Ayubu 39 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Ayubu 39:1-30

139:1 Kum 14:5“Je, wajua ni wakati gani mbuzi wa mlimani wanapozaa?

Je, watambua ni wakati gani kulungu jike azaapo mtoto wake?

239:2 Mwa 31:7-9Je, waweza kuhesabu miezi hadi wazaapo?

Je, unajua majira yao ya kuzaa?

3Wao hujiinamisha na kuzaa watoto wao;

utungu wa kuzaa unakoma.

4Watoto wao hustawi na kuongezeka nguvu nyikani;

huenda zao wala hawarudi tena.

539:5 Mwa 16:12; Ay 6:5“Ni nani aliyemwachia punda-mwitu awe huru?

Ni nani aliyezifungua kamba zake?

639:6 Za 107:34; Yer 2:24; 14:6; Hos 8:9Nimempa nchi isiyokaliwa na watu kuwa masikani yake,

nchi ya chumvi kuwa makao yake.

739:7 Ay 5:22; 3:18Huzicheka ghasia za mji,

wala hasikii kelele za mwendesha gari.

839:8 Isa 32:20Huzunguka vilimani kwa ajili ya malisho

na kutafuta kila kitu kibichi.

939:9 Hes 23:22; Kum 33:17“Je, nyati atakubali kukutumikia?

Atakaa karibu na hori lako usiku?

1039:10 Ay 41:13; Za 32:9Je, waweza kumfungia kwenye matuta kwa kamba?

Je, atalima mabonde nyuma yako?

1139:11 Ay 40:16; 41:12, 22; Za 147:10Je, utamtumainia kwa ajili ya nguvu zake nyingi?

Utamwachia yeye kazi zako nzito?

12Utaweza kumwamini akuletee nafaka yako nyumbani

kutoka shambani na kuikusanya kwenye sakafu yako ya kupuria?

1339:13 Zek 5:9“Mbuni hupigapiga mabawa yake kwa furaha,

lakini hayawezi kulinganishwa

na mabawa na manyoya ya korongo.

14Huyataga mayai yake juu ya ardhi,

na kuyaacha yapate joto mchangani,

1539:15 2Fal 14:9bila kujali kuwa mguu waweza kuyaponda,

kwamba baadhi ya wanyama wa porini wanaweza kuyakanyaga.

1639:16 Ay 39:17; Mao 4:3Yeye huyafanyia makinda yake ukatili kama vile si yake;

hajali kwamba taabu yake inaweza ikawa bure,

1739:17 Ay 21:22; 39:16kwa kuwa Mungu hakumjalia hekima,

wala hakumpa fungu la akili njema.

1839:18 Ay 5:22Lakini akunjuapo mabawa yake kukimbia,

humcheka farasi pamoja na yeye aliyempanda.

1939:19 Ay 39:11“Je, wewe humpa farasi nguvu

au kuivika shingo yake manyoya marefu?

2039:20 Yoe 2:4-5; Ufu 9:7; Yer 8:16Je, wewe humfanya farasi aruke kama nzige,

akistaajabisha kwa tishio la mlio wake wa majivuno?

2139:21 Yer 8:6Huparapara bila woga, akizifurahia nguvu zake,

husonga mbele kukabiliana na silaha.

2239:22 Ay 5:22Huicheka hofu, haogopi chochote,

wala haukimbii upanga.

2339:23 Isa 5:28; Yer 5:16; Nah 3:3Podo hutoa sauti kando yake,

pamoja na mkuki unaongʼaa na fumo.

2439:24 Hes 10:9; Eze 7:14Bila woga na kwa ghadhabu huimeza nchi,

wala tarumbeta iliapo yeye hawezi kusimama.

2539:25 Yos 6:5; Yer 8:6; Amo 2:2Asikiapo sauti ya baragumu yeye hulia, ‘Aha!’

Hunusa harufu ya vita toka mbali,

sauti ya mtoa amri na ukelele wa vita.

26“Je, mwewe huruka kwa hekima yako

na kuyakunjua mabawa yake kuelekea kusini?

27Je, tai hupaa juu kwa amri yako

na kujenga kiota chake mahali pa juu?

28Huishi juu ya miamba mirefu na kukaa huko usiku;

majabali yenye ncha kali ndiyo ngome yake.

