Zabbuli 135 – LCB & CCL

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 135:1-21

Zabbuli 135

1135:1 Zab 113:1; 134:1Mutendereze Mukama.

Mutendereze erinnya lya Mukama.

Mumutendereze mmwe abaddu ba Mukama;

2135:2 a Luk 2:37 b Zab 116:19mmwe abaweereza mu nnyumba ya Mukama,

mu mpya z’ennyumba ya Katonda waffe.

3135:3 a Zab 119:68 b Zab 147:1Mutendereze Mukama, kubanga Mukama mulungi;

mutendereze erinnya lye kubanga ekyo kisanyusa.

4135:4 a Ma 10:15; 1Pe 2:9 b Kuv 19:5; Ma 7:6Kubanga Mukama yeerondera Yakobo okuba owuwe;

ye Isirayiri gwe yeeroboza okuba eky’omuwendo.

5135:5 a Zab 48:1 b Zab 97:9Mmanyi nga Mukama mukulu wa kitiibwa,

era nga Mukama oyo y’asinga bakatonda bonna.

6135:6 Zab 115:3Mukama kyonna ky’asiima ky’akola,

mu ggulu ne ku nsi;

mu nnyanja ne mu buziba bwayo.

7135:7 a Yer 10:13; Zek 10:1 b Yob 28:25 c Yob 38:22Alagira ebire ne byekuluumulula okuva ku nkomerero y’ensi;

atonnyesa enkuba erimu okumyansa,

n’asumulula empewo okuva mu mawanika ge.

8135:8 Kuv 12:12; Zab 78:51Ye yakuba ababereberye ab’e Misiri;

ababereberye b’abantu n’ebibereberye by’ebisolo.

9135:9 a Ma 6:22 b Zab 136:10-15Ye yaweereza obubonero n’ebyewuunyo wakati wo, ggwe Misiri,

eri Falaawo n’abaweereza be bonna.

10135:10 Kbl 21:21-25; Zab 136:17-21Ye yakuba amawanga amangi,

n’atta bakabaka ab’amaanyi era be bano,

11135:11 a Kbl 21:21 b Yos 12:7-24Sikoni kabaka w’Abamoli,

ne Ogi kabaka w’e Basani

ne bakabaka bonna ab’e Kanani.

12135:12 Zab 78:55Ensi yaabwe n’agiwaayo ng’obusika,

okuba obusika bw’abantu be Isirayiri.

13135:13 a Kuv 3:15 b Zab 102:12Ayi Mukama, erinnya lyo lya lubeerera,

era n’obukulu bwo bumanyibwa emirembe gyonna.

14135:14 Ma 32:36Kubanga Katonda aliggyako abantu be omusango,

era alisaasira abaweereza be.

15Abamawanga ebifaananyi byonna ebyole bye basinza,

ebyakolebwa n’emikono gy’abantu mu ffeeza ne zaabu,

16birina emimwa, naye tebyogera;

birina amaaso, naye tebiraba;

17birina amatu naye tebiwulira;

so ne mu kamwa kaabyo temuyitamu mukka.

18Ababikola balibifaanana;

na buli abyesiga alibifaanana.

19Ayi ennyumba ya Isirayiri mutendereze Mukama;

mmwe ennyumba ya Alooni mutendereze Mukama.

20Mmwe ennyumba ya Leevi mutendereze Mukama;

mmwe abatya Mukama mutendereze Mukama.

21135:21 Zab 134:3Mukama ali mu Sayuuni yeebazibwe;

yeebazibwe oyo abeera mu Yerusaalemi.

Mutendereze Mukama.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 135:1-21

Salimo 135

1Tamandani Yehova.

Tamandani dzina la Yehova;

mutamandeni, inu atumiki a Yehova,

2amene mumatumikira mʼnyumba ya Yehova,

mʼmabwalo a nyumba ya Mulungu wathu.

3Tamandani Yehova, pakuti Yehova ndi wabwino;

imbani nyimbo zotamanda dzina lake, pakuti nʼkokoma kutero,

4Pakuti Yehova wasankha Yakobo kuti akhale wake,

Israeli kuti akhale chuma chake chapamtima.

5Ndikudziwa kuti Yehova ndi wamkulu,

kuti Ambuye athu ndi wamkulu kuposa milungu yonse.

6Yehova amachita chilichonse chimene chimamukomera,

kumwamba ndi dziko lapansi,

ku nyanja zazikulu ndi ku malo ake onse akuya.

7Iye amatulutsa mitambo kuchokera ku malekezero a dziko lapansi,

amatumiza zingʼaningʼani pamodzi ndi mvula

ndipo amatulutsa mphepo ku malo ake osungiramo.

8Anakantha ana oyamba kubadwa a Igupto,

ana oyamba kubadwa a anthu ndi nyama.

9Iye anatumiza zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa pakati pako, iwe Igupto,

kutsutsana ndi Farao pamodzi ndi atumiki ake onse.

10Iye anakantha mitundu yambiri ya anthu

ndi kupha mafumu amphamvu:

11Sihoni mfumu ya Aamori,

Ogi mfumu ya Basani,

ndi maufumu onse a ku Kanaani;

12ndipo anapereka dziko lawo ngati cholowa,

cholowa cha anthu ake Aisraeli.

13Dzina lanu, Inu Yehova, ndi losatha mpaka muyaya,

mbiri yanu, Inu Yehova, idziwika mibado yonse.

14Pakuti Yehova adzaonetsa kuti anthu ake ngosalakwa,

ndipo adzachitira chifundo atumiki ake.

15Mafano a mitundu ya anthu ndi siliva ndi golide,

opangidwa ndi manja a anthu.

16Pakamwa ali napo koma sayankhula

maso ali nawo, koma sapenya;

17makutu ali nawo, koma sakumva

ndipo mʼkamwa mwawo mulibe mpweya uliwonse.

18Iwo amene amapanga mafanowo adzakhala ngati mafanowo,

chimodzimodzinso iwo amene amadalira mafanowo.

19Inu nyumba ya Israeli, tamandani Yehova;

inu nyumba ya Aaroni, tamandani Yehova;

20Inu nyumba ya Levi, tamandani Yehova;

Inu amene mumaopa Iye, tamandani Yehova.

21Wodalitsika ndi Yehova kuchokera mʼZiyoni,

amene amakhala mu Yerusalemu.

Tamandani Yehova.