Nyimbo za Mayamiko
1Tsiku limenelo aliyense wa inu adzati:
“Ndikukuyamikani, Inu Yehova;
chifukwa ngakhale munandipsera mtima,
mkwiyo wanu wachoka,
ndipo mwanditonthoza.
2Zoonadi, Mulungu ndiye Mpulumutsi wanga;
ndidzamudalira ndipo sindidzachita mantha.
Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;
Iye wakhala chipulumutso changa.”
3Mudzakondwera popeza Yehova
ali ngati chitsime cha chipulumutso chanu.
4Tsiku limenelo mudzati:
“Yamikani Yehova, tamandani dzina lake;
mulengeze ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu,
ndipo mulalike kuti dzina lake ndi lopambana.
5Imbirani Yehova, pakuti wachita ntchito zazikulu;
zimenezi zidziwike pa dziko lonse lapansi.
6Fuwulani ndi kuyimba mwachimwemwe, inu anthu a ku Ziyoni;
pakuti Woyerayo wa Israeli ndi wamkulu pakati panu.”
Ação de Graças
1Naquele dia, você dirá:
“Eu te louvarei, Senhor!
Pois estavas irado contra mim,
mas a tua ira desviou-se,
e tu me consolaste.
2Deus é a minha salvação;
terei confiança e não temerei.
O Senhor, sim, o Senhor
é a minha força e o meu cântico;
ele é a minha salvação!”
3Com alegria vocês tirarão água
das fontes da salvação.
4Naquele dia, vocês dirão:
“Louvem o Senhor, invoquem o seu nome;
anunciem entre as nações os seus feitos,
e façam-nas saber que o seu nome é exaltado.
5Cantem louvores ao Senhor, pois ele tem feito coisas gloriosas,
sejam elas conhecidas em todo o mundo.
6Gritem bem alto e cantem de alegria, habitantes de Sião,
pois grande é o Santo de Israel no meio de vocês”.