29Kutoka huko hutafuta chakula chake;

macho yake hukiona kutoka mbali.

3039:30 Mt 24:28; Lk 17:37Makinda yake hujilisha damu,

na pale palipo na machinjo, ndipo yeye alipo.”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 39:1-30

1“Kodi iwe umadziwa nthawi imene mbalale yayikazi imaswera?

Kodi umaonerera pamene nswala ikubala?

2Kodi umawerenga miyezi imene zimakhala ndi bere?

Kodi nthawi imene zimaswana iwe umayidziwa?

3Zimakhala tsonga ndi kuswa ana awo;

pamenepo ululu wobereka nʼkutha.

4Ana a nyamazi amakhala ndi mphamvu ndipo amakulira mʼthengo;

kenaka amachoka ndipo sabwereranso.

5“Kodi bulu wakuthengo amamupatsa ndani ufulu wongodziyendera?

Ndani amamasula zingwe zake?

6Ine ndinamupatsa chipululu kuti chikhale mudzi wake,

nthaka ya mchere kuti ikhale malo ake okhalamo

7Iye amakhala kutali ndi phokoso la mu mzinda;

ndipo samva kufuwula kwa oyendetsa nyama zakatundu.

8Amayendayenda mʼmapiri kudya msipu

ndipo amafunafuna msipu uliwonse wobiriwira.

9“Kodi njati ingavomere kukutumikira?

Kodi ingagone mu gome lako usiku?

10Kodi ungathe kuyimanga ndi zingwe kuti izilima?

Kodi ingasalaze nthumbira mʼmunda mwako?

11Kodi ungadalire njatiyo chifukwa champhamvu zake?

Kodi ungayilekere kuti igwire ntchito zako zolemetsa?

12Kodi ungadalire kuti idzakubweretsera tirigu wako

ndi kumuyika ku malo opunthira?

13“Nthiwatiwa imakupiza mapiko ake monyadira,

koma mapikowo sangafanane ndi mapiko ndi nthenga za kakowa.

14Nthiwatiwa imakwirira mazira ake pansi

ndipo amafundidwa ndi nthaka,

15nthiwatiwayo sidera nkhawa kuti mazira ake angathe kuswanyidwa,

ndi kuti nyama zakuthengo zitha kuwaponda.

16Nthiwatiwa imachitira nkhanza ana ake ngati anawo si ake;

Imayiwala zoti inavutika powabala.

17Chifukwa Mulungu anayimana nzeru,

simvetsa kanthu kalikonse.

18Komatu nthiwatiwa ikadzambatuka ndi kuyamba kuthamanga,

imamusiya kutali kavalo ndi wokwerapo wake.

19“Kodi ndiwe amene umamupatsa mphamvu kavalo

kapena kumuveka chenjerere mʼkhosi mwake?

20Kodi ndiwe amene umalipatsa dzombe ulemerero wolumphira,

ukali wake nʼkumachititsa mantha?

21Iye amalumphalumpha moopseza, kukondwerera mphamvu zake,

ndipo amapita ku nkhondo ndi mphamvu zake zonse.

22Iye sachita mantha, saopa chilichonse;

sabwerera mʼmbuyo akaona lupanga.

23Zida zankhondo zimachita kwichikwichi mʼchimake pambali pake

pamodzi ndi mkondo wonyezimira ndi nthungo.

24Kavaloyo amanjenjemera ndi ukali ndi kulumphalumpha;

satha kungoyima pamene wamva kulira kwa lipenga.

25Lipenga likalira amati, ‘Twee!’

Amamva fungo la nkhondo ali patali,

kufuwula kwa anthu olamulira nkhondo ndi mfuwu wankhondo.

26“Kodi kabawi amawuluka ndi nzeru zako,

ndi kutambasula mapiko ake kupita kummwera?

27Kodi umalamulira chiwombankhanga ndiwe kuti chiziwuluka

ndi kumanga chisa chake pamwamba penipeni?

28Chimakhala pa phiri ndipo chimakhala pamenepo usiku;

chimakhala pa msonga penipeni pa mwala.

29Chili pamenepo chimayangʼanayangʼana choti chigwire kuti chidye;

maso ake amachionera patali chinthucho.

30Ana ake amayamwa magazi,

ndipo kumene kuli mitembo ndiko chimapezeka.”