Miyambo 3 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Miyambo 3:1-35

Phindu Lina la Nzeru

1Mwana wanga, usayiwale malangizo anga,

mtima wako usunge malamulo anga.

2Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka

ndipo udzakhala pa mtendere.

3Makhalidwe ochitira ena chifundo ndi owonetsa kukhulupirika asakuchokere.

Uwamangirire mʼkhosi mwako ngati mkanda

ndi kuwalemba pa mtima pako.

4Ukatero udzapeza kuyanja ndi mbiri yabwino

pamaso pa Mulungu ndi anthu.

5Uzikhulupirira Yehova ndi mtima wako wonse

ndipo usadalire nzeru zako za kumvetsa zinthu.

6Pa zochita zako zonse uvomereze kuti Mulungu alipo,

ndipo Iye adzawongola njira zako.

7Usamadzione ngati wa nzeru.

Uziopa Yehova ndi kupewa zoyipa.

8Ukatero thupi lako lidzakhala la moyo wabwino

ndi mafupa ako adzakhala olimba.

9Uzilemekeza Yehova ndi chuma chako chonse;

zokolola zonse zoyamba kucha uzilemekeza nazonso Yehova.

10Ukatero nkhokwe zako zidzadzaza ndi zinthu zambiri,

ndiponso mitsuko yako idzadzaza ndi vinyo.

11Mwana wanga usanyoze malangizo a Yehova,

ndipo usayipidwe ndi chidzudzulo chake.

12Paja Yehova amadzudzula amene amamukonda,

monga abambo achitira mwana amene amakondwera naye.

13Wodala munthu amene wapeza nzeru,

munthu amene walandira nzeru zomvetsa zinthu,

14pakuti phindu la nzeru ndi labwino kuposa la siliva,

phindu lakelo ndi labwino kuposanso golide.

15Nzeru ndi yoposa miyala yamtengowapatali;

ndipo zonse zimene umazikhumba sizingafanane ndi nzeru.

16Mʼdzanja lake lamanja muli moyo wautali;

mʼdzanja lake lamanzere muli chuma ndi ulemu.

17Njira zake ndi njira zosangalatsa,

ndipo mu njira zake zonse muli mtendere.

18Nzeru ili ngati mtengo wopatsa moyo kwa oyigwiritsitsa;

wodala munthu amene amayigwiritsa kwambiri.

19Yehova anakhazikitsa dziko lapansi pogwiritsa ntchito nzeru.

Anagwiritsanso ntchito nzeru zakudziwa bwino zinthu pamene ankakhazikitsa zakumwamba.

20Mwa nzeru zake Yehova anatumphutsa madzi kuchokera mʼnthaka

ndiponso mitambo inagwetsa mvula.

21Mwana wanga usunge nzeru yeniyeni ndi khalidwe lomalingarira zinthu bwino.

Zimenezi zisakuchokere.

22Zimenezi zidzakupatsa moyo,

moyo wake wosangalatsa ndi wabwino ngati mkanda wa mʼkhosi.

23Choncho udzayenda pa njira yako mosaopa kanthu,

ndipo phazi lako silidzapunthwa;

24pamene ugona pansi, sudzachita mantha;

ukadzagona pansi tulo tako tidzakhala tokoma.

25Usaope tsoka lobwera mwadzidzidzi

kapena chiwonongeko chimene chidzagwera anthu oyipa,

26pakuti Yehova adzakulimbitsa mtima

ndipo adzasunga phazi lako kuti lisakodwe mu msampha.

27Usaleke kuchitira zabwino amene ayenera kulandira zabwino,

pamene uli nazo mphamvu zochitira zimenezi.

28Usanene kwa mnansi wako kuti,

“Pita, uchite kubweranso. Ndidzakupatsa mawa”

pamene uli nazo tsopano.

29Usamukonzere chiwembu mnansi wako,

amene anakhala nawe pafupi mokudalira.

30Usakangane ndi munthu wopanda chifukwa

pamene iye sanakuchitire zoyipa.

31Usachite naye nsanje munthu wachiwawa

kapena kutsanzira khalidwe lake lililonse.

32Pakuti Yehova amanyansidwa ndi munthu woyipa

koma amayanjana nawo anthu olungama.

33Yehova amatemberera nyumba ya munthu woyipa,

koma amadalitsa nyumba ya anthu olungama.

34Anthu onyoza, Iye amawanyoza,

koma amakomera mtima anthu odzichepetsa.

35Anthu anzeru adzalandira ulemu,

koma zitsiru adzazichititsa manyazi.

Luganda Contemporary Bible

Engero 3:1-35

Emikisa Egiva mu kuba n’amagezi

13:1 Nge 4:5Mwana wange, teweerabiranga bintu bye nakuyigiriza,

era okuumanga ebiragiro byange mu mutima gwo,

23:2 Nge 4:10kubanga bijja kuwangaaza obulamu bwo ku nsi,

era bikukulaakulanye.

33:3 Kuv 13:9; Nge 6:21; 7:3; 2Ko 3:3Amazima n’ekisa tobyerabiranga;

byesibe mu bulago bwo,

obiwandiike ku mutima gwo.

43:4 1Sa 2:26; Luk 2:52Bw’otyo bw’onoofuna okuganja n’okusiimibwa

eri Katonda n’eri abantu.

