ኢሳይያስ 28 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

ኢሳይያስ 28:1-29

ወዮ ለኤፍሬም

1ለኤፍሬም ሰካራሞች የመታበያ አክሊል ለሆነች፣

በለመለመ ሸለቆ ዐናት ላይ ጕብ ብላ፣

የክብሩ ውበት ለሆነች ጠውላጋ አበባ፣

የወይን ጠጅ ለዘራቸው መኵራሪያ ለሆነች፣

ለዚያች ከተማ ወዮላት!

2እነሆ፤ ጌታ ኀያልና ብርቱ የሆነ ነገር አለው፤

ይህም እንደ በረዶ ወጀብ፣ እንደሚያጠፋ ዐውሎ ነፋስ፣

እንደ ኀይለኛ ማዕበል፣ እንደ ከባድ ዝናብ፣

በኀይል ወደ ምድር ይጥላታል።

3የኤፍሬም ሰካራሞች የመታበያ አክሊል፣

በእግር ይረገጣል።

4በለምለሙ ሸለቆ ዐናት ላይ ጕብ ብላ፣

የክብሩ ውበት የሆነች ጠውላጋ አበባ፣

ከመከር በፊት እንደ ደረሰች፣

ሰውም ድንገት አይቶ እንደሚቀጥፋት

ወዲያውኑም እንደሚውጣት በለስ ትሆናለች።

5በዚያን ቀን የሰራዊት ጌታ እግዚአብሔር

ለተረፈው ሕዝቡ፣

የክብር ዘውድ፣

የውበትም አክሊል ይሆናል።

6እርሱም በፍርድ ወንበር ላይ ለሚቀመጠው፣

የፍትሕ መንፈስ፣

ጦርን ከከተማዪቱ በር ላይ ለሚመልሱም፣

የኀይል ምንጭ ይሆናል።

7እነዚህም በወይን ጠጅ ይንገዳገዳሉ፤

በሚያሰክርም መጠጥ ይወላገዳሉ፤

ካህናቱና ነቢያቱ በሚያሰክር መጠጥ ተንገዳገዱ፤

በወይን ጠጅ ነገር ተምታታባቸው፤

በሚያሰክር መጠጥ ተወላገዱ፤

ራእይ ሲያዩ ይስታሉ፤

ፍርድ ሲሰጡም ይሰናከላሉ።

8የማእድ ገበታቸው ሁሉ በትፋት ተሞልቷል፤

ከትውኪያም የጸዳ ቦታ የለም።

9እነርሱም እንዲህ ይላሉ፤ “የሚያስተምረው ማንን ነው?

መልእክቱን የሚያብራራውስ ለማን ነው?

ወተት ለተዉት ሕፃናት?

ወይስ ጡት ለጣሉት?

10በትእዛዝ ላይ ትእዛዝ፣ በትእዛዝ ላይ

ትእዛዝ፤

በደንብ ላይ ደንብ፣ በደንብ ላይ ደንብ፤28፥10 በዚህና በቍጥር 13 ላይ ዕብራይስጡ፣ ላቨ ላሳቨ ሳቨ ላሳቨ፣ ካቨ ላካቨ ካቨ ለካቨ ይላል፤ ምናልባት ትርጕም የለሽ ንግግርን ለማሳየት ይሆናል፤ ይኸውም የነቢያትን ቃል አስመስሎ መናገርን ሊሆን ይችላል።

እዚህ ጥቂት፣ እዚያ ጥቂት ነውና።”

11እንግዲያማ እግዚአብሔር

በባዕድ ልሳን በእንግዳ ቋንቋ ለዚህ ሕዝብ ይናገራል።

12እርሱ፣

“ይህች የዕረፍት ቦታ ናት፤ የደከመው ይረፍ፤

ይህች የእፎይታ ቦታ ናት” ያለው ለማን ነበር?

