Masalimo 67 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 67:1-7

Salimo 67

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

achititse kuti nkhope yake itiwalire.

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo

ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

6Nthaka yabereka zokolola zake;

tidalitseni Mulungu wathu.

7Mulungu atidalitse

kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 67:1-7

Zabbuli 67

Ya Mukulu wa Bayimbi. Ebivuga eby’enkoba. Zabbuli. Oluyimba.

167:1 Kbl 6:24-26; Zab 4:6Ayi Katonda tukwatirwe ekisa, otuwe omukisa,

era otwakize amaaso go.

267:2 a Is 52:10 b Tit 2:11Ekkubo lyo limanyibwe mu nsi,

n’obulokozi bwo mu mawanga gonna.

3Abantu bakutenderezenga, Ayi Katonda,

abantu bonna bakutenderezenga.

467:4 Zab 96:10-13Amawanga gonna gasanyuke, gayimbe nga gajjudde essanyu.

Kubanga ofuga abantu bonna mu bwenkanya,

n’oluŋŋamya amawanga ag’ensi.

5Abantu bakutenderezenga, Ayi Katonda,

abantu bonna bakutenderezenga.

667:6 Lv 26:4; Zab 85:12; Ez 34:27Ensi erireeta amakungula gaayo;

era Katonda, Katonda waffe, anaatuwanga omukisa.

767:7 Zab 33:8Katonda anaatuwanga omukisa;

n’enkomerero z’ensi zinaamutyanga.