Masalimo 8 – CCL & BDS

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 8:1-9

Salimo 8

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide.

1Inu Yehova Ambuye athu,

dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!

Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu

mʼmayiko onse akumwamba.

2Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda,

Inu mwakhazikitsa mphamvu

chifukwa cha adani anu,

kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.

3Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba,

ntchito ya zala zanu,

mwezi ndi nyenyezi,

zimene mwaziyika pa malo ake,

4munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira,

ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?

5Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba

ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.

6Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu;

munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;

7nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi

ndi nyama zakuthengo,

8mbalame zamlengalenga

ndi nsomba zamʼnyanja

zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.

9Inu Yehova, Ambuye athu,

dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!

La Bible du Semeur

Psaumes 8:1-10

Grandeur de Dieu et de l’homme

1Au chef de chœur. Un psaume de David, (à chanter avec accompagnement) de la harpe de Gath8.1 Sens incertain. On pense qu’il s’agit soit d’une harpe de Gath, la ville de Philistie, soit d’un chant de vendange et de pressoir (voir Ps 81.1 et 84.1)..

2Eternel, notre Seigneur,

que ta gloire est admirable ╵sur la terre tout entière !

Au-dessus du ciel, ╵on célèbre ta splendeur8.2 Hébreu obscur..

3De la bouche des petits enfants ╵et des nourrissons,

tu fais jaillir la louange8.3 D’après les versions anciennes ; cf. Mt 21.16, qui cite ce texte sous cette même forme. Texte hébreu traditionnel : tu as fondé ta force. ╵à l’encontre de tes adversaires,

pour imposer le silence ╵à l’ennemi plein de hargne.

4Quand je contemple le ciel ╵que tes doigts ont façonné,

les étoiles et la lune ╵que tes mains ont disposées,

5je me dis : Qu’est-ce que l’homme, ╵pour que tu en prennes soin,

et qu’est-ce qu’un être humain ╵pour qu’à lui tu t’intéresses8.5 Voir 144.3 ; Jb 7.17-18. Les v. 5-7 sont cités en Hé 2.6-8 ; le v. 7 en 1 Co 15.27 ; Ep 1.22. ?

6Pourtant, tu l’as fait ╵de peu inférieur à Dieu8.6 Autre traduction : inférieur aux êtres célestes.,

tu l’as couronné ╵de gloire et d’honneur.

7Tu lui donnes de régner ╵sur les œuvres de tes mains.

Tu as tout mis sous ses pieds :

8tout bétail, gros ou petit,

et les animaux sauvages,

9tous les oiseaux dans les airs ╵et les poissons de la mer,

tous les êtres qui parcourent ╵les sentiers des mers.

10Eternel, notre Seigneur,

que ta gloire est admirable ╵sur la terre tout entière.