እነርሱ ግን መስማት አልፈለጉም።

13ስለዚህ የእግዚአብሔር ቃል፣

በትእዛዝ ላይ ትእዛዝ፣ በትእዛዝ ላይ ትእዛዝ፤

በደንብ ላይ ደንብ፣ በደንብ ላይ ደንብ፤

እዚህ ጥቂት እዚያ ጥቂት ይሆንባቸዋል።

ይህ የሚሆንባቸው ሄደው ወደ ኋላ እንዲወድቁ፣

እንዲቈስሉና በወጥመድ እንዲያዙ፣

እንዲማረኩም ነው።

14ስለዚህ በኢየሩሳሌም ያለውን ሕዝብ የምትገዙ፣

እናንት ፌዘኞች የእግዚአብሔርን ቃል ስሙ።

15እናንት፣ “ከሞት ጋር ቃል ኪዳን ገብተናል፤

ከሲኦልም ጋር ስምምነት አድርገናል፤

ውሸትን መጠጊያችን፣

ሐሰትን28፥15 ወይም፣ ሐሰተኛ ጣዖታትን መደበቂያችን አድርገናል፤

ታላቅ መቅሠፍት እየጠራረገ ሲያልፍ፣

ሊነካን አይችልም” በማለት ታብያችኋል።

16ስለዚህ ጌታ እግዚአብሔር እንዲህ ይላል፤

“እነሆ፤ የተፈተነ ድንጋይ፣ የመሠረት ድንጋይ፣

ለጽኑ መሠረት የሚሆን የከበረ የማእዘን ድንጋይ፣

በጽዮን አስቀምጣለሁ፤

በእርሱም የሚያምን አያፍርም።

17ፍትሕን የመለኪያ ገመድ፣

ጽድቅንም ቱንቢ አደርጋለሁ፤

ውሸት መጠጊያችሁን የበረዶ ዝናብ ይጠራርገዋል፤

መደበቂያችሁንም ውሃ ያጥለቀልቀዋል።

18ከሞት ጋር የገባችሁት ቃል ኪዳን ይሻራል፤

ከሲኦልም ጋር ያደረጋችሁት ስምምነት ይፈርሳል፤

ታላቁ መቅሠፍት እየጠራረገ ሲያልፍ፣

እናንተም ትጠራረጋላችሁ።

19በመጣ ቍጥር ይዟችሁ ይሄዳል፤

ማለዳ ማለዳ፣ በቀንና በሌሊትም

ይጠራርጋል።”

ይህን ቃል ብታስተውሉ፣

ሽብር በሽብር በሆነ ነበር።

20እግር ዘርግቶ እንዳይተኛ ዐልጋው ዐጭር ነው፤

ሰውነትንም ለመሸፋፈን ብርድ ልብሱ ጠባብ ነው።

21እግዚአብሔር ሥራውን፣ አዎን ድንቅ ሥራውን ሊሠራ፣

ተግባሩን፣ እንግዳ የሆነ ተግባሩን ሊያከናውን፣

በፐራሲም ተራራ እንዳደረገው ይነሣል፣

በገባዖን ሸለቆ እንዳደረገው ይነሣሣል።

22እንግዲህ ፌዛችሁን አቁሙ፤

አለዚያ እስራታችሁ ይጸናባችኋል፤

ጌታ፣ የሰራዊት ጌታ እግዚአብሔር

መላውን ምድር ለማጥፋት ያወጀውን ዐዋጅ ሰምቻለሁ።

23አድምጡ ድምፄን ስሙ፤

አስተውሉ ቃሌንም ስሙ።

24ገበሬ ሊዘራ መሬቱን ሲያዘጋጅ ያለ ማቋረጥ ያርሳልን?

ጓሉን ሲከሰክስ፣ ዐፈሩን ሲያለሰልስ ይከርማልን?

25ዕርሻውን አስተካክሎ፣

ጥቍር አዝሙድና ከሙን አይዘራምን?

ስንዴውንስ በትልሙ28፥25 በዕብራይስጡ የዚህ ቃል ትርጕም በትክክል አይታወቅም።

ገብሱን በተገቢ ቦታው፣

አጃውንም በተመደበው ስፍራ አይዘራምን?

26አምላኩ ያስተምረዋል፤

ትክክለኛውንም መንገድ ያሳየዋል።

27ጥቍር አዝሙድ በመውቂያ መሣሪያ አይወቃም፤

ከሙን የሠረገላ መንኰራኵር አይሄድበትም፤

ጥቍር አዝሙድ በበትር፣

ከሙንም በዘንግ ይወቃል።

28እንጀራን ለመጋገር እህል ይፈጫል፤

ስለዚህ አንድ ሰው ለዘላለም እህል ሲወቃ አይኖርም።

የመውቂያውን መንኰራኵር ቢያኼድበትም፣

ፈረሶቹ አይደፈጥጡትም።

29ይህ ሁሉ የሚሆነው በምክሩ ድንቅ፣ በጥበቡ

ታላቅ ከሆነው፣

ከሰራዊት ጌታ ከእግዚአብሔር ዘንድ ነው።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesaya 28:1-29

Tsoka kwa Efereimu

1Tsoka ufumu wonyada wa zidakwa za ku Efereimu.

Tsoka kwa ulemerero wake wokongola umene ukufota ngati duwa

limene lili pa mutu pa anthu

oledzera a mʼchigwa chachonde.

2Taonani, ambuye ali naye wina wamphamvu ndi nyonga.

Iye adzabwera ngati mkuntho wamatalala ndi namondwe wowononga,

ngati madzi amphamvu osefukira a mvula yamkuntho;

ndipo adzawagwetsa pansi mwankhanza.

3Ulamuliro wa atsogoleri oledzera

a ku Efereimu adzawuthetsa.

4Ndipo ulemerero wokongola wa mzinda umene uli ngati duwa

lofota pamutu pa anthu oledzera a mʼchigwa chachonde uja,

udzakhala ngati nkhuyu yoyambirira kupsa

imene munthu akangoyiona amayithyola

nthawi yokolola isanakwane.

5Tsiku limenelo Yehova Wamphamvuzonse

adzakhala ngati nkhata yaufumu,

chipewa chokongola

kwa anthu ake otsala.

