Apocalipsis 12 – MTDS & CCL

Mushuj Testamento Diospaj Shimi

Apocalipsis 12:1-17

Satanastami jahua pachamanta shitashca

1Chai qʼuipaca, jatun mancharina señalmi, jahua pachapica ricurirca: Intita churarishca shuj huarmimi, luna jahuapi shayacurca. Umapica, chunga ishqui luźerocunayuj coronata churashcami carca. 2Chai huarmica, chichu cashpa ña huachagrishpami, huachana nanaihuan jatunta caparicurca. 3Shujtaj señalpishmi jahua pachapica, cashna ricurirca: Canchis umayuj, chunga gachuyuj amsa puca jatun dragonmi ricurirca. Umacunapica, canchis coronata churashcami carca. 4Chai dragonca, quimsapi chaupishca shuj parte luźerocunatami, paipaj chupahuan jahua pachamanta aisashpa cai pachaman shitarca. Chai dragonca, huachanachicuj huarmipaj ñaupajpimi, huahua huacharinca huahuata millpungapaj shuyacurca. 5Chai huarmica, cʼari huahuatami huacharca. Chai huahuami cai pachapi causacujcunataca, fierro varahuan tucuicunata mandanga. Chai huahuataca, mamata quichushpami, quiquin mandanapi tiyacuj Taita Diospajman aparca. 6Chai huahuapaj mamaca, shitashca pambapi Taita Dios allichishcapimi, miticungapaj rirca. Chaipimi, 1.260 punllacunacama carashpa charirca.

7Chai qʼuipaca, jahua pachapica, shuj jatun macanacuimi tiyarca. Mandaj ángel Miguelmi, paipaj angelcunandij, dragonhuan macanacurca. Dragonpish, paipaj angelcunata pushashcami macanacurca. 8Chai macanacuipica, dragontami misharcacuna. Chaimantami paipish, paipaj angelcunapish, ña mana jahua pachapi cai tucurcacuna. 9Chai jatun dragontaca, jahua pachamantaca ña shitarcami. Paica, ñaupa rucu culebrami, Diablo shutipish, Satanás shutipishmi. Paimi, tucui cai pachapi causacujcunata umashpa tiyan. Paitami tucui paipaj millai angelcunandijta, allpa pachaman shitarca.

10Chai qʼuipaca, jahua pachapi cashna nishpa sinchita caparijtami uyarcani:

«Ñucanchij Taita Dios quishpichishpa mandana punlla chayamushcatajmari.

Paipaj Cristo mandanamari callarishca.

Cunatajca, ñucanchij huauquicunata juchachicujtaca, ña shitashcatajmari.

Paimari ñucanchij Diospaj ñaupajpica tutapish, punllapish juchachishpa purirca.

11Paicunaca, Malta Ovejapaj yahuarmantapish,

Diospaj Shimita huillashcamantapishmi,

diablotaca misharcacuna.

Huañuchishun nijpipish, huañunataca mana mancharcacunachu.

12Chaimanta jahua pachacunapish,

chaicunapi causajcunapish cushicuichigari.

Ashtahuanpish allpapi, mama cuchapi causacujcunaca,

¡imachari tucunguichij!

Diabloca, ña ashalla punllacunata charishcata yachashpami,

jatunta pʼiñarishpa, cancunapajman uriyamushca» nijtami uyarcani.

13Chai dragonca, paita cai pachaman ña shitajpica, cʼari huahuata huachaj huarmitami huañuchisha nishpa llaquichirca. 14Chaimantami chai huarmimanca, jatun aguilapaj ishqui alasta curca. Chaihuanmi culebrapaj ñaupajmanta jatarishpa, pai tiyachun allichishca, shitashca pambaman rirca. Chaipimi, quimsa huata chaupicama carashpa charirca. 15Chai huarmitaca, yacu apachun nishpami, culebraca huarmita catichishpa, paipaj shimimanta jatun yacuta shitarca. 16Dragonpaj shimimanta shamuj jatun yacutaca, allpa chaupirishpami tucui millpurca. Chashnami chai huarmitaca quishpichirca. 17Chaimantami dragonca, chai huarmitaca ashtahuan pʼiñashpa, chai huarmipaj caishuj huahuacunahuan macanacugrirca. Chai huahuacunaca, Taita Dios mandashcacunata alli caźucujcuna, Jesucristo huillashcatapish alli catijcunami.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chivumbulutso 12:1-18