53:5 Zab 37:3, 5Weesige Mukama n’omutima gwo gwonna,

so teweesigamanga ku magezi go gokka.

63:6 a 1By 28:9 b Nge 16:3; Is 45:13Mukama mukulembezenga mu by’okola byonna,

naye anaakuluŋŋamyanga n’owangula.

73:7 a Bar 12:16 b Yob 1:1; Nge 16:6Amagezi go tegakusigulanga,

naye otyanga Mukama, era weewale okukola ebibi.

83:8 a Nge 4:22 b Yob 21:24Onoofunanga obulamu mu mubiri gwo

n’amagumba go ne gadda buggya.

Amagezi n’Obugagga

93:9 Kuv 22:29; 23:19; Ma 26:1-15Mukama mugulumizenga n’eby’obugagga byo; n’ebibala ebisooka eby’ebintu byo byonna eby’omu nnimiro yo,

103:10 a Ma 28:8 b Yo 2:24olwo amaterekero go lwe ganajjulanga ebintu enkumu,

era n’amasenero go ne gajjula ne gabooga omwenge omusu.

113:11 Yob 5:17Mwana wange tonyoomanga kukangavvula kwa Mukama,

n’okunenya kwe kulemenga okukukooya,

123:12 a Nge 13:24; Kub 3:19 b Ma 8:5; Beb 12:5-6*kubanga Mukama anenya oyo gw’ayagala,

nga kitaawe w’omwana bw’anenya mutabani we gwe yeenyumiririzaamu.

13Aweereddwa omukisa oyo afuna amagezi,

omuntu oyo afuna okutegeera,

143:14 Yob 28:15; Nge 8:19; 16:16kubanga amagezi gasinga ffeeza

era galimu amagoba okusinga zaabu.

153:15 a Yob 28:18 b Nge 8:11Amagezi ga muwendo mungi okusinga amayinja ag’omuwendo omungi:

era tewali kyegombebwa kiyinza kugeraageranyizibwa nago.

163:16 Nge 8:18Mu mukono gwago ogwa ddyo mwe muli obuwanguzi;

ne mu mukono gwago ogwa kkono ne mubaamu obugagga n’ekitiibwa.

173:17 Nge 16:7; Mat 11:28-30Mu magezi mulimu essanyu,

era n’amakubo gaago ga mirembe.

183:18 Lub 2:9; Nge 11:30; Kub 2:7Amagezi muti gwa bulamu eri abo abagakwata ne baganyweza;

abo abagakwata ne baganyweza baliweebwa omukisa.

193:19 a Zab 104:24 b Nge 8:27-29Amagezi, Mukama ge yakozesa okuteekawo emisingi gy’ensi;

n’okutegeera kwe yakozesa okuteekawo eggulu;

20n’okumanya kwe, kwe yakozesa okwawula obuziba bw’ennyanja,

era n’ebire ne bivaamu omusulo.

Ab’amagezi Baweebwa Ekitiibwa

213:21 Nge 4:20-22Mwana wange, beeranga n’okuteesa okulungi n’okusalawo ebisaana,

ebyo biremenga okukuvaako,

223:22 Nge 1:8-9binaabeeranga obulamu eri emmeeme yo,

era ekyokwambala ekirungi ekinaawoomesanga obulago bwo.

233:23 Zab 37:24; Nge 4:12Bw’otyo bw’onootambulanga nga onyweredde mu kkubo lyo,

era ekigere kyo tekijjanga kwesittala.

243:24 a Lv 26:6; Zab 3:5 b Yob 11:18Bw’onoogalamiranga toobenga na kutya,

weewaawo bw’oneebakanga otulo tunaakuwoomeranga.

25Totyanga kabenje kootomanyiridde,

wadde okuzikirira okujjira abakozi b’ebibi,

263:26 1Sa 2:9Kubanga Mukama y’anaabeeranga obwesigwa bwo,

era anaalabiriranga ekigere kyo ne kitakwatibwa mu mutego.

27Tommanga birungi abo be bisaanira

bwe kibeera mu buyinza bwo okukikola.

283:28 Lv 19:13; Ma 24:15Togambanga muliraanwa wo nti,

“Genda, onodda enkya ne nkuwa,”

ate nga kye yeetaaga okirina.

29Totegekanga kukola bulabe ku muliraanwa wo,

atudde emirembe ng’akwesiga.

30Tovunaananga muntu n’omu awatali nsonga

nga talina kabi k’akukoze.

313:31 Zab 37:1; Nge 24:1-2Tokwatirwanga obuggya omuntu ayigganya abalala,

era tokolanga nga ye bw’akola,

323:32 a Nge 11:20 b Yob 29:4; Zab 25:14kubanga omuntu omugwagwa wa muzizo eri Mukama,

naye abo abagolokofu abalinamu obwesige.

333:33 a Ma 11:28; Mal 2:2 b Zek 5:4 c Zab 1:3Ekikolimo kya Mukama kiri ku nnyumba y’ababi,

naye awa omukisa ennyumba y’abatuukirivu.

343:34 Yak 4:6*; 1Pe 5:5*Ddala ddala, Mukama anyooma abanyoomi,

naye abeetoowaza abawa ekisa.

35Ab’amagezi balisikira ekitiibwa,

naye abasirusiru baliswazibwa.