Zaburi 101 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 101:1-8

Zaburi 101

Ahadi Ya Kuishi Kwa Uadilifu Na Kwa Haki

Zaburi ya Daudi.

1101:1 Za 33:1; 51:14; 89:1; 145:7Nitaimba juu ya upendo wako na haki yako;

kwako wewe, Ee Bwana, nitaimba sifa.

2101:2 Mwa 17:1; 18:10; 1Sam 18:14; Kum 6:7; Flp 1:10; 1Fal 9:4; 3:14Nitazingatia kuishi maisha yasiyo na lawama:

utakuja kwangu lini?

Nitatembea nyumbani mwangu

kwa moyo usio na lawama.

3101:3 Yos 23:6; 1Sam 12:20; Yer 16:18; Eze 11:21; Hos 9:10; Za 5:5Sitaweka mbele ya macho yangu

kitu kiovu.

Ninayachukia matendo ya watu wasio na imani;

hawatashikamana nami.

4101:4 Mit 3:32; 6:16-19; 11:20; Mt 7:23; 1Kor 5:11; 2Tim 2:19Moyo wa ukaidi utakuwa mbali nami;

nitajitenga na kila ubaya.

5101:5 Kut 20:16; Law 19:16; Za 10:5; Mit 6:17; Lk 18:14Kila amsingiziaye jirani yake kwa siri,

huyo nitamnyamazisha;

mwenye macho ya dharau na moyo wa kiburi

huyo sitamvumilia.

6101:6 Za 101:2; 119:1Macho yangu yatawaelekea waaminifu katika nchi,

ili waweze kuishi pamoja nami;

yeye ambaye moyo wake hauna lawama

atanitumikia.

7Mdanganyifu hatakaa

nyumbani mwangu,

yeye asemaye kwa uongo

hatasimama mbele yangu.

8101:8 Za 5:3; 75:10; 118:10-12; 46:4; Yos 21:12; 2Sam 3:39; Hos 9:2Kila asubuhi nitawanyamazisha

waovu wote katika nchi;

nitamkatilia mbali kila mtenda mabaya

kutoka mji wa Bwana.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 101:1-8

Salimo 101

Salimo la Davide.

1Ndidzayimba za chikondi ndi chiweruzo chanu cholungama;

kwa Inu Yehova ndidzayimba matamando.

2Ndidzatsata njira yolungama;

nanga mudzabwera liti kwa ine?

Ndidzayenda mʼnyumba mwanga

ndi mtima wosalakwa.

3Sindidzayika chinthu chilichonse choyipa

pamaso panga.

Ine ndimadana ndi zochita za anthu opanda chikhulupiriro;

iwo sadzadziphatika kwa ine.

4Anthu a mtima wokhota adzakhala kutali ndi ine;

ine sindidzalola choyipa chilichonse kulowa mwa ine.

5Aliyense wosinjirira mnansi wake mseri

ameneyo ndidzamuletsa;

aliyense amene ali ndi maso amwano ndi mtima wodzikuza,

ameneyo sindidzamulekerera.

6Maso anga adzakhala pa okhulupirika mʼdziko,

kuti akhale pamodzi ndi ine;

iye amene mayendedwe ake ndi wosalakwa

adzanditumikira.

7Aliyense wochita chinyengo

sadzakhala mʼnyumba mwanga.

Aliyense woyankhula mwachinyengo

sadzayima pamaso panga.

8Mmawa uliwonse ndidzatontholetsa anthu

onse oyipa mʼdziko;

ndidzachotsa aliyense wochita zoyipa

mu mzinda wa Yehova.