20:42; Mdo 2:34; Mk 12:36; 16:19; Ebr 1:13; 12:2; Yos 10:24; 1Fal 5:3; 1Kor 15:25; Za 45:6Bwana amwambia Bwana wangu:

“Keti mkono wangu wa kuume,

mpaka nitakapowafanya adui zako

kuwa mahali pa kuweka miguu yako.”

2110:2 Mwa 49:10; Za 45:6; 2:6; 72:8; Isa 14:5; Yer 48:17Bwana ataeneza fimbo yako ya utawala yenye nguvu kutoka Sayuni;

utatawala katikati ya adui zako.

3110:3 Kut 15:11; Mik 5:7Askari wako watajitolea kwa hiari

katika siku yako ya vita.

Ukiwa umevikwa fahari takatifu,

kutoka tumbo la mapambazuko

utapokea umande wa ujana wako.110:3 Au: vijana wako watakujia kama umande.

4110:4 Hes 23:19; Zek 6:13; Ebr 5:6; 5:10; 7:15-17; 7:21; Mwa 14:18Bwana ameapa,

naye hatabadilisha mawazo yake:

“Wewe ni kuhani milele,

kwa mfano wa Melkizedeki.”

5110:5 Za 16:8; 2:12; 68:21; 76:12; Kum 7:24; Isa 60:12; Dan 2:44; Za 2:5; Rum 2:5; Ufu 6:17; 11:18Bwana yuko mkono wako wa kuume,

atawaponda wafalme siku ya ghadhabu yake.

6110:6 Za 9:19; 18:38; Isa 5:25; 34:3; 66:24Atawahukumu mataifa, akilundika mizoga

na kuwaponda watawala wa dunia nzima.

7110:7 Za 3:3; 27:6Atakunywa maji katika kijito kando ya njia,110:7 Au: Yeye atoaye mtu wa kurithi mwingine atamweka kwenye mamlaka.

kwa hiyo atainua kichwa chake juu.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 110:1-7

Salimo 110

Salimo la Davide.

1Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti,

“Khala ku dzanja langa lamanja

mpaka nditasandutsa adani ako

kukhala chopondapo mapazi ako.”

2Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni;

udzalamulira pakati pa adani ako.

3Ankhondo ako adzakhala odzipereka

pa tsiku lako la nkhondo.

Atavala chiyero chaulemerero,

kuchokera mʼmimba ya mʼbandakucha,

udzalandira mame a unyamata wako.

4Yehova walumbira

ndipo sadzasintha maganizo ake:

“Ndiwe wansembe mpaka muyaya

monga mwa unsembe wa Melikizedeki.”

5Ambuye ali kudzanja lako lamanja;

Iye adzaponda mafumu pa tsiku la ukali wake.

6Adzaweruza anthu a mitundu ina,

adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo ndipo adzaphwanya olamulira a pa dziko lonse lapansi.

7Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira;

choncho adzaweramutsa mutu wake.