詩篇 146 – JCB & CCL

Japanese Contemporary Bible

詩篇 146:1-10

146

1真心から、主をほめたたえましょう。

2私は一生涯、主を賛美し、

生きているかぎり、私の神に賛美の歌を歌います。

3人の助けをあてにしてはいけません。

どんなに偉大な指導者も、頼りにはならないのです。

4人はみな死ぬ運命にあるからです。

呼吸が止まり、いのちの火が消えた瞬間に、

その人の人生の計画は、すべて無になるのです。

5しかし、神の助けをあてにし、

主に望みを置く人は幸せです。

6主は、天と地と海と、

その中のいっさいのものをお造りになりました。

どんな約束でも守り抜き、

7貧しい人や虐待されている人に公平なさばきを保証し、

飢えた人には食べ物をお与えになるお方です。

主は囚人を解放し、

8盲人の目を開き、

身をかがめている人の重荷を取り除かれます。

主は正しい人を愛しておられます。

9主は外国人の権利を守り、

孤児や未亡人を支えますが、

その一方、悪者の計画をくつがえされます。

10エルサレムよ。

あなたの主は、永遠に支配なさる王です。

ハレルヤ。主をほめたたえましょう。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 146:1-10

Salimo 146

1Tamandani Yehova.

Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.

2Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse;

ndidzayimba nyimbo zamatamando kwa Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga.

3Musamadalire mafumu,

anthu osakhalitsa, amene sangathe kupulumutsa.

4Pamene mizimu yawo yachoka, iwo amabwerera ku dothi;

zimene ankafuna kuchita zimatha tsiku lomwelo.

5Wodala ndi amene thandizo lake ndi

Mulungu wa Yakobo.

6Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi,

nyanja ndi zonse zili mʼmenemo;

Yehova, amene ndi wokhulupirika kwamuyaya.

7Iye amachitira chilungamo anthu oponderezedwa

ndipo amapereka chakudya kwa anthu anjala.

Yehova amamasula amʼndende,

8Yehova amatsekula maso anthu osaona,

Yehova amadzutsa onse amene awerama pansi,

Yehova amakonda anthu olungama.

9Yehova amasamalira alendo

ndipo amathandiza ana ndi akazi amasiye,

koma amasokoneza njira za anthu oyipa.

10Yehova ndiye Mfumu mpaka muyaya,

Mulungu wako iwe Ziyoni, pa mibado yonse.

Tamandani Yehova.