Zabbuli 36 – LCB & CCL

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 36:1-12

Zabbuli 36

Ya Mukulu wa Bayimbi. Zabbuli ya Dawudi.

136:1 Bar 3:18*Nnina obubaka mu mutima gwange

obukwata ku bwonoonyi bw’omukozi w’ebibi.

N’okutya

tatya Katonda.

2Ye nga bw’alaba yeewaanawaana n’atasobola kutegeera

oba okukyawa ekibi kye.

336:3 a Zab 10:7 b Zab 94:8 c Yer 4:22Ebigambo ebiva mu kamwa ke biba bibi era nga bya bulimba;

takyalina magezi era takyakola birungi.

436:4 a Nge 4:16; Mi 2:1 b Is 65:2 c Zab 52:3; Bar 12:9Ne ku kitanda kye afumiitiriza ebibi by’anaakola;

amalirira okutambuliranga mu kkubo ekyamu,

era ebitali bituufu tabyewala.

5Okwagala kwo, Ayi Mukama, kutuuka ne ku ggulu;

obwesigwa bwo butuuka ku bire.

636:6 Yob 11:8; Zab 77:19; Bar 11:33Obutuukirivu bwo bugulumivu ng’agasozi aganene,

n’obwenkanya bwo buwanvu nnyo ng’ennyanja ennene ennyo.

Ayi Mukama, olabirira abantu n’ebisolo.

736:7 Lus 2:12; Zab 17:8Okwagala kwo okutaggwaawo nga tekugeraageranyizika.

Ab’ebitiibwa n’abatali ba bitiibwa

baddukira mu biwaawaatiro byo.

836:8 a Zab 65:4 b Yob 20:17; Kub 22:1Balya ku bingi eby’omu nnyumba yo ne bakkuta;

obawa ebyokunywa by’omugga gwo ogwesiimisa.

936:9 a Yer 2:13 b 1Pe 2:9Kubanga gw’olina ensulo ey’obulamu,

era gw’otwakiza omusana.

10Yongeranga okwagala abo abakutegeera,

era n’obutuukirivu bwo eri abo abalina emitima emirongoofu.

11Ab’amalala baleme okunninnyirira,

wadde ababi okunsindiikiriza.

1236:12 Zab 140:10Laba, ababi nga bwe bagudde!

Basuuliddwa wansi era tebasobola na ku golokokawo.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 36:1-12

Salimo 36

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide, mtumiki wa Yehova.

1Uthenga uli mu mtima mwanga

wonena za kuchimwa kwa munthu woyipa:

Mu mtima mwake

mulibe kuopa Mulungu.

2Pakuti iye mʼkuona kwake amadzinyenga yekha kwambiri,

sazindikira kapena kudana ndi tchimo lake.

3Mawu a pakamwa pake ndi oyipa ndi achinyengo;

iyeyo waleka kukhala wanzeru ndi kuchita zabwino.

4Ngakhale ali pa bedi pake amakonzekera zoyipa;

iye amadzipereka yekha ku njira ya uchimo

ndipo sakana cholakwa chilichonse.

5Chikondi chanu Yehova, chimafika ku mayiko a kumwamba,

kukhulupirika kwanu mpaka ku mitambo.

6Chilungamo chanu Mulungu chili ngati mapiri aakulu,

chiweruzo chanu chili ngati kuzama kwakukulu.

Yehova mumasunga munthu pamodzi ndi chinyama.

7Chikondi chanu chosatha ndi chamtengowapatali!

Otchuka pamodzi ndi anthu wamba pakati pa anthu

amapeza pothawirapo mu mthunzi wa mapiko anu.

8Iwo amadyerera zinthu zambiri za mʼnyumba yanu;

Inu mumawapatsa chakumwa kuchokera mu mtsinje wanu wachikondwerero.

9Pakuti kwa Inu kuli kasupe wamoyo;

mʼkuwala kwanu ifenso timaona kuwala.

10Pitirizani chikondi chanu pa iwo amene amakudziwani,

chilungamo chanu kwa olungama mtima.

11Musalole kuti phazi la wodzikuza libwere kulimbana nane,

kapena dzanja la oyipa kundithamangitsa.

12Onani momwe ochita zoyipa agonera atagwa,

aponyeni pansi, kuti asathe kudzukanso!