6Iye adzapereka mtima

wachilungamo kwa oweruza,

adzakhala chilimbikitso kwa

amene amabweza adani pa zipata za mzinda.

7Nawonso awa ali dzandidzandi chifukwa cha vinyo

ndipo akusochera chifukwa cha mowa:

ansembe ndi aneneri akudzandira chifukwa cha mowa

ndipo akusokonezeka chifukwa cha vinyo;

akusochera chifukwa cha mowa,

akudzandira pamene akuona masomphenya,

kupunthwa pamene akupereka chigamulo.

8Pa matebulo onse pali masanzi okhaokha

ndipo palibenso malo wopanda zonyansa.

9Iwo akuti, “Kodi munthu ameneyu akufuna aphunzitse ndani?

Uthengawu akufuna kufotokozera yani?

Ndi kwa ana amene aleka kuyamwa,

kwa makanda ongowachotsa kumene ku bere?

10Akuyesa kumatiphunzitsa pangʼonopangʼono

lemba ndi lemba, mzere ndi mzere,

phunziro ndi phunziro.

Zonsezi akungoti apa pangʼono apa pangʼono.”

11Mulungu adzayankhula kwa anthu ake kudzera mwa anthu aziyankhulo zachilendo, ziyankhulo zosamveka bwino.

Mulungu adzayankhula kwa anthu awa, amene

12anakuwuzani kuti,

“Malo opumulira ndi ano,

otopa apumule, malo owusira ndi ano.”

Koma inu simunamvere.

13Choncho Yehova adzakuphunzitsani

pangʼonopangʼono lemba ndi lemba,

mzere ndi mzere, phunziro ndi phunziro.

Kotero mudzayenda ndi kugwa chambuyo,

adzapweteka ndi kukodwa mu msampha

ndipo adzakutengani ku ukapolo.

14Nʼchifukwa chake imvani mawu a Yehova,

inu anthu achipongwe amene mumalamulira anthu awa mu Yerusalemu.

15Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa,

ife tachita mgwirizano ndi manda.

Pamene mliri woopsa ukadzafika

sudzatikhudza ife,

chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu

ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.”

16Tsono zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi:

“Taonani, ndikuyika mwala wovomerezeka ndi amisiri

ngati maziko mu Ziyoni,

mwala wapangodya, wamtengowapatali wopanga maziko amphamvu;

munthu amene awukhulupirira sadzagwedezeka.

17Ntchito zolungama zidzakhala ngati chingwe choyezera maziko ake,

ndipo chilungamo chidzakhala chowongolera mzere;

matalala adzawononga malo anu othawirapo, amene ndi mabodza,

ndipo madzi adzamiza malo anu obisalako.

18Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa;

mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa.

Pakuti mliri woopsa udzafika,

ndipo udzakugonjetsani.

19Ndipo ukadzangofika udzakutengani.

Udzafika mmawa uliwonse,

usiku ndi usana.”

Anthu akadzamvetsetsa uthenga umenewu

adzaopsedwa kwambiri.

20Mudzakhala ngati munthu wogona pa bedi lalifupi kwambiri kuti sangathe kutambalitsapo miyendo;

ndiponso mudzakhala ngati munthu amene wafunda bulangeti lochepa kwambiri kuti sangathe nʼkufunda komwe.

21Yehova adzamenya nkhondo monga anachitira ku phiri la Perazimu

adzakalipa monga anachitira ku chigwa cha Gibiyoni;

adzagwira ntchito yake yooneka ngati yachilendo,

ndipo zimene ati adzachite zidzakhala ngati zodabwitsa.

22Tsopano lekani kunyoza,

mukapanda kutero maunyolo anu adzakuthinani kwambiri;

Ambuye, Yehova Wamphamvuzonse wandiwuza kuti,

“Ndagamula kuti ndidzawononga dziko lapansi.”

23Tcherani khutu ndipo mumve mawu anga;

mvetserani ndipo mumve zimene ndikunena.

24Kodi mlimi wofuna kudzala mbewu amangokhalira kutipula kokhakokha?

Kodi amangokhalira kugawula ndi kugalawuza kokhakokha?

25Pamene iye wasalaza mundawo,

kodi samafesa mawere ndi chitowe?

Kodi suja samadzala tirigu

ndi barele mʼmizere yake,

nadzala mchewere mʼphepete mwa mundawo?

26Mulungu wake amamulangiza

ndi kumuphunzitsa njira yabwino.

27Mawere sapunthira chopunthira cha galeta lopanda mikombero,

kapena chitowe sapuntha popondetsapo mikombero ya galeta;

mawere amapuntha ndi ndodo

ndipo chitowe amapuntha ndi kamtengo.

28Tirigu ayenera kusinjidwa kuti apangire buledi,

komabe munthu samangokhalira kupuntha tiriguyo osalekeza, kuopa kuti angatekedzeke.

Ngakhale kuti amapuntha tiriguyo poyendetsapo mikombero ya galeta,

koma akavalo ake satekedza tiriguyo.

29Izinso zimachokera kwa Yehova Wamphamvuzonse,

wa uphungu wodabwitsa ndi wa nzeru zopambana.