Mayi ndi Chinjoka

1Chizindikiro chachikulu chinaoneka kuthambo; mayi atavala dzuwa, mapazi ake ataponda mwezi, pamutu pake pali chipewa chaufumu chokhala ndi nyenyezi khumi ndi ziwiri. 2Mayiyo anali woyembekezera ndipo pa nthawi yake yochira analira mokuwa chifukwa cha ululu wakubala. 3Kenaka ku thambo kunaonekanso chizindikiro china; chinjoka chachikulu kwambiri, chofiira chomwe chinali ndi mitu isanu ndi iwiri ndi nyanga khumi; pamutu uliwonse chitavala chipewa chaufumu. 4Mchira wake unakokolola gawo limodzi la magawo atatu a nyenyezi kuzichotsa ku thambo ndi kuziponya pa dziko lapansi. Chinjoka chija chinadzayima patsogolo pa mayi uja amene anali pafupi kuberekayu kuti mwanayo akangobadwa chimudye. 5Mayiyo anabereka mwana wamwamuna amene adzalamulira anthu a mitundu ina yonse ndi ndodo yachitsulo. Ndipo mwanayo analandidwa ku dzanja la mayiyo ndi kupita naye kwa Mulungu ku mpando wake waufumu. 6Mayiyo anathawira ku chipululu ku malo kumene Mulungu anamukonzera, kumene akasamalidweko masiku 1,260.

7Zitatero, kumwamba kunayambika nkhondo. Mikayeli ndi angelo ake kumenyana ndi chinjoka chija. Chinjokacho ndi angelo ake anabwezeranso. 8Koma analibe mphamvu ndipo anagonjetsedwa nathamangitsidwa kumwambako. 9Chinjoka chachikulu chija chinagwetsedwa pansi. Ichocho ndiye njoka yakalekale ija yotchedwa Mdierekezi kapena Satana, amene amasocheretsa anthu a pa dziko lonse lapansi. Chinaponyedwa pa dziko la pansi pamodzi ndi angelo ake.

10Kenaka ndinamva mawu ofuwula kumwamba akunena kuti,

“Tsopano chipulumutso, mphamvu,

ufumu wa Mulungu wathu

ndi ulamuliro wa Khristu wake zabwera.

Pakuti woneneza abale athu uja,

amene amangokhalira kuwaneneza pamaso pa Mulungu usana ndi usiku,

wagwetsedwa pansi.

11Abale athuwo anamugonjetsa

ndi magazi a Mwana Wankhosa

ndiponso mawu a umboni wawo.

Iwo anadzipereka kwathunthu,

moti sanakonde miyoyo yawo.

12Choncho, kondwerani, inu dziko lakumwamba

ndi onse okhala kumeneko!

Koma tsoka dziko lapansi ndi nyanja

chifukwa Mdierekezi wagwetsedwa kwa inu!

Iye wadzazidwa ndi ukali

chifukwa akudziwa kuti nthawi yake ndi yochepa.”

13Pamene chinjokacho chinaona kuti chagwetsedwa pa dziko lapansi, chinayamba kuthamangitsa mayi uja amene anali atabala mwana wamwamunayu. 14Mayiyo anapatsidwa mapiko awiri a chiwombankhanga chachikulu kuti athawire ku malo ake aja a ku chipululu. Kumeneko adzasamalidwako zaka zitatu ndi theka kuti chinjoka chija chisamupeze. 15Kenaka chinjoka chija chinalavulira mayiyo madzi ambiri ngati mtsinje, kuti madziwo amukokolole. 16Koma dziko lapansi linamuthandiza mayiyo. Nthaka inatsekuka ndi kumeza mtsinje uja unachokera mʼkamwa mwa chinjokacho. 17Pamenepo chinjokacho chinamupsera mtima mayiyo ndipo chinachoka kupita kukachita nkhondo ndi ana ena onse a mayiyo, ndiye kuti anthu amene anasunga malamulo a Mulungu ndi kuchitira umboni za Yesu.

18Kenaka ndinaona chinjokacho chitayima mʼmbali mwa nyanja.