1 ዜና መዋዕል 24 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

1 ዜና መዋዕል 24:1-31

የካህናት አመዳደብ

1የአሮን ልጆች አመዳደብ እንደሚከተለው ነበረ፤

የአሮን ልጆች ናዳብ፣ አብዩድ፣ አልዓዛር፣ ኢታምር ነበሩ። 2ናዳብና አብዩድ ግን ዘር ሳይተኩ ከአባታቸው በፊት ሞቱ፤ ስለዚህ አልዓዛርና ኢታምር ካህናት ሆነው ያገለግሉ ነበር። 3ዳዊትም የአልዓዛር ዘር የሆነው ሳዶቅና የኢታምር ዘር የሆነው አቢሜሌክ እየረዱት እንደየአገልግሎታቸው ሥርዐት እየለየ መደባቸው። 4ከኢታምር ይልቅ በአልዓዛር ዘሮች መካከል ብዙ መሪዎች ተገኙ፤ አከፋፈላቸውም እንደሚከተለው ነበር፤ ከአልዓዛር ዘሮች ዐሥራ ስድስት የቤተ ሰብ አለቆች፤ ከኢታምርም ዘሮች ስምንት የቤተ ሰብ አለቆች። 5ከአልዓዛርና ከኢታምር ዘሮች መካከል የመቅደሱ ሹማምትና የእግዚአብሔር ሹማምት ስለ ነበሩ፣ ያለ አድልዎ በዕጣ ለዩአቸው።

6የሌዋዊው የናትናኤል ልጅ ጸሓፊው ሸማያ በንጉሡና በሹማምቱ፣ በካህኑ በሳዶቅ፣ በአብያታር ልጅ በአቤሜሌክ እንዲሁም በካህናቱና በሌዋውያኑ ቤተ ሰብ አለቆች ፊት ስማቸውን ጻፈ፤ የጻፈውም አንዱን ቤተ ሰብ ከአልዓዛር ሌላውን ደግሞ ከኢታምር በመውሰድ ነው፤

7የመጀመሪያው ዕጣ ለዮአሪብ፣

ሁለተኛውም ዕጣ ለዮዳሄ ወጣ፤

8ሦስተኛው ለካሪም፣

አራተኛው ለሥዖሪም፣

9አምስተኛው ለመልክያ፣

ስድስተኛው ለሚያሚን፣

10ሰባተኛው ለአቆስ፣

ስምንተኛው ለአብያ፣

11ዘጠነኛው ለኢያሱ፣

ዐሥረኛው ለሴኬንያ፣

12ዐሥራ አንደኛው ለኤሊያሴብ፣

ዐሥራ ሁለተኛው ለያቂም፣

13ዐሥራ ሦስተኛው ለኦፖ፣

ዐሥራ አራተኛው ለየሼብአብ፣

14ዐሥራ አምስተኛው ለቢልጋ፣

ዐሥራ ስድስተኛው ለኢሜር፣

15ዐሥራ ሰባተኛው ለኤዚር፣

ዐሥራ ስምንተኛው ለሃፊጼጽ፣

16ዐሥራ ዘጠነኛው ለፈታያ፣

ሃያኛው ለኤዜቄል፣

17ሃያ አንደኛው ለያኪን፣

ሃያ ሁለተኛው ለጋሙል፣

18ሃያ ሦስተኛው ለድላያ፣

ሃያ አራተኛ ለመዓዝያ ወጣ።

19የእስራኤል አምላክ እግዚአብሔር ባዘዘውና ከቀድሞ አባታቸው ከአሮን በተሰጣቸው መመሪያ መሠረት ወደ እግዚአብሔር ቤተ መቅደስ በሚገቡበት ጊዜ፣ የተወሰነላቸው ሥርዐት ይህ ነበር።

የተቀሩት ሌዋውያን

20ከቀሩት የሌዊ ዘሮች ደግሞ፦

ከእንበረም ወንዶች ልጆች፣ ሱባኤል፤

ከሱባኤል ወንዶች ልጆች፣ ዬሕድያ።

21ከረዓብያ ወንዶች ልጆች፤

አለቃው ይሺያ።

22ከይስዓራውያን ወገን፣ ሰሎሚት፤

ከሰሎሚት ወንዶች ልጆች፣ ያሐት።

23የኬብሮን ወንዶች ልጆች፣ የመጀመሪያው ይሪያ24፥23 ሁለት የዕብራይስጥ ቅጆችና ጥቂት የሰብዓ ሊቃናት ትርጕሞች (እንዲሁም 1ዜና 23፥19 ይመ) ከዚህ ጋር ይስማማሉ፤ አብዛኞቹ የዕብራይስጥ ቅጆች ግን፣ የይሪያ ወንዶች ልጆች ይላሉ፣ ሁለተኛው አማርያ፣ ሦስተኛው የሕዚኤል፣ አራተኛው ይቀምዓም።

