ምሳሌ 16 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

ምሳሌ 16:1-33

1የልብ ዕቅድ የሰው ነው፤

የአንደበት መልስ ግን ከእግዚአብሔር ዘንድ ነው።

2ለሰው መንገዱ ሁሉ ንጹሕ መስሎ ይታየዋል፤

መነሻ ሐሳቡ ግን በእግዚአብሔር ይመዘናል።

3የምታደርገውን ሁሉ ለእግዚአብሔር ዐደራ ስጥ፤

ዕቅድህም ሁሉ ይሳካልሃል።

4እግዚአብሔር ሁሉንም ነገር ለራሱ ዐላማ ሠርቷል፤

ክፉዎችንም እንኳ ለጥፋት ቀን አዘጋጅቷል።

5እግዚአብሔር በልብ የሚታበዩትን ሁሉ ይጸየፋል፤

እነርሱም ከቅጣት እንደማያመልጡ በርግጥ ዕወቅ።

6በፍቅርና በታማኝነት ኀጢአት ይሰረያል፤

እግዚአብሔርን በመፍራት ሰው ከክፋት ይርቃል።

7የሰው መንገድ እግዚአብሔርን ደስ ሲያሰኘው፣

ጠላቶቹ እንኳ አብረውት በሰላም እንዲኖሩ ያደርጋል።

8ከጽድቅ ጋር ጥቂቱ ነገር፣

በግፍ ከሚገኝ ብዙ ትርፍ ይሻላል።

9ሰው በልቡ መንገዱን ያቅዳል፤

እግዚአብሔር ግን ርምጃውን ይወስንለታል።

10የንጉሥ ከንፈሮች እንደ አምላክ ቃል ይናገራሉ፤

አንደበቱ ፍትሕን ያዛባ ዘንድ አይገባም።

11ሐቀኛ መስፈሪያና ሚዛን ከእግዚአብሔር ናቸው፤

በከረጢት ውስጥ ያሉት መመዘኛዎችም ሁሉ ሥራዎቹ ናቸው።

12ክፋትን ማድረግ ለነገሥታት አስጸያፊ ነው፤

ዙፋን የሚጸናው በጽድቅ ነውና።

13ነገሥታት በታማኝ ከንፈሮች ደስ ይላቸዋል፤

እውነት የሚናገረውን ሰው ይወድዱታል።

14የንጉሥ ቍጣ የሞት መልእክተኛ ነው፤

ጠቢብ ሰው ግን ቍጣውን ያበርዳል።

15የንጉሥ ፊት ሲፈካ ሕይወት አለ፤

በጎነቱም ዝናብ እንዳዘለ የበልግ ደመና ነው።

16ከወርቅ ይልቅ ጥበብን ማግኘት፣

ከብርም ማስተዋልን መምረጥ ምንኛ ይበልጣል!

17የቅኖች ጐዳና ከክፋት የራቀ ነው፤

መንገዱንም የሚጠብቅ ሕይወቱን ይጠብቃል።

18ትዕቢት ጥፋትን፣

የእብሪት መንፈስም ውድቀትን ትቀድማለች።

19በተዋረደ መንፈስ ከተጨቈኑት ጋር መሆን፣

ከትዕቢተኞች ጋር ብዝበዛን ከመካፈል ይሻላል።

20ምክርን የሚሰማ ይለመልማል፤

በእግዚአብሔርም የሚታመን ቡሩክ ነው።

21ልባቸው ጠቢብ የሆነ አስተዋዮች ይባላሉ፤

ደስ የሚያሰኙ ቃላትም ዕውቀትን ያዳብራሉ።16፥21 ወይም ቃላትም ተደማጭነት ያስገኛሉ

22ማስተዋልን ገንዘብ ላደረጋት የሕይወት ምንጭ ናት፤

ቂልነት ግን በተላሎች ላይ ቅጣት ታመጣባቸዋለች።

23የጠቢብ ሰው ልብ አንደበቱን ይመራል፤

ከንፈሮቹም ዕውቀትን ያዳብራሉ።16፥23 ወይም አንደበቱን አሳማኝ ያደርጋሉ

24ደስ የሚያሰኝ ቃል የማር ወለላ ነው፤

ለነፍስ ጣፋጭ፣ ለዐጥንትም ፈውስ ነው።

25ለሰው ቀና መስሎ የሚታይ መንገድ አለ፤

በመጨረሻ ግን ወደ ሞት ይመራል።

26ሠራተኛን የዕለት ጕርስ ፍላጎቱ ታታሪ ያደርገዋል፤

ራቡም ይገፋፋዋል።

27ወራዳ ሰው ክፋትን ያውጠነጥናል፤

ንግግሩም እንደሚለበልብ እሳት ነው።

28ጠማማ ሰው ጠብን ይዘራል፤

ሐሜተኛም የቅርብ ወዳጆችን ይለያያል።

29ክፉ ሰው ባልንጀራውን ያባብለዋል፤

መልካም ወዳልሆነውም መንገድ ይመራዋል።

30በዐይኑ የሚጠቅስ ሰው ጠማማነትን ያውጠነጥናል፤

በከንፈሩ የሚያሽሟጥጥም ወደ ክፋት ያዘነብላል።

31ሽበት የክብር ዘውድ ነው፤

የሚገኘውም በጽድቅ ሕይወት ነው።

32ታጋሽ ሰው ከጦረኛ፣

ስሜቱን የሚገዛም ከተማን በጕልበቱ ከሚይዝ ይበልጣል።

33ዕጣ በጕያ ውስጥ ይጣላል፤

ውሳኔው በሙሉ ግን ከእግዚአብሔር ዘንድ ነው።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Miyambo 16:1-33

1Zolinga za mu mtima ndi za munthu,

koma kwa Yehova ndiye kumachokera yankho.

