Masalimo 26 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 26:1-12

Salimo 26

Salimo la Davide.

1Weruzeni Inu Yehova

pakuti ndakhala moyo wosalakwa.

Ndadalira Yehova

popanda kugwedezeka.

2Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni,

santhulani mtima wanga ndi maganizo anga;

3pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse,

ndipo ndimayenda mʼchoonadi chanu nthawi zonse.

4Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo,

kapena kufunsa nzeru kwa achiphamaso.

5Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa

ndipo ndimakana kukhala pansi pamodzi ndi oyipa.

6Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga

ndi kupita kukatumikira pa guwa lanu la nsembe, Inu Yehova,

7kulengeza mofuwula za matamando anu

ndi kuwuza onse za ntchito zanu zodabwitsa.

8Ndimakonda Nyumba imene Inu Yehova mumakhalamo,

malo amene ulemerero wanu umapezekako.

9Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa,

moyo wanga pamodzi ndi anthu akupha anzawo,

10amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa,

dzanja lawo lamanja ladzaza ndi ziphuphu.

11Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa;

mu msonkhano wa anthu anu ndidzatamanda Yehova.

12Ndayima pa malo wopanda zovuta

ndipo ndidzatamanda Yehova mu msonkhano waukulu.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 26:1-12

Zabbuli 26

Zabbuli ya Dawudi.

126:1 a Zab 7:8; Nge 20:7 b Zab 28:7 c 2Bk 20:3; Beb 10:23Onnejjeereze, Ayi Mukama,

kubanga obulamu bwange tebuliiko kya kunenyezebwa;

nneesiga ggwe, Ayi Mukama,

nga sibuusabuusa.

226:2 a Zab 17:3 b Zab 7:9Neetegereza, Ayi Mukama, ongezese;

weekalirize ebiri mu mutima gwange ne mu mmeeme yange.

326:3 2Bk 20:3Kubanga okwagala kwo kwe kunkulembera,

era mu mazima go mwe ntambulira.

426:4 Zab 1:1Situula na bantu balimba,

so siteesaganya na bakuusa.

526:5 Zab 31:6; 139:21Nkyawa ekibiina ky’aboonoonyi;

so situula na bakozi ba bibi.

626:6 Zab 73:13Naaba mu ngalo zange okulaga nga bwe sirina misango;26:6 Okunaaba mu ngalo mu lujjudde, kaali kabonero akalaga ng’omuntu oyo bw’atalina musango

ne ndyoka nzija ku Kyoto kyo, Ayi Mukama;

726:7 Zab 9:1ne nnyimba oluyimba olw’okwebaza,

olwogera ku bikolwa byo ebyewuunyisa.

826:8 Zab 27:4Ennyumba yo mw’obeera njagala, Ayi Mukama,

kye kifo ekijjudde ekitiibwa kyo.

926:9 Zab 28:3Tombalira mu boonoonyi,

wadde mu batemu,

1026:10 1Sa 8:3abakozesa emikono gyabwe okutegeka ebikolwa ebibi,

era abali b’enguzi.

1126:11 Zab 69:18Naye nze ntambula nga siriiko kye nnenyezebwa;

nkwatirwa ekisa, Ayi Mukama, ondokole.

1226:12 a Zab 27:11; 40:2 b Zab 22:22Nnyimiridde watereevu.

Nnaatenderezanga Mukama mu kibiina ky’abantu ekinene.