24የዑዝኤል ልጅ፣

ሚካ ከሚካ ወንዶች ልጆች ሻሚር።

25የሚካ ወንድም ይሺያ፤

ከይሺያ ወንዶች ልጆች ዘካርያስ።

26የሜራሪ ወንዶች ልጆች፤ ሞሖሊ፣ ሙሲ።

የያዝያ ወንድ ልጅ በኖ።

27የሜራሪ ወንዶች ልጆች፤

ከያዝያ በኖ፣ ሾሃም፣ ዘኩር፣ ዔብሪ።

28ከሞሖሊ፤ አልዓዛር፤ ይህ ሰው ወንዶች ልጆች አልነበሩትም።

29ከቂስ፤ የቂስ ወንድ ልጅ፤

ይረሕምኤል።

30የሙሲ ወንዶች ልጆች፤ ሞሖሊ፣ ዔዳር፣ ለኢያሪሙት።

እነዚህ እንግዲህ እንደየቤተ ሰባቸው የተቈጠሩ ሌዋውያን ነበሩ።

31ወንድሞቻቸው የአሮን ዘሮች እንዳደረጉት ሁሉ፣ እነዚህም በንጉሥ ዳዊት፣ በሳዶቅ፣ በአቢሜሌክ እንዲሁም የካህናቱና የሌዋውያኑ ቤተ ሰብ አለቆች ባሉበት ዕጣ ተጣጣሉ፤ የበኵሩም ቤተ ሰቦች እንደ ትንሹ ወንድም ቤተ ሰብ እኩል ዕጣ ተጣለላቸው።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mbiri 24:1-31

Magulu a Ansembe

1Magulu a ana a Aaroni anali awa:

Ana a Aaroni anali Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara. 2Koma Nadabu ndi Abihu anamwalira abambo awo asanamwalire, ndipo analibe ana aamuna. Kotero Eliezara ndi Itamara ankatumikira monga ansembe. 3Mothandizidwa ndi Zadoki chidzukulu cha Eliezara ndi Ahimeleki chidzukulu cha Itamara, Davide anawagawa mʼmagulu molingana ndi ntchito yawo yotumikira. 4Atsogoleri ambiri anapezeka pakati pa zidzukulu za Eliezara kusiyana ndi zidzukulu za Itamara ndipo anagawidwa moyenera: atsogoleri 16 a mabanja ochokera kwa Eliezara, ndipo atsogoleri asanu ndi atatu a mabanja ochokera kwa zidzukulu za Itamara. 5Anawagawa mosakondera pochita maere, pakuti iwo anali akuluakulu a ku malo opatulika ndi akuluakulu a Mulungu pakati pa zidzukulu za Eliezara ndi Itamara.

6Mlembi Semaya mwana wa Netaneli, Mlevi, analemba mayina awo pamaso pa mfumu ndi akuluakulu ake: wansembe Zadoki, Ahimeleki mwana wa Abiatara ndi atsogoleri a mabanja a ansembe ndiponso Alevi, banja limodzi kuchokera kwa Eliezara kenaka limodzi kuchokera kwa Itamara.

7Maere woyamba anagwera Yehoyaribu,

achiwiri anagwera Yedaya,

8achitatu anagwera Harimu,

achinayi anagwera Seorimu,

9achisanu anagwera Malikiya,

achisanu ndi chimodzi anagwera Miyamini,

10achisanu ndi chiwiri anagwera Hakozi,

achisanu ndi chitatu anagwera Abiya,

11achisanu ndi chinayi anagwera Yesuwa,

a khumi anagwera Sekaniya,

12a 11 anagwera Eliyasibu,

a 12 anagwera Yakimu,

13a 13 anagwera Hupa,

a 14 anagwera Yesebeabu,

14a 15 anagwera Biliga,

a 16 anagwera Imeri,

15a 17 anagwera Heziri,

a 18 anagwera Hapizezi,

16a 19 anagwera Petahiya,

a 20 anagwera Ezekieli,

17a 21 anagwera Yakini,

a 22 anagwera Gamuli,

18a 23 anagwera Delaya,

ndipo a 24 anagwera Maaziya.

19Umu ndi mmene anasankhidwira kuti azigwira ntchito yotumikira pamene alowa mʼNyumba ya Yehova, motsatira dongosolo limene anapatsidwa ndi kholo lawo Aaroni, monga momwe Yehova Mulungu wa Israeli anamulamulira.

Alevi Ena Onse

20Za zidzukulu zina zonse za Levi:

Kuchokera kwa ana a Amramu: Subaeli;

kuchokera kwa ana a Subaeli: Yehideya.

21Kwa Rehabiya, kuchokera kwa ana ake:

Mtsogoleri anali Isiya.

22Kuchokera ku banja la Izihari: Selomoti;

kuchokera kwa ana a Selomoti: Yahati.

23Ana a Hebroni: woyamba anali Yeriya, wachiwiri anali Amariya, wachitatu anali Yahazieli ndipo Yekameamu anali wachinayi.

24Mwana wa Uzieli: Mika;

kuchokera kwa ana a Mika: Samiri.

25Mʼbale wa Mika: Isiya;

kuchokera kwa ana a Isiya: Zekariya.

26Ana a Merari: Mahili ndi Musi.

Mwana wa Yaaziya: Beno.

27Ana a Merari:

Kuchokera kwa Yaaziya: Beno, Sohamu, Zakuri ndi Ibiri.

28Kuchokera kwa Mahili: Eliezara, amene analibe ana aamuna.

29Kuchokera kwa Kisi:

Mwana wa Kisi: Yerahimeeli.

30Ndipo ana a Musi: Mahili, Ederi ndi Yerimoti.

Awa anali Alevi potsata mabanja a makolo awo. 31Iwonso anachita maere, monga anachitira abale awo, zidzukulu za Aaroni, pamaso pa mfumu Davide, ndi Zadoki ndi Ahimeleki, atsogoleri a mabanja a ansembe ndi Alevi. Mabanja a mwana wamkulu anachita nawo mofanana ndi a mwana wamngʼono.