2Zochita zonse za munthu zimaoneka zabwino pamaso pake,

koma Yehova ndiye amasanthula zolinga zako.

3Pereka ntchito zako zonse mʼmanja mwa Yehova,

ndipo zolinga zako zidzachitikadi.

4Yehova amachita zonse ndi cholinga chake,

ngakhale anthu oyipa kuti aone tsiku latsoka.

5Munthu aliyense wodzikuza amamunyansa Yehova.

Koma dziwani izi: Iwo sadzakhala osalangidwa.

6Chifukwa cha chikondi chosasinthika ndi kukhulupirika, munthu amakhululukidwa machimo ake;

chifukwa cha kuopa Yehova munthu amapewa zoyipa.

7Pamene makhalidwe a munthu akondweretsa Yehova,

ngakhale adani ake amakhala naye mwa mtendere.

8Kuli bwino kukhala ndi zinthu pangʼono zozipeza mwachilungamo,

kusiyana ndi kukhala ndi zinthu zambiri zozipeza popanda chilungamo.

9Mtima wa munthu umalingalira zochita,

koma Yehova ndiye amakhazikitsa njira zake.

10Mawu a mfumu ali ngati mawu ochokera kwa Mulungu;

ndipo pakamwa pake sipalakwa poweruza mlandu.

11Miyeso ndi masikelo achilungamo zimachokera kwa Yehova;

miyala yonse yoyesera ya mʼthumba anayipanga ndi Yehova.

12Kuchita zoyipa kumanyansa mafumu,

pakuti chilungamo ndiye maziko a ufumu wake.

13Mawu owona amakondweretsa mfumu.

Iyo imakonda munthu woyankhula choonadi.

14Ukali wa mfumu ndi mthenga wa imfa,

koma munthu wanzeru amawupepesa ukaliwo.

15Kuwala kwa nkhope ya mfumu kumapatsa moyo;

ndipo kukoma mtima kwake kuli ngati mitambo ya mvula nthawi ya chilimwe.

16Nʼkwabwino kwambiri kupeza nzeru kupambana golide.

Kukhala womvetsa bwino zinthu nʼkwabwino kupambana ndi kukhala ndi siliva.

17Msewu wa munthu wowongoka mtima umapewa zoyipa;

wopenyetsetsa kumene akupita amasunga moyo wake.

18Kunyada kumafikitsa ku chiwonongeko,

ndipo munthu wodzikuza adzagwa.

19Nʼkwabwino kukhala ndi mtima wodzichepetsa pakati pa anthu oponderezedwa,

kusiyana ndi kugawana zolanda ndi anthu onyada.

20Munthu womvera malangizo zinthu zimamuyendera bwino,

ndipo wodala ndi amene amadalira Yehova.

21A mtima wanzeru amatchedwa ozindikira zinthu,

ndipo mawu ake okoma amawonjezera nzeru.

22Kumvetsa zinthu ndi kasupe wa moyo kwa iwo amene ali nako,

koma uchitsiru umabweretsa chilango kwa zitsiru.

23Mtima wanzeru umathandiza munthu kuyankhula mwa nzeru,

ndipo mawu ake amawonjezera nzeru.

24Mawu okometsera ali ngati chisa cha njuchi,

amakoma mu mtima ndipo amalimbitsa thupi.

25Pali njira ina yooneka ngati yowongoka kwa munthu

koma kumatsiriziro kwake ndi imfa.

26Njala ya munthu wantchito imamuthandiza kulimbikira;

njalayo imamukakamiza kuchitapo kanthu.

27Munthu wopanda pake amakonzekera kuchita zoyipa

ndipo mawu ake ali ngati moto wopsereza.

28Munthu woyipa mtima amayambitsa mikangano,

ndipo miseche imalekanitsa anthu okondana kwambiri.

29Munthu wandewu amakopa mnansi wake,

ndipo amamuyendetsa njira imene si yabwino.

30Amene amatsinzinira maso ake amalingalira zinthu zokhota;

amene amachita msunamo amakonzeka kuchita zoyipa.

31Imvi zili ngati chipewa chaufumu chaulemerero;

munthu amazipeza akakhala moyo wolungama.

32Munthu wosapsa mtima msanga amaposa munthu wankhondo,

munthu wowugwira mtima wake amaposa amene amalanda mzinda.

33Maere amaponyedwa pa mfunga,

koma ndiye Yehova amene amalongosola zonse.