Salimo 72
Salimo la Solomoni.
1Patsani mwana wa mfumu nzeru zanu zoweruzira mwa chilungamo,
Inu Mulungu mupatseni mwana wa mfumu chilungamo chanu.
2Iye adzaweruza anthu anu mwachilungamo,
anthu anu ozunzika mosakondera.
3Mapiri adzabweretsa chuma kwa anthu anu,
timapiri tidzabweretsa zipatso zachilungamo.
4Iye adzateteza ozunzika pakati pa anthu
ndi kupulumutsa ana a anthu osowa;
adzaphwanya ozunza anzawo.
5Adzakhala ndi moyo pa mibado yonse,
nthawi zonse pamene dzuwa ndi mwezi zikuwala.
6Iye adzakhala kugwa kwa mvula pa minda yolimidwa
ngati mivumbi yothirira dziko lapansi.
7Mʼmasiku a munthu wolungama adzakhazikika;
chuma chidzachuluka mpaka mwezi utaleka kuwala.
8Iye adzalamulira kuchokera ku nyanja ina mpaka ku nyanja ina
ndiponso kuchokera ku mtsinje mpaka ku malekezero a dziko lapansi.
9Mafuko a mʼchipululu adzawerama pamaso pake
ndipo adani ake adzanyambita fumbi.
10Mafumu a ku Tarisisi ndi a ku zilumba zakutali
adzabweretsa mitulo kwa iye,
mafumu a ku Seba ndi Seba
adzapereka mphatso kwa iyeyo.
11Mafumu onse adzamuweramira
ndipo mitundu yonse idzamutumikira.
12Pakuti iye adzawombola wosowa amene akulira,
wozunzika amene alibe wina womuthandiza.
13Iye adzachitira chifundo anthu ofowoka ndi anthu osowa
ndi kupulumutsa osowa ku imfa.
14Iye adzalanditsa iwo ku mazunzo ndi chiwawa
pakuti magazi awo ndi amtengo wapatali pamaso pake.
15Iye akhale ndi moyo wautali;
golide ochokera ku Seba apatsidwe kwa iye.
Anthu amupempherere nthawi zonse
ndi kumudalitsa tsiku lonse.
16Mulole kuti tirigu achuluke mʼdziko lonse;
pamwamba pa mapiri pakhale tirigu.
Zipatso zake zichuluke ngati za ku Lebanoni;
zichuluke ngati udzu wakuthengo
17Dzina lake likhazikike kwamuyaya,
lipitirire kukhala monga momwe limakhalira dzuwa.
Mitundu yonse idzadalitsika kudzera mwa iye
ndipo iwo adzamutcha iye wodala.
18Matamando akhale kwa Yehova Mulungu, Mulungu wa Israeli
amene Iye yekha amachita ntchito zodabwitsa.
19Matamando akhale ku dzina lake laulemerero kwamuyaya
dziko lonse lapansi lidzaze ndi ulemerero wake.
Ameni ndi Ameni.
20Uku ndiko kumaliza kwa mapemphero a Davide mwana wa Yese.
Третья книга
Песнь 72
Песнь Ософа.
1Истинно, Всевышний благ к Исроилу,
к тем, чьё сердце чисто!
2А мои ноги едва не поскользнулись,
стопы мои чуть не потеряли опору,
3потому что я позавидовал надменным,
увидев процветание нечестивых.
4Нет им страданий;
они полны здоровья и силы72:4 Или: «Нет им страданий до самой смерти (или: при смерти); они полны силы»..
5Они свободны от тягот человеческих,
и трудностей людских они не знают.
6И поэтому гордость – их ожерелье,
а жестокость – их одеяние.
7Вылезли от тучности глаза их;
их тщеславие не знает границ.
8Слова их полны издевательства и злобы,
и в своей надменности угрожают насилием.
9Открывают уста свои против небес
и ходят по земле, ведя праздные разговоры.
10Потому к ним же обращается народ Всевышнего
и пьёт слова их, как воду из полной чаши.
11Они говорят: «Как может узнать Бог?
Есть ли знание у Высочайшего?»
12Таковы нечестивые:
они всегда беззаботны
и умножают своё богатство.
13Так не напрасно ли я хранил сердце своё в чистоте
и омывал руки свои в невинности?
14Каждый день я подвергался мучениям
и был наказываем каждое утро.
15Но если бы я решил, что буду рассуждать так,
то предал бы народ Твой.
16Когда я пытался всё это понять,
то мне это казалось слишком трудным,
17пока я не вошёл в святилище Всевышнего
и не понял, какой конец ожидает нечестивых.
18Истинно, на скользких путях Ты ставишь их
и предаёшь их полному разрушению.
19Как неожиданно они истреблены,
погибают от ужаса!
20Как сновидение исчезает при пробуждении,
так пропадают и нечестивые, когда встаёшь Ты, Владыка.
21Когда моё сердце наполняла горечь
и терзалась моя душа,
22я был невежествен и ничего не понимал;
как неразумное животное я был пред Тобою.
23И всё же я всегда с Тобою:
Ты держишь меня за правую руку;
24Ты руководишь мною Своим советом
и потом к славе поведёшь меня.
25Кто есть у меня на небесах, кроме Тебя?
И на земле я ничего, кроме Тебя, не желаю.
26Ослабевает моя плоть и моё сердце,
но Всевышний – сила сердца моего
и часть моя навсегда.
27Те, кто далёк от Тебя, погибнут;
Ты губишь всех, кто неверен Тебе.
28А для меня благо приближаться к Всевышнему;
Владыку Вечного я сделал своим убежищем.
Я возвещу о всех делах Твоих.